< תהילים 100 >
מזמור לתודה הריעו ליהוה כל-הארץ | 1 |
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
עבדו את-יהוה בשמחה באו לפניו ברננה | 2 |
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
דעו-- כי יהוה הוא אלהים הוא-עשנו ולא (ולו) אנחנו-- עמו וצאן מרעיתו | 3 |
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
באו שעריו בתודה--חצרתיו בתהלה הודו-לו ברכו שמו | 4 |
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
כי-טוב יהוה לעולם חסדו ועד-דר ודר אמונתו | 5 |
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.