< Halelu 28 >

1 I A oe, e Iehova, e kahea aku ai au e kuu pohaku, mai hookuli mai oe ia'u; O like auanei au me ka poe iho ilalo o ka Iua, ke hookuli mai oe ia'u.
Salimo la Davide. Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa; musakhale osamva kwa ine. Pakuti mukapitirira kukhala chete, ndidzakhala ngati iwo amene atsikira ku dzenje.
2 E hoolohe mai i ka leo o ka'u pule, i ko'u kahea ana'ku ia oe, I ka hapai ana o kuu mau lima i kou wahi hoano.
Imvani kupempha chifundo kwanga pomwe ndikuyitana kwa Inu kuti mundithandize, pomwe ndikukweza manja anga kuloza ku malo anu oyeretsetsa.
3 Mai alako ae ia'u me ka poe aia, me ka poe hana hewa, Ka poe olelo aloha i ko lakou mau hoalauna, He hewa no nae maloko o ko lakou mau naau.
Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa, pamodzi ndi iwo amene amachita zoyipa, amene amayankhula mwachikondi ndi anzawo koma akusunga chiwembu mʼmitima mwawo.
4 E haawi ia lakou e like me ka lakou mau hana; A mamuli o ka hewa o ko lakou hooikaika ana; E haawi ia lakou mamuli o ka hana o ko lakou mau lima; E uku ia lakou no ka lakou hana.
Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo ndi ntchito zawo zoyipa; abwezereni chifuwa cha zimene manja awo achita ndipo mubweretse pa iwo zimene zowayenera.
5 No ka mea, aole lakou i manao i na hana a Iehova, Aole hoi i ka hana ana o kona mau lima, E wawahi oia ia lakou, aole e kukulu ia lakou iluna.
Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova, ndi zimene manja ake anazichita, Iye adzawakhadzula ndipo sadzawathandizanso.
6 E hoomaikaiia'ku o Iehova, No ka mea, ua hoolohe mai no ia i ka leo a ka'u mau pule.
Matamando apite kwa Yehova, popeza Iye wamva kupempha chifundo kwanga.
7 O Iehova kuu ikaika a me kuu palekaua; Ia ia i hilinai ai kun naau, a ua kokuaia mai au; Nolaila i hauoli nui ai kuu naau, A ma kuu mele e hoolea aku ai au ia ia.
Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa; mtima wanga umadalira Iye, ndipo Ine ndathandizidwa. Mtima wanga umalumphalumpha chifukwa cha chimwemwe ndipo ndidzayamika Iye mʼnyimbo.
8 O Iehova ko lakou ikaika; Oia hoi ka ikaika e ola'i kona mea i poniia.
Yehova ndi mphamvu ya anthu ake, linga la chipulumutso kwa wodzozedwa wake.
9 E hoola i kou poe kanaka, a e hoomaikai i kou hooilina: E hanai ia lakou, a e kaikai ia lakou a mau loa.
Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu; mukhale mʼbusa wawo ndipo muwakweze kwamuyaya.

< Halelu 28 >