< Solomona 30 >

1 HE mau wahi olelo a Agura ke keiki a Iake. He wanana; na ke kanaka i hoike mai ia Itiela; ia Itiela laua me Ukala.
Nawa mawu a Aguri mwana wa Yake wa ku Masa: Munthuyo anati kwa Itieli, “Inu Mulungu, ine ndatopa. Inu Mulungu, ine ndatopa. Ndalefukiratu.
2 Owau ka mea hupo loa o na kanaka, Aole o'u wahi noonoo kanaka.
“Ine ndine munthu wopusa kuposa anthu onse; ndilibe nzeru zomvetsa zinthu zonga za munthu.
3 Aole i loaa ia u ka naauao, Aole hoi o'u ike i ka Mea hemolele.
Sindinaphunzire nzeru, ndipo Woyerayo sindimudziwa.
4 Owai ka mea i pii ae i ka lani, a i iho mai hoi? Owai ka mea i hooiliili i ka makani ma kona lima? Owai ka mea i hoopaa i na wai ma kona aahu? Owai ka mea i hoonoho i na welelau a pau o ka honua? Owai hoi kona inoa, owai ka inoa o kana keiki? E hoike mai paha oe.
Kodi ndani anakwera kumwamba ndi kutsikako? Ndani anafumbatapo mphepo mʼmanja mwake? Ndani anamanga madzi mʼchovala chake? Ndani anakhazikitsa mathero onse a dziko lapansi? Dzina lake ndani? Ndiwuze ngati ukudziwa! Ndipo mwana wake dzina lake ndani?
5 Pau loa na huaolelo a ke Akua i ka maemae; Oia ka palekaua i ka poe paulele aku ia ia.
“Mawu ali wonse a Mulungu ndi opanda cholakwika; Iye ndi chishango kwa amene amathawira kwa Iye.
6 Mai hui ae oe i kekahi mea me kana mau huaolelo, O ao mai oia ia oe, a e lilo oe i mea wahahee.
Usawonjezepo kanthu pa mawu ake, kuopa kuti Iye angadzakudzudzule ndi kukupeza kuti ndiwe wabodza.”
7 Elua mau mea a'u i noi aku ai ia oe, Mai aua oe mamua o ko'u make ana.
“Inu Yehova, ndikukupemphani zinthu ziwiri musandimane zimenezo ndisanafe:
8 O ka lapuwale, a o ka wahahee, E hookaawale ae mai o'u aku nei; Mai haawi mai ia'u i ka ilihune, aole hoi i ka waiwai; E hanai mai ia'u i ka ai ku pono no'u;
Choyamba, mundichotsere kutali nane mabodza ndi chinyengo. Chachiwiri, ndisakhale mʼmphawi kapena munthu wachuma. Koma muzindidyetsa chakudya chondikwanira tsiku ndi tsiku
9 O hookuku ai au, a hoole aku hoi, Me ka i ana, Owai la o Iehova? O ilihune hoi au a aihue iho, A hoohiki ino i ka inoa o ko'u Akua.
kuopa kuti ndikakhuta kwambiri ndingayambe kukukanani, nʼkumanena kuti, ‘Yehova ndiye yaninso?’ Kuopanso kuti ndikakhala wosauka ndingayambe kuba, potero nʼkuyipitsa dzina la Mulungu wanga.”
10 Mai hoopii oe i ke kauwa imua o kona haku, O hooino mai oia ia oe, a e lilo oe i lawehala.
“Usamusinjirire wantchito kwa mbuye wake kuopa kuti angakutemberere ndipo iweyo nʼkupezeka wolakwa.”
11 O kekahi hanauna, hoino no i ka makuakane, Aole hoi i hoomaikai i ka makuwahine.
“Alipo ena amene amatemberera abambo awo, ndipo sadalitsa amayi awo.
12 O kekahi hanauna hoi, he maemae ia i ko lakou maka iho, Aole hoi i holoiia ka paumaele.
Pali ena amene amadziyesa okha oyera mtima komatu sanachotse zoyipa zawo.
13 O kekahi hanauna, hookano loa na maka o lakou! Hookiekie hoi na lihilihi o lakou.
Pali ena ndi odzitukumula kwambiri, amene amakweza zikope modzitukumula.
14 O kekahi hanauna, he mau pahikaua ko lakou niho, He mau pahi hoi ko lakou mau kui. E ai ana i ka poe ilihune mai ka honua aku, A o ka poe nele hoi iwaena o na kanaka.
Pali ena amene mano awo ali ngati malupanga ndipo zibwano zawo zili ngati mipeni moti amadya amphawi ndi kuwachotsa pa dziko lapansi. Amachotsanso anthu osauka pakati pa anzawo.”
15 He mau kaikamahine elua ka ka omokoko, E i ana, E ho mai, e ho mai, ea. Akolu no mea piha ole, Eha hoi, aole e olelo mai, Ua ana:
“Msundu uli ndi ana aakazi awiri iwo amalira kuti, ‘Tipatseni! Tipatseni!’” “Pali zinthu zitatu zimene sizikhuta, zinthu zinayi zimene sizinena kuti, ‘Takhuta!’
16 O ka lua, o ka opu pa; A o ka honua i mauu ole i ka wai; A o ke ahi, aole ana olelo mai, Ua nui. (Sheol h7585)
Manda, mkazi wosabala, nthaka yosakhuta madzi ndiponso moto womangoyakirayakira!” (Sheol h7585)
17 O ka maka i hoowahawaha i kona makuakane, A hoole hoi aole e malama i kona makuwahine, E kiko iho ka poe koraka o ke awawa ia mea, A e ai iho no ka poe aito opiopio.
Aliyense amene amanyoza abambo ake, ndi kunyozera kumvera amayi ake, makwangwala a ku chigwa adzamukolowola maso ndipo mphungu zidzadya mnofu wake.
18 Ekolu mau mea kupanaha loa ia'u, Eha hoi, aole au i ike iho.
Pali zinthu zitatu zimene zimandidabwitsa, zinthu zinayi zimene ine sindizimvetsetsa.
19 O ka aoao o ka aito ma ka lewa; O ka aoao o ka nahesa maluna o ka pohaku; O ka aoao o ka moku iwaena o ka moana; A o ka aoao o ke kanaka me ka wahine puupaa.
Ndipo ndi izi: mmene chiwulukira chiwombankhanga mlengalenga; mmene iyendera njoka pa thanthwe; mmene chiyendera chombo pa nyanja; ndiponso mmene mwamuna achitira akakhala ndi namwali.
20 Peneia ka aoao o ka wahine hookamakama, Ai iho la oia a holoi i kona nuku, A olelo ae, Aole au i hana hewa.
Umu ndi mʼmene mkazi amachitira atachita chigololo: Atatha kudya ndi kupukuta pakamwa pake iye amanena kuti “Sindinachite kalikonse kolakwa.”
21 Ekolu mau mea e haunaele ai ka honua, Eha hoi e hiki ole ai ke hoomanawanui:
Pali zinthu zitatu zimene zimanjenjemeretsa dziko lapansi, pali zinthu zinayi zimene dziko lapansi silingathe kuzipirira:
22 O ke kauwa ke lilo i alii; O ka mea lapuwale ke maona i ka ai;
Kapolo amene wasanduka mfumu, chitsiru chimene chakhuta,
23 O ka wahine huhu wale ke mareia oia; A o ke kauwawahine he hooilina o kona hakuwahine.
mkazi wonyozeka akakwatiwa ndiponso wantchito wamkazi akalanda mwamuna wa mbuye wake.
24 Eha mau mea liilii loa ma ka honua nei, A ua akamai loa no nae:
Pali zinthu zinayi zingʼonozingʼono pa dziko lapansi, komatu ndi zochenjera kwambiri:
25 O ka poe anonanona, he poe ikaika ole lakou, Hoomakaukau no nae i ke kau i ka lakou ai;
Nyerere zili ngati anthu opanda mphamvu, komatu zimasungiratu chakudya chake nthawi ya chilimwe;
26 O ka poe rabita, he poe nawaliwali lakou, Ma na pohaku hoi i hana'i i ko lakou mau hale;
mbira zili ngati anthu opanda mphamvu komatu zimakonza pokhalapo pawo mʼmiyala;
27 O ka poe uhini, aole o lakou alii, Hele papa no hoi lakou.
dzombe lilibe mfumu, komatu lonse limakhala mʼmagulumagulu poyenda.
28 O ka moo, lalau no oia me kona mau lima, Aia no ia ma na hale hanohano o ke alii.
Buluzi ungathe kumugwira mʼmanja komatu amapezeka mʼnyumba za mafumu.
29 Ekolu mau mea, i maikai ka hele ana, Eha hoi i maikai ke hele ae.
“Pali zinthu zitatu zimene zimayenda chinyachinya, pali zinthu zinayi zimene zimayenda monyadira:
30 O ka liona ka mea ikaika loa o na holoholona, Aole hoi oia e huli ae mai ke alo aku o lakou a pau;
Mkango umene uli wamphamvu kuposa nyama zonse, ndipo suthawa kanthu kalikonse.
31 O ka ilio hahai, a o ke kao kane hoi, A o ke alii, hiki ole ke ku e ia ia.
Tambala woyenda chinyachinya, mbuzi yayimuna, ndiponso mfumu yoyenda pakati pa anthu ake.
32 Ina he lapuwale oe i kou hookiekie ana, Ina paha he manao ino kou, e kau ana ka lima ma ka waha.
“Ngati wakhala ukupusa ndi kumadzikweza wekha, kapena ngati wakhala ukukonzekera zoyipa, ndiye khala kaye chete, uganizire bwino!
33 Ma ka hooluliluli ana i ka waiu e puka mai ai ka bata, Ma ka uwi ana i ka ihu e kahe mai ai ke koko; A ma ka hooioi ana i ka huhu e puka mai ai hoi ka hakaka.
Paja pakutha mkaka mafuta amapangidwa, ndipo ukapsinya mphuno, magazi amatuluka, ndipo mikangano imakhalapo ukalimbikira kukwiya.”

< Solomona 30 >