< Mika 1 >

1 KA olelo a Iehova ka mea i hiki mai ia Mika no Moreseta, i na la o Iotama, Ahaza, a o Hezekia, na'lii o ka Iuda, ka mea ana i ike ai no Samaria, a no Ierusalema.
Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu.
2 E hoolohe, e na kanaka a pau; E haliu mai, e ka honua, a me kona mea i piha ai: A e lilo o Iehova ka Haku i mea hoike ku e ia oukou, O ka Haku mai kona luakini hoano mai.
Tamverani, inu anthu a mitundu yonse, mvetsera iwe dziko lapansi ndi okhala mʼmenemo, pakuti Ambuye Yehova achitira umboni wokutsutsani, Ambuye akuyankhula ali mʼnyumba yake yopatulika.
3 No ka mea, aia hoi, e hele mai o Iehova mai kona wahi mai, A e iho ilalo a e hehi maluna o na wahi kiekie o ka honua.
Taonani! Yehova akubwera kuchokera ku malo ake; Iye akutsika ndipo akuponda pa malo okwera a dziko lapansi.
4 A hehee na mauna malalo iho ona, A e wahiia na awawa, E like me ke kepau imua o ke ahi, A me ka wai i nininiia ma kahi pali.
Mapiri akusungunuka pansi pake, ndipo zigwa zikugawikana ngati phula pa moto, ngati madzi ochokera mʼphiri.
5 No ka lawehala ana o ka Iakoba keia mea a pau, a no na hewa o ko ka hale o Iseraela. He aha ka hala o ka Iakoba? aole anei o Samaria? A owai na wahi kiekie o Iuda? aole anei o Ierusalema?
Zonsezi ndi chifukwa cha cholakwa cha Yakobo, chifukwa cha machimo a nyumba ya Israeli. Kodi cholakwa cha Yakobo nʼchiyani? Kodi si Samariya? Kodi malo achipembedzo a Yuda ndi ati? Kodi si Yerusalemu?
6 A e hoohalike au ia Samaria me he puu la o ke kula, A me he wahi kanu la no ka pawaina; A e hoolei iho au i na pohaku ona ma ke awawa, A e hoike aku au i kona mau kahua.
“Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja, malo odzalamo mphesa. Miyala yake ndidzayitaya ku chigwa ndipo ndidzafukula maziko ake.
7 A e ulupaia kona mau kii kalai a pau, A o kona waiwai moe kolohe e puhiia i ke ahi, A e luku aku au i kona mau kii a pau: No ka mea, ua loaa ia ia ua mea la no ka uku o ka wahine moe kolohe, A e hoihoiia aku ia i ka uku o ka wahine moe kolohe.
Mafano ake onse ndidzawaphwanyaphwanya; mphatso zake zonse ndidzazitentha ndi moto; ndidzawononga zifanizo zonse za milungu yake. Popeza analandira mphatso zake kuchokera ku malipiro a akazi achiwerewere, mphatsozonso zidzagwiritsidwa ntchito ndi ena ngati malipiro a akazi achiwerewere.”
8 No keia mea, e auwe iho au, a e aoa, A e hele wale au, me ke kapa aahu ole; E hoohalike au i ka auwe ana me ko ka ilio hihiu, A i ka alala ana me ko ka iana wahine.
Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni; ndidzayenda wopanda nsapato ndi wamaliseche. Ndidzafuwula ngati nkhandwe ndi kulira ngati kadzidzi.
9 No ka mea, o kona eha he eha make ia, a ua hiki mai ia i ka Iuda; Ua hiki mai i ka pukapa o kou poe kanaka, a i Ierusalema.
Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika; chafika ku Yuda. Chafika pa chipata chenicheni cha anthu anga, mpaka mu Yerusalemu mwenimwenimo.
10 Mai hai aku oukou ia ma Gata, mai auwe oukou i ka auwe ana; Ma ka hale o Apera e kau i ka lepo maluna iho ou.
Musanene zimenezi ku Gati; musalire nʼkomwe. Mugubuduzike mu fumbi ku Beti-Leafura.
11 E hele aku oe, e ka mea e noho ana ma Sapira, me kou hilahila uhi ole; Aole i hele mai iwaho ka mea o noho ana ma Zaanana, ma ka auwe ana o Betezela; E lawe no ia i kona noho ana mai o oukou aku.
Inu anthu okhala ku Safiro, muzipita ku ukapolo muli amaliseche ndi amanyazi. Iwo amene akukhala ku Zanaani sadzatuluka. Beti-Ezeli akulira mwachisoni; chitetezo chake chakuchokerani.
12 No ka mea, o ka mea e noho ana ma Marota, ua nawaliwali ia no ka iini i ka maikai; Aka, iho mai la ka ino mai Iehova mai ma ka pukapa o Ierusalema.
Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu, akuyembekezera thandizo, chifukwa Yehova wabweretsa tsoka, lafika mpaka pa chipata cha Yerusalemu.
13 E ka mea o noho la ma Lakisa, e hoopaa i ka halekaa i ka lio mama; Oia ke poo o ka hewa no ke kaikamahine o Ziona; No ka mea, ua loaa na lawehala o ka Iseraela iloko ou.
Inu anthu okhala ku Lakisi mangani akavalo ku magaleta. Inu amene munayamba kuchimwitsa mwana wamkazi wa Ziyoni, pakuti zolakwa za Israeli zinapezeka pakati panu.
14 No ia mea, e haawi aku oe i na makana no Moresetagata: E lilo na hale o Akeziba i mea hoopunipuni no na'lii o ka Iseraela.
Chifukwa chake perekani mphatso zolawirana ndi a ku Moreseti Gati. Mzinda wa Akizibu udzaonetsa kunama kwa mafumu a Israeli.
15 Aka hoi, e lawe mai no au i hooilina nou, e ka mea e noho ana ma Maresa: A e hele mai ka nani o ka Iseraela i Adulama.
Ndidzabweretsa mgonjetsi kudzalimbana ndi inu okhala mu Maresa. Ulemerero wa Israeli udzafika ku Adulamu.
16 E hooohule oe, a e ako i ke oho no na keiki o kou makemake; E hoomahuahua oe i kou ohule ana, e like me ka aeto; No ka mea, ua hele pio aku la lakou mai ou aku la.
Metani mipala mitu yanu kuonetsa kuti mukulirira ana anu amene mumawakonda; mudzichititse dazi ngati dembo, pakuti anawo adzatengedwa pakati panu kupita ku ukapolo.

< Mika 1 >