< Ezekiela 41 >

1 MAHOPE iho, lawe mai la oia ia'u i ka luakini, a ana'e la hoi oia i na kia eono kubita ka laula ma kela aoao, a eono kubita ka laula ma keia aoao, ma ka laula o ka halelewa.
Ndipo munthuyo anapita nane mʼchipinda chopatulika cha Nyumba ya Mulungu ndipo anayeza khonde lake; mulifupi mwa khondelo munali mamita atatu mbali iliyonse kutalika kwake.
2 A o ka laula o ka ipuka he umi kubita, a o na aoao o ka ipuka elima kubita ma kekahi aoao, elima hoi ma kekahi aoao: a ana'e la oia i kona loa hookahi kanaha kubita, a o kona laula iwakalua kubita.
Mulifupi mwa khomo munali motalika mamita asanu. Makoma a mbali zonse anali a mamita awiri ndi theka mulifupi mwake. Anayezanso kutalika kwa chipinda chopatulika chija ndipo mulitali mwake munali motalika mamita makumi awiri ndi mulifupi mwake munali mamita khumi.
3 A komo ae la ia iloko, a ana'e la oia i na kia o ka ipuka elua kubita, a o ke pani eono kubita, a o ka laula o ka ipuka ehiku kubita.
Kenaka munthuyo anakalowa mʼkati ndipo anayeza khonde la pa khomo; khondelo linali mita imodzi mulifupi mwake. Mulifupi mwa khondelo munali mamita atatu.
4 A ana ae la oia i kona loa iwakalua kubita, a me ka laula iwakalua kubita mamua o ka luakini: a olelo mai la oia ia'u, Eia ka wahi hoano loa.
Ndiponso anayeza kutalika kwa chipinda chopatulika chenichenicho. Mulitali mwake munali mamita khumi, ndipo mulifupi mwake munali mamita khumi. Munthuyo anandiwuza kuti, “Ichi ndicho chipinda chopatulika kwambiri.”
5 Alaila ana'e la oia i ka paia o ka hale, eono kubita, a me ka laula o kela keena aoao, o keia keena aoao, eha kubita, a puni ka hale ma na aoao a pau.
Tsono munthuyo anayeza khoma la Nyumba ya Mulungu; kuchindikira kwake kunali mamita atatu. Panalinso zipinda zina kuzungulira Nyumba ya Mulungu ndipo chilichonse chinali cha mamita awiri mulifupi wake.
6 A o na keena aoao he kanakolukumamakolu no ia e pili ana kekahi aoao i kekahi aoao, a komo ae la ia mau mea i ka paia o ka hale, ka mea no na keena aoao a puni, i paa lakou, aole hoi lakou i paa iloko o ka paia o ka hale.
Zipindazo zinali zitatu zosanjikizana. Chigawo chilichonse chinali ndi zipinda makumi atatu. Pa makoma a Nyumba ya Mulungu panali zochirikiza zipindazo kuti zisatsamire khoma la Nyumba ya Mulungu.
7 A ua hoomahuahuaia'e, a ua hoopuniia'e ka pii ana'e i na keena aoao; no ka mea, o ka hoopuni ana'e o ka hale, ua pii ae ia iluna a puni ka hale; nolaila o ka laula o ka hale maluna'e no ia, a pela i mahuahua'e mai lalo a luna mawaena hoi.
Zipinda za mʼmbalizo zinkapita zikulirakulira pomakwera chipinda ndi chipinda potsata kukulirakulira kwa zochirikiza za zipinda zija. Pambali pa Nyumba ya Mulungu panali makwerero okwerera pamwamba, kuchokera chigawo chapansi kudzera chapakati, mpaka kukafika pamwamba.
8 Nana aku la hoi au i ke kiekie o ka hale a puni; o na kumu o na keena aoao, he ohe okoa o na kubita nui eono.
Ndinaona chiwundo kuzungulira Nyumba ya Mulungu. Chinapanga maziko a zipindazo ndipo chinali cha mamita atatu.
9 O ka manoanoa o ka paia, no ke keena aoao mawaho, elima kubita ia; a o ke koena o ka hale, no na keena aoao oloko ia.
Khoma lakunja la zipindazo linali la mamita awiri ndi theka kuchindikira kwake. Pakati pa chiwundocho
10 A mawaena o na keena he iwakalua kubita ka laula a puni ka hale, ma kela aoao keia aoao.
ndi zipinda za Nyumba ya Mulungu panali bwalo limeneli la mamita khumi kupingasa kwake kuzungulira Nyumba yonse ya Mulungu.
11 Ku pono ae la na puka o na keena aoao i kahi koena, kekahi puka ma ke kukulu akau, a o kekahi puka ma ke kukulu hema; a o ka laula o kahi i koe, elima ia mau kubita a puni.
Zitseko za zipinda zamʼmbalizo zinali zotsekulira ku chiwundo. Chitseko chimodzi chinkayangʼana kumpoto ndipo china chinkayangʼana kummwera. Chiwundo chosamangapo kanthu chinali mamita awiri ndi theka kukula kwake kuzungulira ponseponse.
12 A o ka hale imua o kahi kaawale, ma ke kala komohana, kanahiku kubita ka laula; a o na paia o ka hale elima kubita ka manoanoa a puni, a he kauaiwa kubita kona loa.
Nyumba imene inali chakummwera moyangʼanana ndi bwalo la Nyumba ya Mulungu inali mamita 35 mulifupi mwake. Khoma la nyumbayo linali mamita awiri ndi theka kuchindikira kwake kuzungulira ponseponse, ndipo mulitali mwake linali mamita 45.
13 Pela ia i ana aku la i ka hale, hookahi haneri kubita ka loa; a i kahi kaawale, a me kona hale, a me kona mau paia, hookahi haneri kubita ka loa;
Ndipo munthuyo anayeza Nyumba ya Mulungu ndipo mulitali mwake inali mamita makumi asanu. Nyumbayo ndi makoma ake, zonse zinali za mamita makumi asanu.
14 A i ka laula hoi o ke alo o ka hale, a ma kahi kaawale ma ka hikina hookahi haneri kubita.
Kumaso kwa Nyumba ya Mulungu chakummawa kwa bwalolo mulifupi mwake munali mamita makumi asanu.
15 A ana'e la hoi oia i ka loa o ka hale e ku pono ana i kahi kaawale, ka mea ma kona kua, a me kona mau papaluna ma kela aoao keia aoao, hookahi haneri kubita me ka luakini iloko, a me na lanai o ka pahale;
Kenaka anayeza kutalika kwa nyumba yoyangʼanana ndi bwalo chakumadzulo kwa Nyumba ya Mulungu, kuphatikizapo njira zamʼkati ku mbali iliyonse. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu. Chipinda chachikulu cha Nyumba ya Mulungu, chimene chili chamʼkati, khonde lamʼkati loyangʼanana ndi bwalo,
16 Na laau ku o ka ipuka, a me na pukamakani paa, a me na kia a puni, i ko lakou akolu ana, e ku pono ana i ka paepae, ua uhiia me ka laau a puni, a mai ka honua a hiki i na pukamakani, a ua uhiia na pukamakani;
mazenera ndi maferemu ake, zonsezi zinali zokutidwa ndi matabwa. Pamwamba moyangʼanana ndi chiwundo, Nyumba ya Mulungu inakutidwa ndi matabwa kuyambira pansi mpaka ku mazenera, (mazenerawo anali okutidwa),
17 A hiki i ka mea maluna o ka ipuka, a hiki hoi i ka hale oloko, a mawaho hoi, a ma ka paia okoa a puni maloko a mawaho hoi ma na ana.
pamwamba pa khomo lolowera ku malo opatulika amʼkati komanso kuzungulira makoma onse kunja ndi mʼkati,
18 Ua hanaia hoi ia me na keruba a me na laau pama; a he laau pama mawaena o kekahi keruba a me kekahi keruba; a elua helehelena hoi ko kela keruba ko keia keruba.
anajambulapo zithunzi za kerubi mmodzi atakhala pakati pa kanjedza muwiri. Kerubi aliyense anali ndi nkhope ziwiri:
19 He helehelena kanaka i ku pono i ka laau pama ma kekahi aoao, a he helehelena liona opiopio i ku pono i ka laau pama ma kekahi aoao; ua hanaia ia ma ka hale a puni.
imodzi inali nkhope ya munthu yoyangʼana kanjedza mbali imodzi, ndi ina inali nkhope ya mkango yoyangʼana kanjedza mbali ina. Zinajambulidwa kuzungulira Nyumba ya Mulungu yonse.
20 Mai ka honua ae a hiki iluna o ka ipuka ua hanaia na keruba a me na laau pama, a ma ka paia hoi o ka luakini.
Motero kuyambira pansi mpaka pamwamba pa khomo komanso pa makoma onse a chipinda chachikulu cha Nyumba ya Mulungu, anajambula zithunzi za akerubi ndi kanjedza pa makoma onse a malo opatulika.
21 O na laau ku o ka luakini, ua hana huinaha ia, ma ke alo o kahi hoano; ua like kekahi me kekahi i ka nana aku.
Mphuthu za chipinda chachikulu cha Nyumba ya Mulungu kutalika kwake mbali zonse kunali kofanana. Ndipo kumaso kwa malo opatulika kunali chinthu china chooneka ngati
22 O ke kuabu laau, ekolu kubita kona kiekie, a o kona loa elua kubita; a o kona mau kihi, a o kona loa, a o kona mau paia he laau ia: a olelo mai la oia ia'u, Eia ka papa imua o Iehova.
guwa lansembe la matabwa. Msinkhu wake unali mita imodzi ndi theka, mulitali mwake munali mita imodzi, mulifupi mwake munalinso mita imodzi. Mphuthu zake, tsinde lake ndi mbali zonse zinali za matabwa. Munthuyo anandiwuza kuti, “Tebulo limeneli ndilo limakhala pamaso pa Yehova.”
23 Elua hoi ipuka ko ka luakini a me kahi hoano.
Chipinda chachikulu chija chinali ndi zitseko ziwiri. Malo opatulika aja analinso ndi zitseko ziwiri.
24 Elua hoi pani ko kela ipuka ko keia ipuka, na pani pelu, elua paui no kekahi puka, a elua pani no kekahi puka.
Chitseko chilichonse chinali ndi zigawo ziwiri zopatukana.
25 Ua hanaia hoi ma ia mau mea, ma na paui o ka luakini na keruba a me na laau pama, e like me ka hanaia ma na paia; a he mau papa laau mauoanoa ma ke alo o ka lanai mawaho.
Ndipo pa zitsekopo anajambulipo zithunzi za akerubi ndi kanjedza monga zomwe anajambulapo pa makoma. Kunja kwake kunali ngati denga lamatabwa pamwamba pa khonde lamʼkati.
26 A he mau puka makani paa a me na laau pama ma kekahi aoao, a me kekahi aoao, ma na aoao o ka lanai, a me na keeua aoao o ka hale ma na papa manoanoa.
Pa mbali zonse za khonde lamʼkatilo panali mazenera, ndipo pa makoma ake onse anajambulapo zithunzi za kanjedza.

< Ezekiela 41 >