< Ezekiela 1 >

1 EIA keia, i ke kanakolu o ka makahiki, i ka malama ha, i ka la alima o ka mahina, e noho ana au iwaena o ka poe pio ma ka muliwai o Kebara, hamama mai la ka lani, a ike aku la au i na hihio o ke Akua.
Tsiku lachisanu la mwezi wachinayi, chaka cha makumi atatu, ine ndinali pakati pa amʼndende mʼmbali mwa mtsinje wa Kebara. Tsono kumwamba kunatsekuka ndipo ndinaona maonekedwe a Mulungu mʼmasomphenya.
2 I ka la alima o ka malama, oia ka lima o ka makahiki o ke pio ana o ke alii o Iehoiakima,
Pa tsiku lachisanu la mwezi, chaka chachisanu Yehoyakini ali mʼndende,
3 Hiki maopopo mai la ka olelo a Iehova ia Ezekiela ke keiki a Buzi i ke kahuna ma ka aina o Kaledea, ma ka muliwai Kebara; a malaila i kau mai ai ka lima o Iehova maluna iho ona.
Yehova anayankhula ndi wansembe Ezekieli, mwana wa Buzi, mʼmbali mwa mtsinje wa Kebara mʼdziko la Ababuloni. Dzanja la Yehova linali pa iye kumeneko.
4 Nana aku la an, aia hoi he puahiohio e hele mai ana mai ke kukulu akau mai, he ao nui, a me ke ahi e pakaawili ana ia ia iho, he olinolino a puui ia, a mai waenakonu ona e like i ka nana aku rae ke keleawe olinolino mai loko mai o ke ahi.
Ndinayangʼana ndipo ndinangoona mphepo yamkuntho ikubwera kuchokera kumpoto. Panali mtambo waukulu wozunguliridwa ndi kuwala ndipo moto unali lawilawi kuchokera mu mtambowo. Pakati pa motowo pankaoneka ngati mkuwa wonyezimira.
5 A mai waenakonu mai ona ka like ana o na mea ola eha: eia ko lakou ano, he ano like me ko ke kanaka ko lakou.
Mʼkatikati mwa motowo munali zinthu zinayi zamaonekedwe a nyama. Thupi lawo limaoneka ngati la munthu
6 Papaha ko lakou mau helehelena, a papaha ko lakou mau eheu.
koma chilichonse chinali ndi nkhope zinayi ndiponso mapiko anayi.
7 O ko lakou mau wawae, he mau wawae pololei, a o ka manea o ko lakou mau wawae, ua like ia me ka manea o ka wawae o ke keiki bipi: olinolino mai la lakou e like me ke keleawe i hoohualiia i ka nana aku.
Miyendo yake inali yowongoka; mapazi ake anali a ziboda ngati phazi la mwana wangʼombe. Ndipo zibodazo zinkawala ngati mkuwa wonyezimira.
8 He mau lima kanaka ko lakou malalo iho o ko lakou mau eheu, ma na aoao eha; no lakou hoi ko lakou mau helehelena a me ko lakou mau eheu.
Mʼmunsi mwa mapiko awo kumbali zonse zinayi, nyamazo zinali ndi manja a munthu. Zonse zinayi zinali ndi nkhope ndi mapiko,
9 O ko lakou mau eheu ua hui pu kekahi me kekahi; aole i haliu ae i ko lakou hele ana, hele pololei lakou kela mea keia mea mamua.
ndipo mapiko awowo anakhudzana. Chilichonse chimapita molunjika kutsogolo; sizimatembenuka pamene zimayenda.
10 A o ka like ana o ko lakou mau helehelena, he helehelena no ke kanaka a me ka helehelena o ka liona ko lakou a eha ma ka aoao akau, a me ka helehelena o ka bipikauo ma ka aoao hema; a o ka helehelena o ka aeto ko lakou a eha.
Nkhope zawo zimaoneka motere: Chilichonse chinali ndi nkhope ya munthu, ndipo mbali ya kumanja chilichonse chinali ndi nkhope zinayi zosiyana motere: nkhope ya munthu, nkhope ya mkango ku dzanja lamanja, nkhope ya ngʼombe ku dzanja lamanzere, ndipo kumbuyo kwake nkhope ya chiwombankhanga.
11 Pela ko lakou mau helehelena; a kikoo aku ko lakou mau eheu maluna; ua hui na eheu elua o kela mea keia mea, a ua uhi na eheu elua i ko lakou mau kino.
Ndi mʼmene zinalili nkhope zawo. Mapiko awo anali otambasukira mmwamba. Chamoyo chilichonse chinali ndi mapiko awiri okhudzana ndi mapiko a chinzake. Chinalinso ndi mapiko ena awiri ophimbira thupi lake.
12 Hele pololei ae lakou mamua kela mea keia mea: ma kahi e hele ai ka uhane, malaila lakou i hele ai: aole lakou i haliu ae i ko lakou hele ana.
Zamoyozo zinkayenda molunjika kutsogolo. Kulikonse kumene mzimu umazitsogolera kupita, nazonso zimapita kumeneko, osatembenuka pamene zikupita.
13 A o ka helehelena like ana o na mea ola, ua like ko lakou ano i ka nana aku me na lanahu ahi e a ana, a me na ipukukui; hele ia iwaena o na mea ola; olinolino ke ahi, a mailoko aku o ke ahi i puka ai ka uwila.
Pakati pa zamayozo panali chinthu chooneka ngati makala oyaka kapena miyuni yoyaka. Moto umayendayenda pakati pa zamayozo; wowala kwambiri, ndipo mphenzi zimatuluka pakati pawo.
14 A holo aku la na mea ola a hoi mai la me he anapu ana la o ka uwila i ka nana aku.
Zamoyozo zinkathamanga uku ndi uko ngati kungʼanima kwa mphenzi.
15 A i ko'u nana ana'ku i na mea ola, aia hoi, o ka huila hookahi ma ka honua e pili ana i na mea ola, me kona mau aoao eha.
Pamene ndinali kuyangʼana zamoyozo, ndinangoona mikombero ndipo pansi pambali pa chamoyo chilichonse panali mkombero umodzi.
16 O ke ano o na huila, a me ko lakou hanaia'na ua like me ka topasa i ka nana aku, hookahi ano ko lakou eha: a o ko lakou ano i ka nana aku a me ko lakou hanaia'na, me he huila la iloko o kekahi huila.
Maonekedwe a mikomberoyo anali ngati mwala wonyezimira. Mikombero yonse inali yofanana ndipo mapangidwe awo anali ngati wongolowanalowana.
17 I ko lakou hele ana, hele lakou ma ko lakou mau aoao eha, aole i haliu ae i ko lakou hele ana.
Mikombero ija poyenda inkatha kupita mbali iliyonse yomwe zamoyozo zinayangʼana popanda kutembenuka.
18 A o ko lakou mau apo, ua kiekie lakou he mea weliweli, a ua paapu ko lakou mau apo i na maka, a puni lakou a eha.
Marimu a mikomberoyo anali aatali ndi ochititsa mantha ndipo marimu onse anayi anali ndi maso ponseponse.
19 A hele na mea ola, hele pu ae la na huila ma ka pili o lakou, a kaikaiia'ku na mea ola mai ka honua aku, kaikaiia aku no hoi na huila.
Zamoyozo zinkati zikamayenda, mikomberoyo imayendanso mʼmbali mwake; ndipo zamoyozo zinkati zikamakwera mmwamba, mikomberoyo imakweranso.
20 Aia ma kahi e hele ai ka uhane, malaila lakou i hele ai, malaila e hele ai ka uhane, ua kaikai pu ia na huila me lakou; no ka mea, maloko o na hulla ka uhane o ka mea ola.
Kulikonse kumene mzimu wake unkazitsogolera, zamoyozo zinkapita komweko. Ndipo mikombero ija inkapita nawo pamodzi popeza kuti mzimu wa zamoyozo ndiwo umayendetsa mikombero ija.
21 A hele kela mau mea, hele hoi keia mau mea, a ku kela mau mea, ku no hoi keia mau mea; a i ka wa i kaikaiia'ku kela mau mea mai ka honua aku, alaila kaikai pu ia na huila me lakou, no ka mea, maloko o na huila ka uhane o ka mea ola.
Zamoyo zija zinkati zikamayenda mikombero imayendanso. Zamoyozo zimati zikayima, nayonso mikombero inkayima. Zamoyozo zinkati zikawuluka, mikomberonso imawuluka nazo pamodzi chifukwa mzimu wa zamoyo zija ndiwo umayendetsa mikombero ija.
22 A o ka like ana o ka lani maluna o na poo o na mea ola ua like ia i ka nana aku me ke aniani weliweli, i hoholaia maluna o ko lakou mau poo iluna.
Pamwamba pa mitu ya zamoyozo panali chinthu chonga thambo, lowala ndipo kunyezimira kwake ngati galasi loyangʼanitsa ku dzuwa, loyalidwa pamwamba pa mitu yake.
23 A malalo ae o ka lani, pololei no ko lakou mau eheu ku pono kekahi i kekahi; elua ko kekahi me ko kekahi i uhi ma keia aoao, a elua hoi ko kekahi me ko kekahi i uhi ma kela aoao o ko lakou mau kino.
Zamoyozo zinatambalitsa mapiko ake mʼmunsi mwa thambo lija, mapiko ake ena kumakhudzana, mapiko awiri kumaphimba thupi lake.
24 A i ko lakou helo ana, lohe aku la au i ka halulu ana o ko lakou mau eheu e like me ka halulu ana o na wai he nui no, me he leo la o ka Mea mana loa; ka leo o ka halulu e like me ka leo o ka puali kaua; a ku lakou, kuu iho la lakou i ko lakou mau eheu ilalo.
Pamene zamoyo zimayenda ndimamva phokoso la mapiko ake, ngati mkokomo wa madzi ambiri, ngati liwu la Wamphamvuzonse, ngati phokoso la gulu lankhondo. Zimati zikayima zinkagwetsa mapiko ake.
25 A he leo no mai ka lani mai iluna o ko lakou mau poo, i ka wa i ku ai lakou, a ua kuu iho ko lakou mau eheu.
Ndipo panamveka mawu kuchokera pamwamba pa thambo la pa mitu ya zamoyo zija. Nthawi iyi nʼkuti zamoyozo zitayima ndi kugwetsa pansi mapiko ake.
26 A maluna o ka lani iluna o ko lakou mau poo, he mea like me ka nohoalii, me he pohaku sapire la i ka nana aku; a maluna o ka mea like me ka nohoalii, he mea like me ke kanaka maluna iho ona i ka nana aku.
Pamwamba pa thambo la pa mitu yake panali chinthu chimene chimaoneka ngati mpando waufumu wopangidwa ndi mwala wa safiro, ndipo pamwamba pa mpando waufumuwo panali chinthu chooneka ngati munthu.
27 A ike aku la au i ka mea like me ke keleawe olinolino, i ka nana aku, e like me ke ahi i ka nana aku a puni iloko, mai ka ikea ana o kona puhaka, a maluna aku, a mai ka ikea ana o kona puhaku ilalo, ike aku la au i ka mea like me ke ahi i ka nana aku, a he olinolino kona a puni.
Ndinaona kuti mmwamba mwa chiwuno chake munali ngati chitsulo chowala konsekonse ngati moto. Mʼmunsi mwa chiwuno chake munalinso ngati moto wokhawokha. Kuwala kwa mphamvu kunamuzungulira munthuyo.
28 E like me ke ano o ke anuenue iloko o ke ao i ka la ua, pela ke ano o ka olinolino a puni i ka nana aku. Oia ka mea ikeia o ke ano o ka nani o Iehova. A ike au, moe iho la au ilalo ke alo, a lohe au i ka leo o kekahi e olelo ana:
Kuwalako kunali ndi maonekedwe a utawaleza mʼmitambo tsiku limene kwagwa mvula. Umu ndi mmene ulemerero wa Yehova umaonekera. Pamene ndinawuona ndinagwa pansi ndipo ndinamva mawu akundiyankhula.

< Ezekiela 1 >