< Pukaana 1 >

1 EIA na inoa o na keiki a Iseraela, i hele aku me Iakoba i Aigupita, o kela kanaka keia kanaka i hele aku me ko ka hale ona.
Awa ndi mayina a ana a Israeli amene anapita ku Igupto pamodzi ndi Yakobo abambo awo, aliyense ndi banja lake:
2 O Reubena, o Simeona, o Levi, o Iuda,
Rubeni, Simeoni, Levi, Yuda;
3 O Isakara, o Zebuluna, o Beniamina,
Isakara, Zebuloni, Benjamini;
4 O Dana, o Napetali, o Gada a o Asera.
Dani, Nafutali; Gadi ndi Aseri.
5 O na mea ola a pau i puka mai ai, mai loko ae o ko Iakoba puhaka, he kanahiku lakou; a ma Aigupita no o Iosepa.
Anthu onse obadwa mwa Yakobo analipo 70. Yosefe nʼkuti ali kale ku Igupto.
6 A make iho la o Iosepa, a me kona poe hoahanau a pau, a me ia hanauna a pau.
Tsono Yosefe ndi abale ake onse ndiponso mʼbado wawo wonse anamwalira.
7 Hanau nui iho la na mamo a Iseraela, a laha loa ae la, a kawowo loa: ua nui loa ko lakou ikaika, a ua piha hoi ka aina ia lakou.
Koma Aisraeli anaberekana ndi kuchuluka kwambiri nakhala amphamvu kwambiri, kotero kuti anadzaza dzikolo.
8 A ku mai la kekahi alii hou ma Aigupita, aole i ike ia Iosepa.
Pambuyo pake mfumu yatsopano imene sinkamudziwa Yosefe, inayamba kulamulira dziko la Igupto.
9 I mai la ia i kona poe kanaka, Aia hoi, ua oi aku ka nui o na kanaka mamo a Iseraela, a me ko lakou ikaika i ko kakou.
Iyo inati kwa anthu ake, “Taonani, Aisraeli achuluka ndipo ndi amphamvu kwambiri kuposa ife.
10 E hana maalea kakou ia lakou; o nui auanei lakou, a hiki mai ke kaua, huipu lakou me ko kakou poe enemi, a e kaua mai hoi ia kakou, a pela ia lakou e pii aku ai mai ka aina aku.
Tiyeni tiwachenjerere. Tikapanda kutero adzachuluka kuposa ife, ndipo ngati kutakhala nkhondo, adzadziphatika kwa adani athu nadzamenyana nafe, kenaka nʼkudzachoka mʼdziko muno.”
11 A hoonoho aku lakou i na luna hooluhi maluna o lakou, i mea e hookaumaha loa ai ia lakou i na haua nui. A hana iho la lakou i na kulanakauhale papaa no Parao, o Pitoma, a o Ramese.
Kotero anayika akapitawo kuti aziwazunza ndi kuwagwiritsa ntchito yolemetsa mokakamiza. Iwo anamangira Farao mizinda ya Pitomu ndi Ramesesi kumene ankasungirako chakudya.
12 E like me ko lakou hooluhi ana mai, pela no hoi ko lakou nei mahuahua, a me ka palahalaha ana aku. A makau loa lakou i na mamo a Iseraela.
Koma pamene ankawazunza kwambiri, Aisraeli ndiye ankachulukirachulukira mpaka kubalalikira mʼdziko lonse. Kotero Aigupto anayamba kuopa Aisraeliwo
13 Hoohana iho la ko Aigupita i na mamo a Iseraela me ka hookoikoi.
ndipo anawagwiritsa ntchito mwankhanza kwambiri.
14 Hooawahia iho la lakou i ko lakou nei ola ana i ka hana luhi iloko o ka palolo, a i na pohakulepo, a me na hana a pau ma ka mahinaai: a o ka hana a pau a lakou i hoohana iho ai ia lakou nei, he mea koikoi ia.
Aigupto anachititsa moyo wa Aisraeli kukhala owawa kwambiri powagwiritsa ntchito yakalavulagaga yowumba njerwa ndi kuponda dothi lomangira, pamodzi ndi ntchito zina zosiyanasiyana zamʼminda. Iwo anakakamiza Aisraeli mwankhanza kuti agwire ntchito yowawayi.
15 Olelo mai la ke alii o Aigupita i na palekeiki Hebera, o Sipera ka inoa o kekahi, a o Pua hoi ka inoa o kekahi;
Mfumu ya Igupto inati kwa azamba a Chihebri omwe mayina awo anali Sifira ndi Puwa,
16 I mai la, A i palekeiki olua i na wahine Hebera, a nana olua iloko o na paholoi; ina he keikikane ia, alaila e pepehi olua ia ia; aka ina he kaikamahine, e ola no ia.
“Mukamathandiza amayi a Chihebri pa mwala wochirira, muzionetsetsa kuti akabadwa mwana wamwamuna muzipha, koma akakhala wamkazi muzimuleka akhale ndi moyo.”
17 Aka, makau iho la na palekeiki i ke Akua; aole laua i hana i ka mea a ke alii o Aigupita i kauoha ai in laua; aka, hoola ae la laua i na keikikane.
Koma azambawo ankaopa Mulungu ndipo sanachite zimene mfumu ya Igupto inawawuza kuti achite. Iwo analeka ana aamuna kuti akhale ndi moyo.
18 Kii mai la ke alii o Aigupita i na palekeiki, i mai la ia laua, No ke aha la olua i hana'i i keia mea, a hoola i na keikikane?
Kenaka mfumu ya Igupto inayitanitsa azamba aja ndi kuwafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mwachita zimenezi? Bwanji mwasiya ana aamuna kuti akhale ndi moyo?”
19 I aku la na palekeiki ia Parao, No ka mea, aole i like na wahine Hebera me ko Aigupita poe wahine, he hiki wawe ko lakou, aole e hiki aku na palekeiki, a hanau e no lakou.
Azambawo anamuyankha Farao kuti, “Amayi a Chihebri sali ngati amayi a Chiigupto; Iwo ndi amphamvu ndipo amachira azamba asanafike.”
20 A hoomaikai mai la ke Akua i na palekeiki: a mahuahua aku la na kanaka, a ua nui loa no hoi ko lakou ikaika.
Kotero Mulungu anawakomera mtima azambawo, ndipo Aisraeli anapitirirabe kuchulukana nakhala amphamvu kwambiri.
21 A no ka makau ana o na palekeiki i ke Akua, a no kona hoomahuahua ana i ko lakou mau ohana,
Pakuti azambawo ankaopa Mulungu, Iye anawapatsa mabanja awoawo.
22 Kauoha ae la o Parao i kona poe kanaka a pau, i aku la, O na keikikane a pau ke hanau mai, e kiola aku ia lakou i ka muliwai, aka, o na kaikamahine a pau, ka oukou ia e hoola ai.
Pamenepo Farao analamulira anthu ake onse kuti, “Mwana wamwamuna aliyense akabadwa, mukamuponye mu mtsinje wa Nailo, koma wamkazi mulekeni akhale ndi moyo.”

< Pukaana 1 >