< Zabura 121 >

1 Waƙar haurawa. Na tā da idanuna zuwa wajen tuddai, ta ina ne taimakona zai zo?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Taimakona zai zo daga wurin Ubangiji, wanda ya kafa sama da ƙasa.
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 Ba zai bari ƙafarka tă yi santsi ba, shi da yake tsaronka ba zai yi gyangyaɗi ba;
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 tabbatacce, shi da yake tsaron Isra’ila ba ya gyangyaɗi ko barci.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 Ubangiji yana tsaronka, Ubangiji ne inuwa a hannun damanka;
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 rana ba za tă buge ka cikin yini ba balle wata da dare.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 Ubangiji zai kiyaye ka daga dukan masifa, zai tsare ranka;
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 Ubangiji zai kiyaye shigarka da fitarka yanzu da har abada kuma.
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Zabura 121 >