< Sòm 114 >
1 Lè Israël te sòti an Égypte, lakay Jacob soti de yon pèp lang etranje,
Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
2 Juda te vin sanktiyè Li a, Israël, wayòm Li.
Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
3 Lanmè a te gade e te sove ale. Jourdain an te vire fè bak.
Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
4 Mòn yo te sote tankou belye, kolin yo tankou ti mouton.
mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
5 Sa k pase ou menm, O lanmè, ke ou te sove ale konsa? O Jourdain an, ke Ou te vire fè bak konsa?
Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
6 O mòn yo, ke ou sote tankou belye konsa? O kolin yo, tankou ti mouton konsa?
inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
7 Pran tranble, O latè, devan SENYÈ a, Devan Bondye a Jacob la,
Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
8 Ki te fè wòch la devni yon ma dlo, wòch silèks la yon sous k ap koule.
amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.