< Neemi 7 >
1 Alò, lè miray la te fin rebati, mwen te fin monte pòt yo e gadyen pòtay yo avèk chantè yo avèk Levit yo te chwazi.
Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
2 Anplis, mwen te mete Hanani, frè mwen an, avèk Hanania, kòmandan fò a, an chaj Jérusalem. Paske li te yon nonm fidèl e te gen lakrent Bondye plis pase anpil moun.
Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
3 Mwen te di yo: “Pa kite pòtay Jérusalem yo ouvri jiskaske solèy la vin cho ak pandan gad yo an plas yo, fè yo fèmen pòt yo e boulonnen yo. Anplis, chwazi gad yo soti nan pèp Jérusalem nan, chak moun sou pòs li e chak moun devan pwòp kay pa li.”
Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
4 Alò, vil la te byen gran avèk anpil espas, men moun ladann yo pa t anpil e kay yo potko bati.
Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
5 Konsa, Bondye mwen an te mete sa nan kè m pou rasanble sitwayen enpòtan lavil yo, chèf yo avèk pèp la pou vin anrejistre pa lign zansèt yo. Mwen te twouve liv a zansèt a sila ki te monte an premye yo, e ladann, rekò swivan an:
Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
6 Sila yo se pèp pwovens ki te monte soti an kaptivite nan egzil ke Nebucadnetsar, wa Babylone nan, te pote ale yo, e ki te retounen Jérusalem avèk Juda, chak moun nan lavil pa li;
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
7 moun ki te vini avèk Zorobabel yo, Josué, Néhémie, Azaria, Raamia, Nachamani, Mardochée, Bilschan, Mispéreth, Bigvaï, Nehum, Baana. Kantite mesye nan pèp Israël yo:
Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
8 Fis a Pareosch yo, de-mil-san-swasann-douz.
Zidzukulu za Parosi 2,172
9 Fis a Schephathia yo, twa-san-senkant-de.
Zidzukulu za Sefatiya 372
10 Fis a Arach yo, sis-san-senkant-de.
Zidzukulu za Ara 652
11 Fis a Pachath-Moab yo, fis a Josué yo avèk Joab, de-mil-ui-san-dizwit.
Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
12 Fis a Élam yo, mil-de-san-senkant-kat.
Zidzukulu za Elamu 1,254
13 Fis a Zatthu yo, ui-san-karann-senk.
Zidzukulu za Zatu 845
14 Fis a Zaccaï yo, sèt-san-swasant.
Zidzukulu za Zakai 760
15 Fis a Binnuï yo, sis-san-karann-tuit.
Zidzukulu za Binuyi 648
16 Fis a Bébaï yo, sis-san-venn-tuit
Zidzukulu za Bebai 628
17 Fis a Azgad yo, de-mil-twa-san-venn-de.
Zidzukulu za Azigadi 2,322
18 Fis a Adonikam yo, sis-san-swasann-sèt.
Zidzukulu za Adonikamu 667
19 Fis a Bigvaï yo, de-mil-swasann-sèt.
Zidzukulu za Abigivai 2,067
20 Fis a Adin yo, Sis-san-senkann-senk.
Zidzukulu za Adini 655
21 Fis a Ather yo, nan fanmi Ézéchias, katra-ven-di-zuit.
Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
22 Fis a Haschum yo, twa-san-venn-tuit.
Zidzukulu za Hasumu 328
23 Fis a Betsaï yo, twa-san-venn-tuit.
Zidzukulu za Bezayi 324
24 Fis a Hariph yo, san-douz.
Zidzukulu za Harifu 112
25 Fis a Gabaon yo, katre-ven-kenz.
Zidzukulu za Gibiyoni 95.
26 Mesye a Bethléem yo avèk Netopha, san-katre-ven-uit.
Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
27 Mesye a Anathoth yo, san-venn-tuit.
Anthu a ku Anatoti 128
28 Mesye a Beth-Azmaveth yo, karann-de.
Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
29 Mesye a Kirjath-Jearim yo, a Kephira, avèk Beéroth, sèt-san-karann-twa.
Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
30 Mesye a Rama yo avèk Guéba, sis-san-ven-te-yen.
Anthu a ku Rama ndi Geba 621
31 Mesye nan Micmas yo, san-venn-de.
Anthu a ku Mikimasi 122
32 Mesye nan Béthel avèk Aï yo, san-venn-twa.
Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
33 Mesye nan lòt Nebo yo, san-karann-de.
Anthu a ku Nebo winayo 52
34 Fis a lòt Élam yo, mil-de-san-senkann-kat.
Ana a Elamu wina 1,254
35 Fis a Harim yo, twa-san-ven.
Zidzukulu za Harimu 320
36 Fis a Jéricho yo, twa-san-karann-senk.
Zidzukulu za Yeriko 345
37 Fis a Lod, Hadid avèk Ono yo, sèt-san-ven-te-yen.
Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
38 Fis a Senaa yo, twa-mil-nèf-san-trant.
Zidzukulu za Senaya 3,930.
39 Prèt yo: fis a Jedaeja lakay Josué yo, nèf-san-swasann-trèz.
Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
40 Fis a Immer yo, mil-senkann-de.
Zidzukulu za Imeri 1,052
41 Fis a Paschhur yo, mil-de-san-karann-sèt.
Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
42 Fis a Harim yo, mil-di-sèt.
Zidzukulu za Harimu 1,017.
43 Levit yo: fis a Josué ak Kadmiel yo, avèk fis a Hodeva yo, swasann-katòz.
Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
44 Chantè yo: fis a Asaph yo, san-karann-tuit.
Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
45 Gadyen pòtay yo: fis a Schallum yo, fis a Ather yo, fis a Thaimon yo, fis a Akkub yo, fis a Hathitha yo, fis a Schobaï yo, san-trann-tuit.
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
46 Sèvitè tanp yo: fis a Tsicha yo, fis a Hasupha yo, fis a Thabbaoth yo.
Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
47 Fis a Kéros yo, fis a Sia yo, fis a Padon yo.
Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
48 Fis a Lebana yo, fis a Hagaba yo, fis a Salmaï yo.
Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
49 Fis a Hanan yo, fis a Guiddel yo, fis a Gachar yo.
Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
50 Fis a Reaja yo, fis a Retsin yo, fis a Nekoda yo.
Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
51 Fis a Gazzam yo, fis a Uzza yo, fis a Paséach yo.
Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
52 Fis a Bésaï yo, fis a Mehunim yo, fis a Nephischsim yo.
Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
53 Fis a Bakbuk yo, fis a Hakupha yo, fis a Harhur yo.
Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
54 Fis a Batslith yo, fis a Mehida yo, fis a Harscha yo,
Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
55 fis a Barkos yo, fis a Sisera yo, fis a Thamach yo,
Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
56 fis a Netsiach yo, fis a Hathipha yo.
Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
57 Fis a sèvitè Salomon yo: fis a Sothaï yo, fis a Sophéreth yo, fis a Perida yo.
Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
58 Fis a Jaaia yo, fis a Darkon yo, fis a Guiddel yo.
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
59 Fis a Schephathia yo, fis a Hatthil yo, fis a Pokéreth-Hatsebaïm yo, fis a Amon yo.
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
60 Tout sèvitè tanp yo avèk fis a sèvitè Salomon yo, twa-san-katre-ven-douz.
Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
61 Sila yo se te yo menm ki te monte soti Tel-Melah yo, Tel-Harsha, Cherub, Addon e Immer yo, men yo pa t kab bay prèv lakay papa zansèt pa yo, pou demontre ke se Izrayelit yo te ye:
Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
62 fis a Delaiah yo, fis a Tobiah yo, fis a Nekoda yo, sis-san-karann-de.
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
63 Nan prèt yo: fis a Hobaja yo, fis a Hakkots yo, fis a Barzillaï yo, ki te pran kon madanm youn nan fis a Barzillaï yo, Galaadit la e te rele selon non pa yo.
Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
64 Sila yo te fè rechèch nan achiv zansèt yo, men yo pa t kapab twouve yo; akoz sa, yo te konsidere pa pwòp e pa t kab fè sèvis kon prèt.
Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
65 Gouvènè a te pale yo ke yo pa t pou manje soti nan bagay sen pase tout lòt bagay yo, jiskaske yon prèt vin leve avèk Ourim avèk Thoumim nan.
Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
66 Asanble a an antye te karann-de-mil-twa-san-swasant moun,
Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
67 anplis, sèvitè avèk sèvant pa yo, sou sila yo te gen sèt-mil-twa-san-trann-sèt moun; epi yo te gen de-san-karann-senk gason avèk fanm nan chantè yo.
Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
68 Cheval pa yo te sèt-san-trann-sis; milèt yo, de-san-karann-senk;
Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
69 chamo yo, kat-san-trann-senk, bourik yo, si-mil-sèt-san-ven.
Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
70 Kèk moun pami tèt lakay zansèt yo te fè don pou travay la. Gouvènè a te bay nan trezò a travay la mil ons an lò, senkant basen ak senk-san-trant nan vètman prèt yo.
Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
71 Kèk moun pami tèt lakay zansèt yo te bay nan trezò travay la ven-mil ons an lò ak de-mil-de-san min an ajan.
Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
72 Sa ki te bay pa tout lòt moun nan pèp la te ven-mil ons an lò, ak de-mil min an ajan, avèk swasann-sèt nan vètman prèt.
Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
73 Alò, prèt yo, Levit yo, gadyen pòtay yo, chantè yo, kèk moun nan pèp la, sèvitè tanp yo ak tout Israël te rete nan vil pa yo. Lè setyèm mwa a te vin rive, fis Israël yo te vin antre nan pwòp vil pa yo.
Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.