< Jòb 27 >
1 Alò, Job te kontinye diskou li. Li te di:
Ndipo Yobu anapitiriza kuyankhula kwake:
2 Kon Bondye viv la, ki te retire dwa m, Toupwisanki te fè m gen nanm anmè a,
“Ndithu pali Mulungu wamoyo, amene wakana kundiweruza molungama, Wamphamvuzonse, amene wawawitsa mtima wanga,
3 paske tan lavi toujou nan mwen. Souf Bondye la nan nen m.
nthawi zonse pamene ndili ndi moyo, mpweya wa Mulungu uli mʼmphuno mwanga,
4 Lèv mwen, anverite, p ap pale sa ki pa dwat, ni lang mwen pa p pale manti.
pakamwa panga sipadzatuluka mawu oyipa, lilime langa silidzayankhula zachinyengo.
5 Fòk se lwen m pou m ta bay ou rezon. Jiskaske m mouri, mwen p ap lage entegrite m.
Sindidzavomereza kuti inu mukunena zoona; mpaka imfa yanga, sindidzataya ungwiro wanga.
6 Mwen kenbe fèm a ladwati mwen. Mwen p ap lage l menm. Kè m pa repwoche m depi gen lavi ladan m.
Ndidzasunga chilungamo changa ndipo sindidzalola kuti chindichokere; chikumbumtima changa sichidzanditsutsa nthawi yonse ya moyo wanga.
7 “Kite lènmi m kapab tankou mechan a. Kite sila ki leve kont mwen, san jistis.
“Mdani wanga akhale ngati woyipa, wondiwukira akhale ngati munthu wosalungama!
8 Paske ki espwa sila ki san Bondye a genyen lè l koupe retire nèt, lè Bondye fè l oblije bay lavi li?
Nanga chiyembekezo cha munthu wosapembedza nʼchiyani pamene aphedwa, pamene Mulungu achotsa moyo wake?
9 Èske Bondye va tande kri li lè malè rive li?
Kodi Mulungu amamva kulira kwake pamene zovuta zamugwera?
10 Èske li va pran plezi nan Toupwisan an? Èske li va rele non Bondye a nan tout tan sa yo?
Kodi adzapeza chikondwerero mwa Wamphamvuzonse? Kodi adzapemphera kwa Mulungu nthawi zonse?
11 Mwen va enstwi ou nan pwisans Bondye. Pwojè Toupwisan an, mwen p ap kache l.
“Ndidzakuphunzitsani za mphamvu ya Mulungu ndipo sindidzabisa njira za Wamphamvuzonse.
12 Gade byen, nou tout gen tan wè sa. Ebyen, poukisa nou aji nan foli?
Inu mwadzionera nokha zonsezi. Nanga bwanji mukuyankhula zopanda pake?
13 “Sa se pòsyon a moun mechan an ki va sòti Bondye, ak eritaj ke mechan yo va resevwa nan men Toupwisan an.
“Pano pali chilango chimene Mulungu amasungira woyipa, cholowa chimene munthu wankhanza amalandira kuchokera kwa Wamphamvuzonse.
14 Malgre fis li yo anpil, yo destine pou nepe. Konsa, desandan li yo ap toujou manke pen.
Angakhale ana ake achuluke chotani adzaphedwa ndi lupanga ndipo zidzukulu zake zidzasowa zakudya.
15 Sila ki swiv li yo va antere nan lamò e vèv li yo p ap kriye pou li.
Amene adzatsalireko adzafa ndi mliri, ndipo akazi awo amasiye sadzawalira.
16 Malgre li fè gwo pil ajan an vin tankou se tè e prepare vètman anpil tankou ajil,
Ngakhale aunjike siliva ngati fumbi, ndi kukundika zovala ngati mchenga,
17 li kab prepare l, men se moun ladwati yo k ap mete li, se inosan yo k ap divize ajan an.
zimene wasungazo wolungama ndiye adzavale, ndipo anthu osalakwa ndiwo adzagawane siliva wakeyo.
18 Li te bati kay li tankou papiyon, oswa tankou kay poto gadyen te fè.
Nyumba imene akuyimanga ili ngati mokhala kadziwotche, ili ngati msasa umene mlonda amamanga.
19 Li kouche byen rich, men li pa janm vin genyen ankò; li ouvri zye li, men li pa la.
Amapita kokagona ali wolemera koma kutha kwake nʼkomweko; akatsekula maso ake, chuma chake chonse chapita.
20 Gwo laperèz yo rive pran l tankou yon flèv. Yon move tan vole retire l pandan lannwit.
Zoopsa zimamukokolola ngati madzi achigumula; mphepo yamkuntho imamunyamula usiku.
21 Van lès la pote l ale e li pati. Li fè l vire tounen kite plas li.
Mphepo ya kummawa imamuwulutsa ndipo iye saonekanso ndipo imamuchotsa pamalo pake.
22 Paske l ap plonje sou li san epanye, pandan li eseye envite l chape nan men l.
Imakuntha pa iye osamuchitira chisoni, pamene akuyesa kuthawa mphamvu zake mwaliwiro.
23 Pèp la va bat men yo sou li. Yo va sifle sou li kon koulèv, pou li kite plas li a.”
Mphepoyo imamuwomba ndithu ndipo kuchokera pamalo pake imamuopseza.”