< Psalm 121 >

1 Ein Wallfahrtslied. Ich hebe meine Augen auf zu den Bergen: Woher kommt mir Hilfe?
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndikweza maso anga ku mapiri; kodi thandizo langa limachokera kuti?
2 Meine Hilfe kommt von dem HERRN, der Himmel und Erde gemacht hat!
Thandizo langa limachokera kwa Yehova, wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
3 Er wird deinen Fuß nicht wanken lassen, und der dich behütet, schläft nicht.
Sadzalola kuti phazi lako literereke; Iye amene amakusunga sadzawodzera.
4 Siehe, der Hüter Israels schläft noch schlummert nicht.
Taonani, Iye amene amasunga Israeli sadzawodzera kapena kugona.
5 Der HERR behütet dich; der HERR ist dein Schatten über deiner rechten Hand,
Yehova ndiye amene amakusunga; Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.
6 daß dich am Tage die Sonne nicht steche, noch der Mond des Nachts.
Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana, kapena mwezi nthawi ya usiku.
7 Der HERR behüte dich vor allem Übel, er behüte deine Seele;
Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako.
8 der HERR behüte deinen Ausgang und Eingang von nun an bis in Ewigkeit!
Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalm 121 >