< 1 Chronik 25 >

1 Und David samt den Heerführern sonderte von den Söhnen Asaphs, Hemans und Jedutuns solche zum Dienste aus, welche weissagten zum Harfen, Psalter und Zimbelspiel. Die Zahl der Männer, die diesen Dienst verrichteten, war:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 von den Söhnen Asaphs: Sakkur, Joseph, Netanja, Asarela, unter der Leitung Asaphs, welcher nach Anweisung des Königs weissagte.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Von Jedutun: die Söhne Jedutuns waren: Gedalja, Zeri, Jesaja, Chaschabja, Mattitja und Simei, ihrer sechs, unter der Leitung ihres Vaters Jedutun, welcher mit der Harfe weissagend dankte und den HERRN lobte.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Von Heman: die Söhne Hemans waren: Buckija, Mattanja, Ussiel, Schebuel, Jerimot, Chananja, Chanani, Eliata, Giddalti, Romamti-Eser, Joschbekascha, Malloti, Hotir und Machasiot.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Alle diese waren Söhne Hemans, des Sehers des Königs; nach den Worten Gottes von der Erhöhung des Horns, gab Gott dem Heman vierzehn Söhne und drei Töchter.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Alle diese waren unter der Leitung ihrer Väter Asaph, Jedutun und Heman beim Gesang im Hause des HERRN, mit Zimbeln, Psaltern und Harfen zum Dienst im Hause Gottes nach der Anweisung des Königs tätig.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Und ihre Zahl samt ihren Brüdern, aller, die im Gesang unterrichtet waren und verstanden, dem HERRN zu singen, betrug zweihundertachtundachtzig.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 Sie warfen aber das Los über ihr Amt, der Kleinste wie der Größte, der Lehrer wie der Schüler.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 Und das erste Los für Asaph fiel auf Joseph. Das zweite fiel auf Gedalja samt seinen Brüdern und Söhnen, ihrer zwölf;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 das dritte auf Sakkur samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 das vierte auf Jizri samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf;
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 das fünfte auf Netanja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 Das sechste auf Buckija samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 Das siebente auf Jescharela samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 Das achte auf Jesaja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 Das neunte auf Mattanja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 Das zehnte auf Simei samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 Das elfte auf Asareel samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 Das zwölfte auf Chaschabja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 Das dreizehnte auf Schubael samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 Das vierzehnte auf Mattitja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 Das fünfzehnte auf Jeremot samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 Das sechzehnte auf Chananja samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 Das siebzehnte auf Joschbekascha samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 Das achtzehnte auf Chanani samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 Das neunzehnte auf Malloti samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 Das zwanzigste auf Eliata samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 Das einundzwanzigste auf Hotir samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 Das zweiundzwanzigste auf Gidalti samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 Das dreiundzwanzigste auf Machasiot samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 Das vierundzwanzigste auf Romamti-Eser samt seinen Söhnen und Brüdern, ihrer zwölf.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< 1 Chronik 25 >