< Psalm 122 >

1 Ein Lied Davids im höhern Chor. Ich freue mich des, das mir geredet ist, daß wir werden ins Haus des HERRN gehen,
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
2 und daß unsere Füße werden stehen in deinen Toren, Jerusalem.
Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
3 ist gebauet, daß es eine Stadt sei, da man zusammenkommen soll,
Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
4 da die Stämme hinaufgehen sollen, nämlich die Stämme des HERRN, zu predigen dem Volk Israel, zu danken dem Namen des HERRN.
Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
5 Denn daselbst sitzen die Stühle zum Gericht, die Stühle des Hauses David.
Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
6 Wünschet Jerusalem Glück! Es müsse wohlgehen denen, die dich lieben!
Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
7 Es müsse Friede sein inwendig in deinen Mauern und Glück in deinen Palästen!
Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
8 Um meiner Brüder und Freunde willen will ich dir Frieden wünschen.
Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
9 Um des Hauses willen des HERRN, unsers Gottes, will ich dein Bestes suchen.
Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.

< Psalm 122 >