< Psaumes 53 >

1 Pour la fin, pour Maheleth. Intelligence à David. Ils se sont corrompus, et sont devenus abominables dans leurs iniquités; il n’en est pas qui fasse le bien.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide. Chitsiru chimati mu mtima mwake, “Kulibe Mulungu.” Iwo ndi oyipa ndipo njira zawo ndi zonyansa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino.
2 Dieu, du haut du ciel, a jeté un regard sur les fils des hommes, afin de voir s’il en est un intelligent ou cherchant Dieu.
Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano pa ana a anthu kuti aone ngati alipo wina wanzeru, wofunafuna Mulungu.
3 Tous se sont détournés, tous ensemble sont devenus inutiles; il n’en est pas qui fassent le bien; il n’en est pas même un seul.
Aliyense wabwerera, iwo onse pamodzi akhala oyipa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino, ngakhale mmodzi.
4 Est-ce qu’ils ne connaîtront point, tous ceux qui opèrent l’iniquité, qui dévorent mon peuple comme un morceau de pain?
Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi; anthu amene amadya anthu anga monga mmene anthu amadyera buledi, ndipo sapemphera kwa Mulungu?
5 Ils n’ont pas invoqué le Seigneur, ils ont tremblé de frayeur là où n’était pas la crainte. Parce que Dieu a dispersé les os de ceux qui plaisent aux hommes; ils ont été confondus, parce que le Seigneur les a méprisés.
Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu pamene panalibe kanthu kochititsa mantha. Mulungu anamwazamwaza mafupa a anthu amene anakuthirani nkhondo; inuyo munawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawanyoza.
6 Qui fera sortir de Sion le salut d’Israël? Lorsque Dieu aura ramené la captivité de son peuple, Jacob exultera: Israël sera dans l’allégresse.
Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni! Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake, lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale!

< Psaumes 53 >