< Job 17 >

1 Mes esprits se dissipent, mes jours vont être éteints, le sépulcre [m'attend].
“Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
2 Certes il n'y a que des moqueurs auprès de moi, et mon œil veille toute la nuit dans les chagrins qu'ils me font.
Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
3 Donne-moi, je te prie, [donne-moi] une caution auprès de toi; [mais] qui est-ce qui me touchera dans la main?
“Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
4 Car tu as caché à leur cœur l'intelligence, c'est pourquoi tu ne les élèveras point.
Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
5 Et les yeux même des enfants de celui qui parle avec flatterie à ses intimes amis, seront consumés.
Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
6 Il m'a mis pour être la fable des peuples, et je suis [comme] un tambour devant eux.
“Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
7 Mon œil est terni de dépit, et tous les membres de mon corps sont comme une ombre.
Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
8 Les hommes droits seront étonnés de ceci, et l'innocence se réveillera contre l'hypocrite.
Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
9 Toutefois le juste se tiendra ferme dans sa voie, et celui qui a les mains nettes, se renforcera.
Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
10 Retournez donc vous tous, et revenez, je vous prie; car je ne trouve point de sage entre vous.
“Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
11 Mes jours sont passés, mes desseins sont rompus, [et] les pensées de mon cœur [sont dissipées].
Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
12 On me change la nuit en jour, et on fait que la lumière se trouve proche des ténèbres.
Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
13 Certes je n'ai plus à attendre que le sépulcre, qui va être ma maison; j'ai dressé mon lit dans les ténèbres. (Sheol h7585)
Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
14 J'ai crié à la fosse: tu es mon père; et aux vers: vous êtes ma mère et ma sœur.
ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
15 Et où seront les choses que j'ai attendues, et qui est-ce qui verra ces choses qui ont été le sujet de mon attente?
tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
16 Elles descendront au fond du sépulcre; certes elles reposeront ensemble [avec moi] dans la poussière. (Sheol h7585)
Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)

< Job 17 >