< Job 25 >

1 Or Baldad le Sauchite dit:
Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 Pourquoi Celui qui a créé toute chose commence-t-il par inspirer crainte de lui?
“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
3 Qui pourra prendre en défaut l'activité des pirates? Contre qui le tentateur ne dresse-t-il pas des embûches?
Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
4 Comment un mortel est-il juste aux yeux du Seigneur? Quel fils de la femme est pur devant lui?
Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
5 S'il commande à la lune, elle cessera de luire; et pour lui les étoiles sont-elles pures?
Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
6 Résigne-toi donc, l'homme n'est que pourriture; le fils de l'homme n'est qu'un vermisseau.
nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”

< Job 25 >