< Jérémie 40 >

1 Et la parole du Seigneur vint de nouveau à Jérémie, lorsqu'il était encore enchaîné dans le préau de la prison;
Yehova anayankhula ndi Yeremiya pamene Nebuzaradani mtsogoleri wa asilikali olonda mfumu anamasula Yeremiyayo ku Rama. Anamupeza Yeremiya ali womangidwa ndi unyolo pamodzi ndi amʼndende ena onse a ku Yerusalemu ndi a ku Yuda amene ankapita nawo ku ukapolo ku Babuloni.
2 Voici ce que lui dit le Seigneur, créateur de la terre, qui l'a formée pour la redresser; son nom est le Seigneur:
Mtsogoleriyu anamupeza Yeremiya, anamuwuza kuti, “Yehova Mulungu wako analengeza kale zakuti malo ano adzawonongedwa.
3 Crie vers moi et je te répondrai, et je te ferai connaître de grandes choses et très certaines que tu ne sais pas.
Ndipo tsopano Yehova wachitadi zimenezi monga mmene ananenera. Izi zonse zachitika chifukwa anthu inu munachimwira Yehova ndipo simunamumvere.
4 Car voici ce que dit le Seigneur, concernant les maisons de cette ville et les palais du roi de Juda, qui ont été détruits pour en faire des palissades et des ouvrages avancés,
Koma tsopano taona, lero ndikukumasula unyolo umene unali mʼmanja mwako. Ngati ukufuna kupita nane ku Babuloni, tiye ndipo adzakusamala bwino. Koma ngati sukufuna kupita, ndiye usapite. Dziko ndi limeneli monga ukulioneramo. Uli ndi ufulu kupita kulikonse kumene ukufuna.”
5 Qu'on opposait aux Chaldéens, et qui furent remplis de cadavres d'hommes frappés par moi dans mon indignation et ma colère, quand je détournai d'eux ma face en punition de leurs méchancetés.
Yeremiya asanayankhe, Nebuzaradani anamuwuzanso kuti, “Ngati supita ndiye pita, ubwerere kwa Gedaliya, mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani, amene mfumu ya ku Babuloni inamusankha kuti akhale bwanamkubwa wa Yuda. Ukakhale naye pakati pa anthu, kapena upite kulikonse ukufuna.” Ndipo mtsogoleri uja anamupatsa Yeremiya chakudya ndi mphatso zina ndi kumulola kuti apite.
6 Voilà que je lui apporte le remède et la guérison; je me montrerai à elle et je la guérirai; je lui donnerai la sécurité et la paix.
Motero Yeremiya anapita kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa ndipo anakakhala naye kumeneko pakati pa anthu amene anatsala mʼdzikomo.
7 Et je ramènerai les captifs de Juda et les captifs d'Israël, et je les réédifierai comme ils étaient autrefois.
Panali atsogoleri ena a nkhondo ndi anthu awo amene sanadzipereke nawo. Iwowa anamva kuti mfumu ya ku Babuloni inasankha Gedaliya mwana wa Ahikamu kukhala bwanamkubwa wa dzikolo ndipo kuti yamuyika kukhala wolamulira amuna, akazi ndi ana amene anali osauka kwambiri mʼdzikomo, amene sanawagwire ukapolo kupita nawo ku Babuloni.
8 Et je les purifierai de toutes les iniquités qu'ils ont commises envers moi, et je ne me souviendrai plus des péchés où ils sont tombés en se révoltant contre moi.
Iwowa anapita ku Mizipa kwa Gedaliya. Amene anapitawo ndi awa: Ismaeli mwana wa Netaniya, Yohanani ndi Yonatani ana a Kareya, Seraya mwana wa Tanihumeti, ana a Efai a ku Netofa, ndi Yezaniya mwana wa Maaka, iwowo pamodzi ndi anthu awo.
9 Et ce sera un sujet de joie, de louange et de grandeur pour tout peuple de la terre qui apprendra le bien que je leur ferai; et les gentils seront effrayés et jaloux des biens et de toute la paix que je lui donnerai.
Gedaliya mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani, anawalonjeza iwo pamodzi ndi anthuwo mwalumbiro. Ndipo anati, “Musaope kuwatumikira Ababuloni. Khalani mʼdziko muno, tumikirani mfumu ya ku Babuloni, ndipo zinthu zidzakuyenderani bwino.
10 Voici ce que dit le Seigneur: On entendra encore en ce lieu dont vous dites: C'est un désert abandonné des bêtes et des hommes; les villes de Juda, les alentours de Jérusalem sont dépeuplés; car il n'y a plus ni hommes ni bétail;
Ine ndidzakhala ku Mizipa kuti ndizikuyimirirani kwa Ababuloni amene azidzabwera kwa ife, koma inu muzikolola vinyo wanu, zipatso zanu, mafuta anu ndi kuzisunga mʼmitsuko yanu, nʼkumakhala mʼmizinda imene mwalandayo.”
11 On y entendra la voix des fêtes et des joies, la voix de l'époux et la voix de l'épouse, et les voix de ceux qui diront: Rendez gloire au Seigneur tout-puissant; car le Seigneur est bon, et sa miséricorde est éternelle. Alors on apportera des présents au temple du Seigneur, parce que je ferai revenir tous les captifs de cette terre, et qu'ils seront comme ils étaient autrefois, dit le Seigneur,
Nawonso Ayuda onse a ku Mowabu, ku Amoni, ku Edomu ndi a ku mayiko ena onse anamva kuti mfumu ya ku Babuloni inasiyako anthu ena ku Yuda ndipo kuti inasankha Gedaliya mwana wa Ahikamu, mwana wa Safani, kukhala bwanamkubwa wawo.
12 Voici ce que dit le Seigneur Dieu des armées: En ce lieu désert où l'on ne voit ni hommes ni bétail, il y aura encore, dans toutes ses villes, des cabanes de pasteurs qui y feront reposer leurs troupeaux,
Tsono Ayuda onsewo anabwerera ku Yuda, ku Mizipa kwa Gedaliya, kuchokera ku mayiko onse kumene anabalalikira. Ndipo anakolola zipatso zochuluka ndi vinyo wambiri.
13 Il y en aura dans les villes des montagnes, dans les villes de Séphila, dans les villes de Nacheb, et en la terre de Benjamin, et autour de Jérusalem, et dans les villes de Juda les brebis viendront encore sous la main de ceux qui les comptent, dit le Seigneur.
Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri a ankhondo onse amene sanadzipereke aja anabwera ku Mizipa kwa Gedaliya
ndipo anamufunsa kuti, “Kodi sukudziwa kuti Baalisi mfumu ya Aamoni watuma Ismaeli mwana wa Netaniya kuti akuphe?” Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu sanawankhulupirire.
Tsono Yohanani mwana wa Kareya, mwamseri anawuza Gedaliya ku Mizipa kuti, “Loleni ndipite ndikaphe Ismaeli mwana wa Netaniya, ndipo palibe amene ati adziwe. Akuphereninji ndi kuchititsa Ayuda onse, amene akuzungulirani kuti abalalike ndi kuti otsala a ku Yuda awonongeke?”
Koma Gedaliya mwana wa Ahikamu anawuza Yohanani mwana wa Kareya kuti, “Usachite zimenezo! Zimene ukunena za Ismaeli ndi zabodza.”

< Jérémie 40 >