< 1 Chroniques 1 >

1 Adam, Seth, Enos,
Adamu, Seti, Enosi
2 Caïnan, Malalehel, Jared,
Kenani, Mahalaleli, Yaredi,
3 Enoch, Mathusalem, Larnech, Noé.
Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.
4 Fils de Noé: Sem, Cham, Japheth.
Ana a Nowa, Semu, Hamu ndi Yafeti.
5 Fils de Japheth: Corner, Magog, Madaï, Javan, Elisa, Thobel, Mosoch et Thiras.
Ana aamuna a Yafeti anali: Gomeri, Magogi, Madai, Yavani, Tubala, Mesaki ndi Tirasi.
6 Fils de Gomer: Ascenez, Rhiphath et Thorgama.
Ana aamuna a Gomeri anali: Asikenazi, Rifati ndi Togarima
7 Fils de Javan: Elisa, Tharsis, les Citians et les Rhodiens.
Ana aamuna a Yavani anali: Elisa, Tarisisi, Kitimu ndi Rodanimu.
8 Fils de Cham: Chus, Mesraïm, Phuth et Chanaan.
Ana aamuna a Hamu anali: Kusi, Miziraimu, Puti ndi Kanaani
9 Fils de Chus: Saba, Evila, Sabatha, Regma et Sabalhaca. Fils de Regma: Saba et Dadan.
Ana aamuna a Kusi anali: Seba, Havila, Sabita, Raama ndi Sabiteka Ana aamuna a Raama anali: Seba ndi Dedani.
10 Et Chus engendra Nemrod; celui-ci commença à être puissant et chasseur sur la terre.
Kusi anali abambo a Nimurodi amene anali wankhondo wamphamvu kwambiri pa dziko lapansi.
11 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Igupto ndiye kholo la Aludi, Aanami, Alehabu, Anafutu,
12 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Apaturusi, Akasilu (kumene kunachokera Afilisti) ndi Akafitori.
13 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Kanaani anabereka mwana wake wachisamba Sidoni, ndipo anaberekanso Ahiti,
14 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Ayebusi, Aamori, Agirigasi
15 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Ahivi, Aariki, Asini
16 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Aaravadi, Azemari ndi Ahamati.
17 Fils de Sem: Elam, Assur, Arphaxad,
Ana aamuna a Semu anali: Elamu, Asuri, Aripakisadi, Ludi ndi Aramu. Ana aamuna a Aramu anali: Uzi, Huri, Geteri ndi Mesaki.
18 Salé,
Aripakisadi anabereka Sela ndipo Selayo anabereka Eberi:
19 Salé,
Eberi anabereka ana aamuna awiri: wina anamutcha Pelegi, chifukwa pa nthawiyo anthu a pa dziko lapansi anagawikana. Dzina la mʼbale wake linali Yokitani.
20 Salé,
Yokitani anabereka Alimodadi, Selefi, Hazari-Maveti, Yera,
21 Salé,
Hadoramu, Uzali, Dikila
22 Salé,
Obali, Abimaeli, Seba,
23 Salé,
Ofiri, Havila ndi Yobabu. Onsewa anali ana aamuna a Yokitani.
24 Salé,
Semu, Aripakisadi, Sela
25 Héber, Phaleg, Réhu,
Eberi, Pelegi, Reu
26 Sarug, Nachor, Tharé.
Serugi, Nahori, Tera
27 Abraham.
ndi Abramu (amene ndi Abrahamu).
28 Fils d'Abraham: Isaac et Ismaël.
Ana a Abrahamu ndi awa: Isake ndi Ismaeli.
29 Voici leurs familles: premier-né d'Ismaël: Nabaïoth, Cédar, Abdéel, Massan,
Zidzukulu zake zinali izi: Nebayoti ndiye anali mwana woyamba wa Ismaeli, kenaka Kedara, Adibeeli, Mibisamu,
30 Masma, Duala, Massi, Choddan, Thèman,
Misima, Duma, Masa, Hadadi, Tema,
31 Jethur, Naphis, Cedma; voilà les fils d'Ismaël.
Yeturi, Nafisi ndi Kedema. Awa anali ana a Ismaeli.
32 Fils de Cettura, concubine d'Abraham: elle lui enfanta: Zameran, Jezan, Madian, Madal, Jesboc et Sué. Fils de Jezan: Dedan et Saba.
Ana a Ketura mzikazi wa Abrahamu anali awa: Zimurani, Yokisani, Medani, Midiyani, Isibaki ndi Suwa. Ana a Yokisani ndi awa: Seba ndi Dedani
33 Fils de Madian: Gephar, Aphir, Enoch, Abida et Elduga; voilà tous les fils de Cettura.
Ana aamuna a Midiyani anali, Efai, Eferi, Hanoki, Abida ndi Elida. Onsewa anali zidzukulu za Ketura.
34 Abraham engendra Isaac. Fils d'Isaac: Jacob et Esaü.
Abrahamu anabereka Isake. Ana a Isake anali awa: Esau ndi Israeli.
35 Fils d'Esaü: Eliphaz, Raguel, Jehul, Jeglon et Coré.
Ana aamuna a Esau anali awa: Elifazi, Reueli, Yeusi, Yolamu ndi Kora.
36 Fils d'Eliphaz: Thêman, Omar, Sophar, Gatham, Canez, Thamna et Amalec.
Ana a Elifazi anali awa: Temani, Omari, Zefo, Gatamu ndi Kenazi: Amene anabereka ndi Timna: Amaleki.
37 Fils de Raguel: Nachoth, Zaré, Somé et Mozé.
Ana a Reueli anali awa: Nahati, Zera, Sama ndi Miza.
38 Fils de Seïr: Lotan, Sobal, Sébégon, Ana, Dison, Asar et Rison.
Ana a Seiri anali awa: Lotani, Sobala, Zibeoni, Ana, Disoni, Ezeri ndi Disani.
39 Fils de Lotan: Horri et Héman; sœur de Lotan, Thamna.
Ana aamuna a Lotani anali awa: Hori ndi Homamu. Timna anali mlongo wake wa Lotani.
40 Fils de Sobal: Alon, Machanath, Tébel, Sophi et Onan. Fils de Sébégon: Eth et Sonan.
Ana aamuna a Sobala anali awa: Alivani, Manahati, Ebala, Sefo ndi Onamu. Ana aamuna a Zibeoni anali awa: Ayiwa ndi Ana.
41 Fils de Sonan: Dison. Fils de Dison: Emeron, Asebon, Jethram et Harran.
Mwana wa Ana anali Disoni. Ana a Disoni anali awa: Hemudani, Esibani, Itirani ndi Kerani
42 Fils d'Asar: Balaam, Zucam, Acan. Fils de Bison, Os et Aran.
Ana aamuna a Ezeri anali awa: Bilihani, Zaavani ndi Yaakani. Ana aamuna a Disani anali awa: Uzi ndi Arani.
43 Et voici leurs rois: Balac, fils de Béor; le nom de sa ville est Dennaba.
Awa ndi mafumu amene ankalamulira dziko la Edomu, mfumu iliyonse ya Israeli isanayambe kulamulira kumeneko: Bela mwana wa Beori, mzinda wake ankawutcha Dinihaba.
44 Balac mourut, et Jobab, fils de Zara de Bosora, régna à sa place.
Bela atamwalira, Yobabu mwana wa Zera wochokera ku Bozira analowa ufumu mʼmalo mwake.
45 Jobab mourut, et Asom, de la terre des Thêmanites, régna à sa place.
Yobabu atamwalira, Husamu wochokera ku dziko la Atemani, analowa ufumu mʼmalo mwake.
46 Asom mourut, et Adad, fils de Barad, régna à sa place; ce fut lui qui vainquit Madian dans le champ de Moab; le nom de sa ville est Gethaim.
Husamu atamwalira, Hadadi mwana wa Bedadi, amene anagonjetsa Amidiyani mʼdziko la Mowabu, analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Aviti.
47 Adad mourut, et Sebla (Samada) de Maseca régna à sa place.
Hadadi atamwalira, Samila wochokera ku Masireka analowa ufumu mʼmalo mwake.
48 Sebla mourut, et Saul de Rooboth, sur l'Euphrate, régna à sa place.
Samila atamwalira, Sauli wochokera ku Rehoboti wa ku Mtsinje analowa ufumu mʼmalo mwake.
49 Saul mourut, et Balaennor (Ballanan), fils d'Achobor, régna à sa place.
Sauli atamwalira, Baala-Hanani mwana wa Akibori analowa ufumu mʼmalo mwake.
50 Balaennor mourut, et Arad, fils de Barad, régna à sa place; le nom de sa ville est Phogor.
Pamene Baala-Hanani anamwalira, Hadadi analowa ufumu mʼmalo mwake. Mzinda wake unkatchedwa Pau, ndipo dzina la mkazi wake linali Mehatabeli mwana wa Matiredi, mwana wamkazi wa Me-Zahabu.
51 Chefs d'Edom: le chef Thaman (Thamna), le chef Golada (Gola), le chef Jéther,
Hadadi anamwaliranso. Mafumu a ku Edomu anali: Timna, Aliva, Yeteti,
52 Le chef Elibamas (Olibema), le chef Ela, le chef Phinon,
Oholibama, Ela, Pinoni,
53 Le chef Cenez, le chef Théman, le chef Bassor (Mazar),
Kenazi, Temani, Mibezari,
54 Le chef Magediel, le chef Zaphoin: voilà les chefs d'Edom.
Magidieli ndi Iramu. Awa anali mafumu a ku Edomu.

< 1 Chroniques 1 >