< Jérémie 45 >
1 La parole que Jérémie le prophète dit à Baruc, fils de Nérija, lorsqu’il écrivait ces paroles-là dans un livre, sous la dictée de Jérémie, en la quatrième année de Jehoïakim, fils de Josias, roi de Juda, disant:
Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku.
2 Ainsi dit l’Éternel, le Dieu d’Israël, à ton sujet, Baruc:
“Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti:
3 Tu as dit: Malheur à moi! car l’Éternel a ajouté le chagrin à ma douleur; je me suis fatigué dans mon gémissement, et je n’ai pas trouvé de repos.
Iwe unati, ‘Kalanga ine! Yehova wawonjezera chisoni pa mavuto anga. Ine ndatopa ndi kubuwula ndipo sindikupeza mpumulo.’”
4 Tu lui diras ainsi: Ainsi dit l’Éternel: Voici, ce que j’avais bâti, je le renverse, et ce que j’avais planté, je l’arrache, – tout ce pays.
Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse.
5 Et toi, tu chercherais pour toi de grandes choses? Ne les cherche pas; car voici, je fais venir du mal sur toute chair, dit l’Éternel; mais je te donnerai ta vie pour butin, dans tous les lieux où tu iras.
Kodi tsono ukudzifunira wekha zinthu zazikulu? Usadzifunire. Pakuti ndidzagwetsa mavuto pa anthu onse, koma ndidzasunga moyo wako kulikonse kumene ungadzapite.”