< Néhémie 7 >

1 Lorsque la muraille fut rebâtie et que j’eus posé les battants des portes, les portiers, les chantres et les lévites furent chargés de la surveillance.
Khoma linamangidwa ndipo zitseko zinayikidwa. Pambuyo pake alonda a Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo ndiponso Alevi anasankhidwa.
2 Je donnai autorité sur Jérusalem à Hanani, mon frère, et à Ananie, commandant de la citadelle, car c’était un homme fidèle et craignant Dieu plus que beaucoup d’autres.
Kenaka ine ndinasankha mʼbale wanga Hanani pamodzi ndi Hananiya woyangʼanira nsanja yankhondo kukhala olamulira Yerusalemu chifukwa iyeyu anali munthu odalirika ndi woopa Mulungu kuposa anthu ena.
3 Et je leur dis: « Que les portes de Jérusalem ne soient pas ouvertes avant que soit venue la chaleur du soleil; le soir, pendant que les gardes seront encore à leur poste, on fermera les portes et on mettra les barres; et, pendant la nuit, on établira des gardes pris parmi les habitants de Jérusalem, chacun à son poste, et chacun devant sa maison.
Ine ndinawawuza kuti, “Musalole kuti zipata za Yerusalemu zitsekulidwe mpaka dzuwa litatentha, ndipo alonda asanaweruke aonetsetse kuti atseka zitseko ndi kuzipiringidza. Musankhe alonda pakati pa anthu okhala mu Yerusalemu, ena akhale pa malo pawo ndi ena akhale moyangʼanana ndi nyumba zawo.”
4 Or la ville était spacieuse et grande, mais il n’y avait que peu d’habitants au milieu d’elle, et toutes les maisons n’étaient pas rebâties.
Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe.
5 Mon Dieu me mit au cœur d’assembler les grands, les magistrats et le peuple, pour en faire le dénombrement. Je trouvai un registre généalogique de ceux qui étaient montés les premiers, et j’y vis écrit ce qui suit:
Ndipo Mulungu wanga anayika mu mtima mwanga maganizo oti ndisonkhanitse anthu olemekezeka, akuluakulu ndi anthu onse kuti alembetse mayina mwa mabanja awo. Ndinapeza buku limene munalembedwa mayina a mabanja a iwo amene anayamba kubwera kuchokera ku ukapolo. Izi ndi zimene ndinazipeza zitalembedwa mʼmenemo:
6 Voici les gens de la province qui revinrent de l’exil, — ceux que Nabuchodonosor, roi de Babylone, avait emmenés captifs, et qui retournèrent à Jérusalem et en Juda, chacun dans sa ville, —
Awa ndi anthu a mʼchigawo cha Yuda amene anabwerera kuchokera ku ukapolo amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawatenga ukapolo. Iwo anabwerera ku Yerusalemu ndi ku Yuda, aliyense ku mzinda wa makolo ake.
7 qui revinrent avec Zorobabel, Josué, Néhémie, Azarias, Raamias, Nahamani, Mardochée, Belsan, Mespharath, Bégoaî, Nahum, Baana: Nombre des hommes du peuple d’Israël:
Anabwera pamodzi ndi atsogoleri awa: Zerubabeli, Yesuwa, Nehemiya, Azariya, Raamiya, Nahamani, Mordekai, Bilisani, Misipereti, Bigivai, Nehumu ndi Baana. Tsono chiwerengero cha anthu a ku Israeli chinali chotere:
8 les fils de Pharsos, deux mille cent soixante-douze;
Zidzukulu za Parosi 2,172
9 les fils de Saphatias, trois cent soixante-douze;
Zidzukulu za Sefatiya 372
10 les fils d’Aréa, six cent cinquante-deux;
Zidzukulu za Ara 652
11 les fils de Phahath-Moab, des fils de Josué et de Joab, deux mille huit cent dix-huit;
Zidzukulu za Pahati-Mowabu (kudzera mu mʼbado wa Yesuwa ndi Yowabu) 2,818
12 les fils d’Elam, mille deux cent cinquante-quatre;
Zidzukulu za Elamu 1,254
13 les fils de Zethua, huit cent quarante-cinq;
Zidzukulu za Zatu 845
14 les fils de Zachaï, sept cent soixante;
Zidzukulu za Zakai 760
15 les fils de Bannui, six cent quarante-huit;
Zidzukulu za Binuyi 648
16 les fils de Bébaï, six cent vingt-huit;
Zidzukulu za Bebai 628
17 les fils d’Azgad, deux mille trois cent vingt-deux;
Zidzukulu za Azigadi 2,322
18 les fils d’Adonicam, six cent soixante-sept;
Zidzukulu za Adonikamu 667
19 les fils de Béguaï, deux mille soixante-sept;
Zidzukulu za Abigivai 2,067
20 les fils d’Adin, six cent cinquante-cinq;
Zidzukulu za Adini 655
21 les fils d’Ater, fils d’Ezéchias, quatre-vingt-dix-huit;
Zidzukulu za Ateri (kudzera mwa Hezekiya) 98
22 les fils de Hasem, trois cent vingt-huit;
Zidzukulu za Hasumu 328
23 les fils de Bésaï, trois cent vingt-quatre;
Zidzukulu za Bezayi 324
24 les fils de Hareph, cent douze;
Zidzukulu za Harifu 112
25 les fils de Gabaon, quatre-vingt quinze;
Zidzukulu za Gibiyoni 95.
26 les gens de Bethléem et de Nétopha, cent quatre-vingt-huit;
Anthu a ku Betelehemu ndi Netofa 188
27 les gens d’Anathoth, cent vingt-huit;
Anthu a ku Anatoti 128
28 les gens de Beth-Azmoth, quarante-deux;
Anthu a ku Beti-Azimaveti 42
29 les gens de Cariathiarim, de Céphira et de Béroth: sept cent quarante-trois;
Anthu a ku Kiriati Yeyarimu Kefira ndi Beeroti 743
30 les gens de Rama et de Géba, six cent vingt et un;
Anthu a ku Rama ndi Geba 621
31 les gens de Machmas, cent vingt deux;
Anthu a ku Mikimasi 122
32 les gens de Béthel et de Haï, cent vingt-trois;
Anthu a ku Beteli ndi Ai 123
33 les gens de l’autre Nébo, cinquante-deux;
Anthu a ku Nebo winayo 52
34 les fils de l’autre Elam, mille deux cent cinquante-quatre;
Ana a Elamu wina 1,254
35 les fils de Harem, trois cent vingt;
Zidzukulu za Harimu 320
36 les fils de Jéricho, trois cent quarante cinq;
Zidzukulu za Yeriko 345
37 les fils de Lod, de Hadid et d’Ono, sept cent vingt et un;
Zidzukulu za Lodi, Hadidi ndi Ono 721
38 les fils de Sénaa, trois mille neuf cent trente.
Zidzukulu za Senaya 3,930.
39 Prêtres: les fils d’Idaïas, de la maison de Josué, neuf cent soixante-treize;
Ansembe anali awa: A banja la Yedaya (ndiye kuti zidzukulu za Yesuwa) 973
40 les fils d’Emmer, mille cinquante-deux;
Zidzukulu za Imeri 1,052
41 les fils de Phashur, mille deux cent quarante-sept;
Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247
42 les fils d’Arem, mille dix-sept.
Zidzukulu za Harimu 1,017.
43 Lévites: les fils de Josué et de Cedmiel, des fils d’Oduïas; soixante-quatorze.
Alevi anali awa: A banja la Yesuwa ndi Kadimieli, ndiye kuti zidzukulu za Hodaviya 74.
44 Chantres: les fils d’Asaph: cent quarante-huit.
Anthu oyimba: Zidzukulu za Asafu 148.
45 Portiers: les fils de Sellum, les fils d’Ater, les fils de Telmon, les fils d’Accub, les fils de Hatita, les fils de Sobaï; cent trente-huit.
Alonda a ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Salumu, Ateri, Talimoni, Hatita ndi Sobai 138.
46 Nathinéens: les fils de Soha, les fils de Hasupha, les fils de Tebbaoth,
Anthu ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu anali awa: Zidzukulu za Ziha, zidzukulu za Hasufa, zidzukulu za Tabaoti,
47 les fils de Céros, les fils de Siaa, les fils de Phadon,
Zidzukulu Kerosi, zidzukulu za Siya, zidzukulu za Padoni
48 les fils de Lébana, les fils de Hagaba, les fils de Selmaï,
Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,
49 les fils de Hanan, les fils de Géddel, les fils de Gaher,
Zidzukulu za Hanani, zidzukulu za Gideli, zidzukulu za Gahari,
50 les fils de Raaïas, les fils de Rasin, les fils de Nécoda,
Zidzukulu za Reyaya, zidzukulu za Rezini, zidzukulu za Nehoda,
51 les fils de Gézem, les fils d’Aza, les fils de Phaséa,
Zidzukulu za Gazamu, zidzukulu za Uza, zidzukulu za Paseya,
52 les fils de Bésée, les fils de Munim, les fils de Néphusim,
Zidzukulu za Besai, zidzukulu za Meunimu, zidzukulu za Nefusimu,
53 les fils de Bacbuc, les fils de Hacupha, les fils de Harhur,
Zidzukulu za Bakibuku, zidzukulu za Hakufa, zidzukulu za Harihuri,
54 les fils de Besloth, les fils de Mahida, les fils de Harsa,
Zidzukulu za Baziliti, zidzukulu za Mehida, zidzukulu za Harisa,
55 les fils de Bercos, les fils de Sisara, les fils de Théma,
Zidzukulu za Barikosi, zidzukulu za Sisera, zidzukulu za Tema
56 les fils de Nasia, les fils de Hatipha.
Zidzukulu za Neziya, ndi zidzukulu za Hatifa.
57 Fils des serviteurs de Salomon: les fils de Sothaï, les fils de Sophéreth, les fils de Pharida,
Zidzukulu za antchito a Solomoni: Zidzukulu za Sotai, zidzukulu za Sofereti, zidzukulu za Perida
58 les fils de Jahala, les fils de Darcon, les fils de Jeddel,
zidzukulu za Yaala, zidzukulu za Darikoni, zidzukulu za Gideli,
59 les fils de Saphatias, les fils de Hatil, les fils de Phochéreth-Asebaïm, les fils d’Amon.
zidzukulu za Sefatiya, zidzukulu za Hatilu zidzukulu za Pokereti-Hazebaimu ndi zidzukulu Amoni.
60 Total des Nathinéens et des fils des serviteurs de Salomon: trois cent quatre-vingt-douze.
Anthu onse ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi zidzukulu za antchito a Solomoni analipo 392.
61 Voici ceux qui partirent de Thel-Mêla, Thel-Harsa, Chérub, Addon et Emmer, et qui ne purent pas faire connaître leur maison paternelle et leur race, pour montrer qu’ils étaient d’Israël:
Ali munsiwa anachokera ku Teli-Mela, Teri-Harisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, koma sanathe kunena mwa tchutchutchu kuti makolo awo kapena mafuko awo analidi Aisraeli kapena ayi.
62 les fils de Dalaïas, les fils de Tobie, les fils de Nécoda, six cent quarante-deux.
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.
63 Et parmi les prêtres: les fils de Habia, les fils d’Accos, les fils de Berzellaï, qui avait pris pour femme une des filles de Berzellaï, le Galaadite, et fut appelé de leur nom.
Ndiponso ena pakati pa ansembe anali awa: zidzukulu za Hobiya, zidzukulu za Hakozi ndi zidzukulu za Barizilai (munthu amene anakwatira mwana wamkazi wa Barizilai wa ku Giliyadi ndipo amatchedwa dzina limenelo).
64 Ils cherchèrent leur titre attestant leurs généalogies, mais on ne le trouva point. Ils furent déclarés impurs et exclus du sacerdoce,
Iwowa anafufuzafufuza mayina awo mʼbuku la mibado ya mabanja awo ndipo sanapeze mayina awo kotero anachotsedwa pa unsembe nawerengedwa ngati odetsedwa pa chipembedzo.
65 et le gouverneur leur interdit de manger des choses très saintes, jusqu’à ce que le prêtre se levât pour consulter Dieu par l’Urim et le Thummim.
Choncho bwanamkubwa anawawuza anthuwo kuti asamadye nawo chakudya china chilichonse choperekedwa kwa Mulungu mpaka patapezeka wansembe wodziwa kugwiritsa bwino ntchito ya Urimu ndi Tumimu.
66 L’assemblée tout entière était de quarante-deux mille trois cent soixante personnes,
Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.
67 sans compter leurs serviteurs et leurs servantes, qui étaient au nombre de sept mille trois cent trente-sept; parmi eux se trouvaient deux cent quarante cinq chanteurs et chanteuses.
Kuwonjezera pamenepa panali antchito awo aamuna ndi aakazi 7,337 ndiponso anthu aamuna ndi aakazi oyimba nyimbo okwanira 245.
68 Ils avaient sept cent trente-six chevaux, deux cent quarante-cinq mulets,
Panali akavalo 736, abulu angʼonoangʼono 245.
69 quatre cent trente cinq chameaux et six mille sept cent vingt ânes.
Ngamira zawo zinalipo 435 ndipo abulu analipo 6,720.
70 Plusieurs des chefs de famille firent des dons pour l’œuvre. Le gouverneur donna au trésor mille dariques d’or, cinquante coupes, cinq cent trente tuniques sacerdotales.
Atsogoleri ena a mabanja anapereka mphatso zothandizira ntchito. Bwanamkubwa anapereka ku thumba losungira chuma, ndalama zagolide za makilogalamu asanu ndi atatu, mabeseni makumi asanu ndi zovala za ansembe 530.
71 Plusieurs des chefs de famille donnèrent au trésor de l’œuvre vingt mille dariques d’or et deux mille deux cents mines d’argent.
Atsogoleri ena amabanja anapereka ku thumba losungira chuma ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndiponso ndalama za siliva zokwana makilogalamu 1,250.
72 Ce que le reste du peuple donna fut de vingt mille dariques d’or, deux mille mines d’argent et soixante-sept tuniques sacerdotales.
Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67.
73 C’est ainsi que les prêtres et les lévites, les chantres, les portiers, des gens du peuple, les Nathinéens et tout Israël s’établirent dans leurs villes.
Choncho ansembe, Alevi, alonda a Nyumba ya Mulungu, anthu oyimba nyimbo, ena mwa anthu wamba, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu pamodzi ndi Aisraeli ena onse ankakhala mʼmizinda yawo. Pofika mwezi wachisanu ndi chiwiri Aisraeli onse anali atakhazikika mʼmizinda yawo.

< Néhémie 7 >