< Jobin 26 >

1 Job vastasi ja sanoi:
Pamenepo Yobu anayankha kuti,
2 "Kuinka oletkaan auttanut voimatonta, tukenut heikkoa käsivartta!
“Wamuthandizadi munthu wopanda mphamvu! Walimbitsadi dzanja la munthu wofowoka!
3 Kuinka oletkaan neuvonut taitamatonta ja ilmituonut paljon ymmärrystä!
Wapereka malangizo kwa munthu amene alibe nzeru! Ndipotu waonetsadi nzeru zochuluka!
4 Kenelle oikein olet puheesi pitänyt, ja kenen henki on sinusta käynyt?
Kodi wakuthandiza ndani kuti uyankhule mawu awa? Ndipo ndi mzimu wa yani umene unayankhula pakamwa pako?
5 Haamut alhaalla värisevät, vetten ja niiden asukasten alla.
“Mizimu ya anthu akufa ikunjenjemera pansi pa madzi, ndi zonse zokhala mʼmadzimo.
6 Paljaana on tuonela hänen edessänsä, eikä ole manalalla peitettä. (Sheol h7585)
Dziko la anthu akufa ndi lapululu pamaso pa Mulungu; chiwonongeko ndi chosaphimbidwa. (Sheol h7585)
7 Pohjoisen hän kaarruttaa autiuden ylle, ripustaa maan tyhjyyden päälle.
Mulungu anayala thambo la kumpoto pa phompho; Iye anakoloweka dziko lapansi mʼmalo mwake pamene panali popanda nʼkanthu komwe.
8 Hän sitoo vedet pilviinsä, eivätkä pilvet halkea niiden alla.
Amasunga madzi ambiri mʼmitambo yake, koma mitamboyo siphulika chifukwa cha kulemera kwa madziwo.
9 Hän peittää valtaistuimensa näkyvistä, levittää pilvensä sen ylitse.
Iye amaphimba mwezi wowala, amawuphimba ndi mitambo yake.
10 Hän on vetänyt piirin vetten pinnalle, siihen missä valo päättyy pimeään.
Mulungu anawalembera madzi malire wonga uta, kukhala malire pakati pa kuwunika ndi mdima.
11 Taivaan patsaat huojuvat ja hämmästyvät hänen nuhtelustaan.
Mizati yochirikiza mitambo yakumwamba imanjenjemera, ndi kudabwa pa kudzudzula kwake.
12 Voimallansa hän kuohutti meren, ja taidollansa hän ruhjoi Rahabin.
Ndi mphamvu zake anatontholetsa nyanja; ndi nzeru zake anakantha chirombo cha mʼmadzi chija chotchedwa Rahabe.
13 Hänen henkäyksestään kirkastui taivas; hänen kätensä lävisti kiitävän lohikäärmeen.
Ndi mpweya wake anayeretsa zamumlengalenga, dzanja lake linapha chinjoka chothawa chija.
14 Katso, nämä ovat ainoastaan hänen tekojensa äärten häämötystä, ja kuinka hiljainen onkaan kuiskaus, jonka hänestä kuulemme! Mutta kuka käsittää hänen väkevyytensä jylinän?"
Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake; tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona! Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?”

< Jobin 26 >