< Nehemian 10 >

1 Ja ne, jotka sinettinsä painoivat, olivat Nehemia Tirsata Hakalian poika, ja Zidkia,
Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
2 Seraja, Asaria, Jeremia,
Seraya, Azariya, Yeremiya
3 Pashur, Amaria, Malkia,
Pasuri, Amariya, Malikiya,
4 Hattus, Sebania, Malluk,
Hatusi, Sebaniya, Maluki,
5 Harim, Meremot, Obadia,
Harimu, Meremoti, Obadiya,
6 Daniel, Ginnetun, Baruk,
Danieli, Ginetoni, Baruki,
7 Mesullam, Abia, Mijamin,
Mesulamu, Abiya, Miyamini
8 Maasia, Bilgai ja Semaja: ne olivat papit.
Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
9 Mutta Leviläiset olivat: Jesua Asanian poika, Binnui, Henadadin lapsista, Kadmiel,
Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
10 Ja heidän veljensä: Sebania, Hodia, Kelita, Pelaja, Hanan,
ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
11 Miika, Rehob, Hasabia,
Mika, Rehobu, Hasabiya,
12 Sakkur, Serebia, Sebania,
Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
13 Hodia, Bani ja Beninu,
Hodiya, Bani ndi Beninu.
14 Kansan päämiehet olivat: Paros, Pahatmoab, Elam, Sattu, Bani,
Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
15 Bunni, Asgad, Bebai,
Buni, Azigadi, Bebai,
16 Adonia, Bigvai, Adin,
Adoniya, Bigivai, Adini,
17 Ater, Hiskia, Assur,
Ateri, Hezekiya, Azuri,
18 Hodia, Hasum, Betsai,
Hodiya, Hasumu, Bezayi
19 Hariph, Anatot, Neubai,
Harifu, Anatoti, Nebayi,
20 Magpias, Mesullam, Hesir,
Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
21 Mesesabel, Zadok, Jaddua,
Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
22 Pelatia, Hanan, Anaja,
Pelatiya, Hanani, Ananiya,
23 Hosea, Hanania, Hasub,
Hoseya, Hananiya, Hasubu
24 Halohes, Pilha, Sobek,
Halohesi, Piliha, Sobeki,
25 Rehum, Hasabna, Maeseja,
Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
26 Ahia, Hanan, Anan,
Ahiya, Hanani, Anani,
27 Malluk, Harim ja Baena;
Maluki, Harimu ndi Baana.
28 Ja muu kansa, papit, Leviläiset, ovenvartiat, veisaajat, Netinimit ja kaikki, jotka olivat erinneet maan kansoista Jumalan lain tykö vaimoinsa, poikainsa ja tytärtensä kanssa, ja kaikki, jotka sen ymmärtää taisivat.
Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
29 Ja heidän voimallisensa ottivat veljeinsä puolesta sen vastaan. Ja he tulivat vannomaan ja lupaamaan valallansa, vaeltaaksensa Jumalan laissa, joka heille oli annettu Moseksen Jumalan palvelian kautta, pitääksensä ja tehdäksensä kaikki Herran meidän Jumalamme käskyt, tuomiot ja säädyt;
tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
30 Ja ettei meidän pidä antaman maan kansoille tyttäriämme, emmekä myös ota pojillemme heidän tyttäriänsä.
“Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
31 Ja jos maan kansa tuo sabbatina kauppakalua ja kaikkinaista vuoden tuloa myytäväksi, niin emme ota heiltä sabbatina ja pyhäpäivänä; ja että me seitsemännen vuoden annamme olla vapaana kaikista rasituksista;
“Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
32 Ja panemme käskyn itse päällemme, että annamme kolmannen osan yhdestä siklistä ajastajasta Jumalamme huoneen palvelukseen:
“Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
33 Näkyleiväksi, alinomaiseksi ruokauhriksi, alinomaiseksi polttouhriksi, sabbatina, uusilla kuilla ja juhlapäivinä, ja pyhitetyille, ja syntiuhriksi, jolla Israel sovitetaan, ja kaikkinaiseksi tarpeeksi Jumalamme huoneessa.
Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
34 Ja me heitimme arpaa pappein, Leviläisten ja kansan välillä halkouhrista, joita joka vuosi piti vietämän meidän Jumalamme huoneesen, isäimme huonetten jälkeen, määrätyillä ajoilla poltettaa Herran meidän Jumalamme alttarilla, niinkuin laissa kirjoitettu on;
“Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
35 Ja että me joka vuosi tuomme maamme esikoisia ja kaikkinaisten puiden ensimäisiä hedelmiä Herran huoneesen;
“Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
36 Ja esikoiset pojistamme ja eläimistämme, niinkuin laissa kirjoitettu on; ja esikoiset härjistämme ja lampaistamme, että meidän pitää viemän meidän Jumalamme huoneesen papeille, jotka palvelevat Jumalamme huoneessa.
“Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
37 Ja meidän pitää viemän taikinasta ensimäisen, ja ylennyksemme, ja kaikkinaisia puun hedelmiä, viinaa ja öljyä papeille, meidän Jumalamme huoneen kammioihin, ja Leviläisille kymmenykset meidän maastamme, että Leviläiset kaikissa kaupungeissa pitää saaman kymmenykset meidän työstämme.
“Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
38 Ja papin Aaronin pojan pitää myös saaman Leviläisten kanssa heidän kymmenyksistänsä, ja Leviläisten pitää viemän kymmenyksistänsä kymmenennen osan meidän Jumalamme huoneesen, tavarahuoneen kammioihin.
Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
39 Sillä Israelin lapset ja Levin lapset piti myös viemän jyväin, viinan ja öljyn ylennyksen kammioihin; ja siellä pitää oleman pyhät astiat, ja papit, jotka palvelevat, ja ovenvartiat, ja veisaajat. Ja emme luovu meidän Jumalamme huoneesta.
Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”

< Nehemian 10 >