< Joosuan 12 >

1 Ja nämät ovat maan kuninkaat, jotka Israelin lapset löivät, ja ottivat heidän maansa tuolla puolella Jordania, auringon nousemista päin, Arnonin ojasta Hermonin vuoreen asti, ja kaikki lakeudet itään päin:
Aisraeli anagonjetsa dziko lonse la kummawa kwa Yorodani, kuyambira ku chigwa cha Arinoni mpaka ku phiri la Herimoni pamodzi ndi dera lonse la kummawa kwa Araba. Iwo anatenga dzikoli kukhala lawo, ndipo mafumu a dzikoli anali awa:
2 Sihon Amorilaisten kuningas, joka asui Hesbonissa ja hallitsi Aroerista, joka on Arnonin ojan reunalla, ja keskellä ojaa, ja puolen Gileadia Jabbokin ojaan asti, joka on Ammonin lasten raja,
Sihoni mfumu ya Aamori, amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi.
3 Ja lakeutta Kinneretin mereen asti itään päin, ja korven mereen, Suolaiseen mereen itään päin, BetJesimotin tietä myöten, ja lounaasta alaspäin lähelle Asdot Pisgaa;
Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga.
4 Siihen myös Ogin Basanin kuninkaan maan rajat, joka vielä jäänyt oli uljaista, ja asui Astarotissa ja Edreissä,
Ogi mfumu ya mzinda wa Basani, amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi.
5 Ja hallitsi Hermonin vuorella, Salkassa ja koko Basanissa, Gessurin ja Maakatin maan rajoihin, ja puolen Gileadia, joka Sihonin Hesbonin kuninkaan maan raja oli.
Dera la ufumu wake linafika ku phiri la Herimoni, ku Saleka ndi dziko lonse la Basani mpaka ku malire ndi anthu a ku Gesuri Makati. Ufumu wake unaphatikizanso theka la Giliyadi mpaka ku malire a mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.
6 Moses Herran palvelia ja Israelin lapset löivät heitä; ja Moses Herran palvelia antoi sen Rubenilaisille, Gadilaisille ja puolelle Manassen sukukunnalle omaisuudeksi.
Mose mtumiki wa Yehova ndi Aisraeli anawagonjetsa ndipo anapereka dziko lawo kwa anthu a fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti chikhale cholowa chawo.
7 Nämät ovat maan kuninkaat, jotka Josua löi ja Israelin lapset tällä puolella Jordania länteen päin, BaalGadista Libanonin vuorenlakeudella, sileään vuoreen, joka ulottuu Seiriin, jonka Josua Israelin sukukunnille antoi omaisuudeksi itsekullekin osansa jälkeen,
Yoswa ndi Aisraeli onse anagonjetsa mafumu onse okhala kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodani kuyambira ku Baala-Gadi, ku chigwa cha Lebanoni mpaka ku phiri la Halaki, kumapita cha ku Seiri. Yoswa anagawira dzikolo mafuko a Israeli kuti likhale cholowa chawo.
8 Vuorilla, laaksoissa, lakeudella, vetten tykönä, korvessa, ja lounaan puolessa: Hetiläiset, Amorilaiset, Kanaanealaiset, Pheresiläiset, Heviläiset ja Jebusilaiset;
Dziko limeneli linali dera la ku mapiri, chigwa cha kumadzulo, chigwa cha Yorodani, ku matsitso a kummawa, ndi dziko la chipululu la kummwera. Amene ankakhala mʼdzikoli anali Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Mafumu ake anali awa:
9 Jerihon kuningas, yksi; Ain kuningas, joka BetElin sivussa on, yksi;
mfumu ya Yeriko imodzi mfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi
10 Jerusalemin kuningas, yksi; Hebronin kuningas, yksi;
mfumu ya Yerusalemu imodzi mfumu ya Hebroni imodzi
11 Jarmutin kuningas, yksi; Lakiksen kuningas, yksi;
mfumu ya Yarimuti imodzi mfumu ya Lakisi imodzi
12 Eglonin kuningas, yksi; Geserin kuningas, yksi;
mfumu ya Egiloni imodzi mfumu ya Gezeri imodzi
13 Debirin kuningas, yksi; Gederin kuningas, yksi;
mfumu ya Debri imodzi mfumu ya Gederi imodzi
14 Horman kuningas, yksi; Aradin kuningas, yksi;
mfumu ya Horima imodzi mfumu ya Aradi imodzi
15 Libnan kuningas, yksi; Adullamin kuningas, yksi;
mfumu ya Libina imodzi mfumu ya Adulamu imodzi
16 Makkedan kuningas, yksi; BetElin kuningas, yksi;
mfumu ya Makeda imodzi mfumu ya Beteli imodzi
17 Tapuan kuningas, yksi; Hepherin kuningas, yksi;
mfumu ya Tapuwa imodzi mfumu ya Heferi imodzi
18 Aphekin kuningas, yksi; Lassaronin kuningas, yksi;
mfumu ya Afeki imodzi mfumu ya Lasaroni imodzi
19 Madonin kuningas, yksi; Hatsorin kuningas, yksi;
mfumu ya Madoni imodzi mfumu ya Hazori imodzi
20 SimronMeronin kuningas, yksi; Aksaphin kuningas, yksi;
mfumu ya Simuroni Meroni imodzi mfumu ya Akisafu imodzi
21 Taanakin kuningas, yksi; Megiddon kuningas, yksi;
mfumu ya Taanaki imodzi mfumu ya Megido imodzi
22 Kedeksen kuningas, yksi; Jokneamin kuningas Karmelin tykönä, yksi;
mfumu ya Kadesi imodzi mfumu ya Yokineamu ku Karimeli imodzi
23 DornaphatDorin kuningas, yksi, ja pakanain kuningas Gilgalissa, yksi;
mfumu ya Dori ku Nafoti Dori imodzi mfumu ya Goyini ku Giligala imodzi
24 Tirtsan kuningas, yksi. Ne kaikki ovat yksineljättäkymmentä kuningasta.
mfumu ya Tiriza imodzi mafumu onse pamodzi analipo 31.

< Joosuan 12 >