< Jeremian 6 >
1 Kootkaat teitänne, te Benjaminin lapset, Jerusalemista, ja puhaltakaat torveen Tekoassa, ja nostakaat lippu Betkeremissä; sillä pohjasta on pahuus ja suuri viheliäisyys käsissä.
“Thawani, inu anthu a ku Benjamini! Tulukani mu Yerusalemu! Lizani lipenga ku Tekowa! Kwezani mbendera ku Beti-Hakeremu! Pakuti tsoka lalikulu likubwera kuchokera kumpoto, ndipo chiwonongekocho nʼchachikulu.
2 Minä olen verrannut Zionin tyttären kauniisen ja ihanaiseen:
Kodi mzinda wa Ziyoni suli ngati msipu wokongola kwambiri, kumene abusa amafikako ndi ziweto zawo?
3 Mutta paimenet tulevat hänen tykönsä laumoinensa; he panevat majansa hänen ympärillensä, ja kukin kaitsee paikassansa,
Abusa ndi nkhosa zawo adzabwera kudzalimbana nawo; adzamanga matenti awo mowuzinga, ndipo aliyense adzakhazika anthu ake pamalo pake.”
4 (Ja sanoo: ) pyhittäkäät sota häntä vastaan, nouskaat ja käykäämme puolipäivänä ylös; voi meitä! sillä ehtoo joutuu ja varjo tulee suureksi.
Adzanena kuti, “Konzekani kuwuthira nkhondo mzindawo! Nyamukani, kuti tiwuthire nkhondo mzindawu masana ano. Koma tili ndi tsoka, dzuwa lapendeka, ndipo zithunzithunzi za kumadzulo zikunka zitalika.
5 Nouskaat ja astukaamme ylös yöllä, ja hävittäkäämme hänen jalot huoneensa.
Tsono nyamukani kuti tiwuthire nkhondo mzindawu usiku uno ndi kuwononga malinga ake!”
6 Sillä näin sanoo Herra Zebaot: kaatakaat puita, ja tehkäät multaseiniä Jerusalemia vastaan; sillä kaupunki pitää kuritettaman, sen sisällä on sula vääryys.
Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Dulani mitengo ndipo mumange mitumbira yankhondo kulimbana ndi Yerusalemu. Mzinda umenewu uyenera kulangidwa; wadzaza ndi kuponderezana.
7 Niinkuin lähde kuohuttaa vetensä; niin kuohuu myös hänen pahuutensa; vääryys ja hävitys siinä kuullaan, kitu ja vaiva on aina minun edessäni.
Monga momwe chitsime chimatulutsira madzi ndi mmenenso Yerusalemu amatulutsira zoyipa zake. Chiwawa ndi chiwonongeko ndi zomwe zimamveka mu mzindamo; nthenda yake ndi mabala ake ndimaziona nthawi zonse.
8 Anna sinuas kurittaa, Jerusalem, ettei minun sydämeni kääntyisi pois sinusta, etten minä sinua hävittäisi, niin ettei kenkään asu siinä maassa.
Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro, kuopa kuti chikondi changa pa iwe chingakuchokere ndi kusandutsa dziko lako kukhala bwinja mopanda munthu wokhalamo.”
9 Näin sanoo Herra Zebaot: mitä Israelissa jäänyt on, se pitää myös sulaksi saaliiksi joutuman niinkuin viinapuu; kokota kätes koriin niinkuin viinamarjain poimia.
Yehova Wamphamvuzonse anandiwuza kuti, “Adani adzawakunkha ndithu anthu otsala a Israeli, monga momwe amachitira populula mphesa. Tsono iwe yesetsa kupulumutsa amene ungathe monga mmene amachitira munthu wokolola mphesa.”
10 Kenelle siis minä puhun ja todistan, että joku kuulis? Katso, heidän korvansa ovat ympärileikkaamatta eikä taida kuulla; katso, he pitävät Herran sanan pilkkana ja ei kärsi sitä.
Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza? Ndinene mawu ochenjeza kwa yani kuti amve? Makutu awo ndi otsekeka kotero kuti sangathe kumva. Mawu a Yehova ndi onyansa kwa iwo; sasangalatsidwa nawo.
11 Sentähden olen minä niin täynnä Herran vihaa, etten minä taida lakata vuodattamasta, sekä lasten päälle kaduilla, ja myös nuorukaisten kokouksen päälle yhtä haavaa; sillä sekä mies että vaimo, ijällinen ja ikivanha pitää otettaman kiinni.
Koma ine ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova, ndipo ndatopa ndi kusunga mkwiyo wa Yehova. Yehova anandiwuza kuti, “Tsono ndidzawutulutsira mkwiyo umenewu pa ana oyenda mʼmisewu ndi pa achinyamata amene asonkhana pamodzi; pakutinso mwamuna ndi mkazi wake adzatengedwa, pamodzi ndi okalamba amene ali ndi zaka zochuluka.
12 Heidän huoneensa pitää tuleman muukalaisten käsiin, heidän peltonsa ja emäntänsä yhtä haavaa; sillä minä ojennan käteni maan asujain ylitse, sanoo Herra.
Nyumba zawo adzazipereka kwa ena, pamodzi ndi minda yawo ndi akazi awo. Ndidzatambasula dzanja langa kukantha anthu okhala mʼdzikomo,” akutero Yehova.
13 Sillä he kaikki ahnehtivat, sekä pienet että suuret; prophetat ja papit opettavat väärin,
“Kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu, onse ali ndi dyera lofuna kupeza phindu mwa kuba; aneneri pamodzi ndi ansembe omwe, onse amachita zachinyengo.
14 Ja lohduttavat kansaani hänen viheliäisyydessänsä, sitä halpana pitämään, ja sanovat: rauha, rauha; ja ei rauhaa olekaan.
Amapoletsa zilonda za anthu anga pamwamba pokha. Iwo amanena kuti, ‘Mtendere, mtendere,’ pamene palibe mtendere.
15 Sentähden pitää heidän häpiään tuleman, että he kauhistuksen tekevät; ja vaikka he tahtovat olla häpäisemättä, eikä taida hävetä, kuitenkin pitää heidän jokaisen lankeeman toinen toisensa päälle; ja koska minä heitä kuritan, silloin pitää heidän lankeeman, sanoo Herra.
Kodi amachita manyazi akamachita zonyansazo? Ayi, sachita manyazi ndi pangʼono pomwe; sadziwa ndi kugwetsa nkhope komwe. Choncho iwo adzagwera pakati pa anzawo amene agwa kale; adzagwa pansi tsiku limene ndidzawalange,” akutero Yehova.
16 Näin sanoo Herra: seisokaat teillä, katsokaat ja kysykäät entisiä teitä, kuka oikia tie on, sitä te vaeltakaat, niin te löydätte levon teidän sieluillenne. Mutta he sanovat: emme vaella.
Yehova akuti, “Imani pa mphambano ndipo mupenye; kumeneko ndiye kuli njira zakale, funsani kumene kuli njira yabwino. Yendani mʼmenemo, ndipo mudzapeza mpumulo wa miyoyo yanu. Koma inu munati, ‘Ife sitidzayenda njira imeneyo.’
17 Ja minä olen pannut teille vartiat: ottakaat vaari torven äänestä; mutta he sanovat: emme ota vaaria.
Ine ndinakupatsani alonda oti akuyangʼanireni ndipo ndinati, ‘Imvani kulira kwa lipenga!’ koma inu munati, ‘Sitidzamvera.’
18 Sentähden, te pakanat, kuulkaat, ja ota vaari, sinä kokous, niistä mitkä heidän seassansa tapahtuu.
Nʼchifukwa chake imvani, inu anthu a mitundu ina; yangʼanitsitsani, inu amene mwasonkhana pano, chimene chidzawachitikire anthuwo.
19 Maa, kuule sinä; katso, minä annan tulla kovan onnen tälle kansalle, heidän ansaitun palkkansa, ettei he pidä lukua minun sanastani, mutta hylkäävät minun lakini.
Imvani, inu anthu okhala pa dziko lapansi, ndikubweretsa masautso pa anthu awa. Zimenezi ndi mphotho ya ntchito zawo. Iwowa sanamvere mawu anga ndipo anakana lamulo langa.
20 Mitä minä lukua pidän pyhästä savusta, joka rikkaasta Arabiasta tulee, eli hyvästä kanelista, joka kaukaiselta maalta tulee? Teidän polttouhrinne ei ole minulle otollinen eikä teidän uhrinne kelpaa minulle.
Kodi pali phindu lanji ngakhale mubwere ndi lubani kuchokera ku Seba, kapena zonunkhira zina kuchokera ku dziko lakutali? Nsembe zanu zopsereza Ine sindidzalandira; nsembe zanu sizindikondweretsa.”
21 Sentähden sanoo Herra näin: katso, minä annan tälle kansalle lankeemuksen: siihen pitää sekä isät että lapset kaikki itsensä loukkaaman, ja kylän miehet pitää hukkuman toinen toisensa kanssa.
Choncho Yehova akuti, “Ndidzayika zokhumudwitsa pamaso pa anthu awa. Abambo ndi ana awo aamuna onse adzapunthwa ndi kugwa; anansi awo ndi abwenzi awo adzawonongeka.”
22 Näin sanoo Herra: katso, kansa on tuleva pohjoisesta maakunnasta, ja suuri kansa on nouseva maan vieristä.
Yehova akunena kuti, “Taonani, gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto; mtundu wa anthu amphamvu wanyamuka kuchokera kumathero a dziko lapansi.
23 Jolla on joutset ja kilvet, hän on julma ja armotoin; heidän äänensä pauhaa niinkuin meri; he ajavat hevosilla, he ovat niinkuin varustettu sotaväki sinua vastaan, sinä tytär Zion.
Atenga mauta ndi mikondo; ndi anthu ankhanza ndi opanda chifundo. Phokoso lawo lili ngati mkokomo wa nyanja. Akwera pa akavalo awo ndipo akonzekera ngati anthu ankhondo, kudzakuthirani nkhondo anthu a ku Ziyoni.”
24 Me olemme kuulleet heistä sanoman, ja meidän kätemme ovat nääntyneet; tuska ja ahdistus on meidät käsittänyt niinkuin lapsensynnyttäjän.
A ku Ziyoni akuti “Ife tamva mbiri yawo, ndipo manja anthu alefukiratu. Nkhawa yatigwira, ndipo tikumva ululu ngati mayi pa nthawi yake yochira.
25 Älkään kenkään lähtekö pellolle, ja älköön kenkään tielle menkö; sillä joka paikassa on rauhattomuus vihollisen miekan tähden.
Musapite ku minda kapena kuyenda mʼmisewu, pakuti mdani ali ndi lupanga, ndipo ponseponse anthu akuchita mantha.
26 O sinä, minun kansani tytär, pue säkki ylles ja aseta itses tuhkaan, sure niinkuin ainoaa poikaa suurella murheella; sillä hävittäjä tulee äkisti meidän päällemme.
Inu anthu anga, valani ziguduli ndipo gubudukani pa phulusa; lirani mwamphamvu ngati munthu wolirira mwana wake mmodzi yekha, pakuti mwadzidzidzi wowonongayo adzabwera kudzatipha.
27 Minä olen pannut sinun vartian torniksi ja linnaksi minun kansassani, tietämään ja koettelemaan heidän teitänsä.
“Iwe Yeremiya, ndakuyika kuti ukhale choyesera zitsulo. Uwayese anthu anga monga ungayesere chitsulo kuti uwone makhalidwe awo.
28 He ovat kaikki peräti pois luopuneet, vaeltain petollisesti; he ovat kaikki turmeltu vaski ja rauta.
Onsewo ali ndi khalidwe lokanika ndi lowukira ndipo akunka nanena zamiseche. Iwo ndi olimba ngati mkuwa ndi chitsulo. Onse amangochita zoyipa zokhazokha.
29 Palkeet ovat tulella poltetut, lyijy raukee pois, sulaaminen on hukassa; sillä ei paha ole eroitettu.
Moto mu mvukuto ukuyaka kwambiri; mtovu watha kusungunuka ndi moto. Koma ntchito yosungunulayo sikupindula chifukwa zoyipa sizikuchokapo.
30 Sentähden he myös kutsutaan hyljätyksi hopiaksi, sillä Herra on heidät hyljännyt.
Iwo ali ngati siliva wotayidwa, chifukwa Yehova wawakana.”