< Psalmaro 150 >

1 Haleluja! Gloru Dion en Lia sanktejo, Gloru Lin en la firmaĵo de Lia forto.
Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
2 Gloru Lin por Liaj potencaj faroj, Gloru Lin laŭ Lia granda majesto.
Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
3 Gloru Lin per sonado de trumpeto, Gloru Lin per psaltero kaj harpo.
Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
4 Gloru Lin per tamburino kaj danco, Gloru Lin per kordinstrumentoj kaj fluto.
Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
5 Gloru Lin per laŭtaj cimbaloj, Gloru Lin per tintantaj cimbaloj.
Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
6 Ĉio spiranta gloru la Eternulon. Haleluja!
Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.

< Psalmaro 150 >