< Zechariah 9 >

1 The birthun of the word of the Lord, in the lond of Adrach, and of Damask, the reste therof; for `of the Lord is the iye of man, and of alle lynagis of Israel.
Mawu a Yehova odzudzula dziko la Hadiraki ndi mzinda wa Damasiko pakuti maso a anthu ndiponso mafuko onse a Israeli ali pa Yehova—
2 And Emath in termes therof, and Tirus, and Sidon; for thei token to hem wisdom greetli.
ndiponso mzinda wa Hamati, umene ukuchita malire ndi dzikoli, komanso pa Turo ndi Sidoni, ngakhale kuti iwo ndi anzeru kwambiri.
3 And Tirus bildide his strengthing, and gaderide siluer as erthe, and gold as fen of stretis.
Ndipo Turo anadzimangira linga; wadziwunjikira siliva ngati fumbi, ndi golide ngati zinyalala za mʼmisewu.
4 Lo! the Lord schal welde it, and schal smyte in the see the strengthe therof, and it schal be deuourid bi fier.
Taonani Ambuye adzamulanda chuma chakecho ndi kuwononga mphamvu zake mʼnyanja, ndipo adzapserera ndi moto.
5 Ascalon schal see, and schal drede; and Gasa, `and schal sorewe ful myche; and Accaron, for the hope therof is confoundid; and the kyng schal perische fro Gasa, and Ascalon schal not be enhabited;
Mzinda wa Asikeloni udzaona zimenezi, nʼkuchita mantha; Gaza adzanjenjemera ndi ululu, chimodzimodzinso Ekroni, chifukwa chiyembekezo chake chidzatheratu. Mfumu ya ku Gaza idzaphedwa ndipo Asikeloni adzakhala opanda anthu.
6 and a departere schal sitte in Asotus, and Y schal distrie the pride of Filisteis.
Mu Asidodi mudzakhala mlendo, ndipo ndidzathetsa kunyada kwa Afilisti.
7 And Y schal take awei the blood therof fro the mouth of him, and abhomynaciouns of hym fro the myddil of teeth of hym, and he also schal be left to our God; and he schal be as a duyk in Juda, and Accaron as Jebusei.
Ndidzachotsa nyama ya magazi mʼkamwa mwawo, chakudya choletsedwa mʼmano mwawo. Amene atsala adzakhala anthu a Mulungu wathu, adzasanduka atsogoleri mu Yuda, ndipo Ekroni adzakhala ngati Ayebusi.
8 And Y schal cumpasse myn hous of these that holden kniythod to me, and goen, and turnen ayen; and `an vniust axere schal no more passe on hem, for now Y siy with myn iyen.
Koma Ine ndidzalondera Nyumba yanga ndi kuyiteteza kwa ankhondo osakaza. Palibenso mdani amene adzagonjetse anthu anga, pakuti tsopano ndikuwayangʼanira.
9 Thou douyter of Sion, make ioie withoutforth ynow, synge, thou douyter of Jerusalem; lo! thi kyng schal come to thee, he iust, and sauyour; he pore, and stiynge on a sche asse, and on a fole, sone of a sche asse.
Sangalala kwambiri, iwe mwana wamkazi wa Ziyoni! Fuwula, mwana wamkazi wa Yerusalemu! Taona, mfumu yako ikubwera kwa iwe, yolungama ndi yogonjetsa adani, yodzichepetsa ndi yokwera pa bulu, pa mwana wamphongo wa bulu.
10 And Y schal leese foure horsid carte of Effraym, and an hors of Jerusalem, and the bouwe of batel schal be distried; and he schal speke pees to hethene men, and the power of him schal be fro see til to see, and fro floodis til to the endis of erthe.
Ndidzachotsa magaleta ankhondo ku Efereimu ndi akavalo ankhondo ku Yerusalemu, ndipo uta wankhondo udzathyoka. Mfumuyo idzabweretsa mtendere pakati pa mitundu ya anthu. Ulamuliro wake udzayambira ku nyanja ina mpaka ku nyanja ina, ndipo kuchokera ku Mtsinje (Yufurate) mpaka ku malekezero a dziko lapansi.
11 And thou in blood of thi testament sentist out thi boundun men fro lake, in which is not water.
Tsono kunena za iwe, chifukwa cha magazi a pangano lako ndi Ine, ndidzamasula amʼndende ako, ndidzawatulutsa mʼdzenje lopanda madzi.
12 Ye boundun of hope, be conuertid to strengthing; and to dai Y schewynge schal yelde to thee double thingis,
Bwererani ku malo anu otetezedwa, inu amʼndende achiyembekezo; ngakhale tsopano ndikulengeza kuti ndidzakubwezerani zabwino mowirikiza.
13 for Y schal stretche forthe to me Juda as a bowe, Y fillide `the lond of Effraym. And Y schal reise thi sones, thou Sion, on thi sones, thou lond of Grekis, and Y schal sette thee as the swerd of stronge men.
Ndidzakoka Yuda monga ndimakokera uta wanga, ndipo Efereimu ndiye muvi wake. Ndidzadzutsa ana ako iwe Ziyoni, kulimbana ndi ana ako iwe Grisi, ndipo ndidzakusandutsa iwe lupanga la munthu wankhondo.
14 And the Lord God schal be seyn on hem, and the dart of him schal go out as leit.
Pamenepo Yehova adzaonekera kwa anthu ake; mivi yake idzangʼanima ngati chingʼaningʼani. Ambuye Yehova adzaliza lipenga; ndipo adzayenda mu mkuntho wochokera kummwera,
15 And the Lord God schal synge in a trumpe, and schal go in whirlwynd of the south; the Lord of oostis schal defende hem, and thei schulen deuoure, and make suget with stoonys of a slynge; and thei drynkynge schulen be fillid as with wyn, and schulen be fillid as viols, and as hornes of the auter.
ndipo Yehova Wamphamvuzonse adzawateteza. Iwo adzawononga ndipo adzagonjetsa ndi miyala ya legeni. Adzamwa magazi ndi kubangula ngati amwa vinyo; magazi adzayenderera ngati a mʼmbale yowazira magazi pa ngodya za guwa lansembe.
16 And the Lord God `of hem schal saue hem in that dai, as a floc of his puple, for hooli stoonus schulen be reisid on the lond of hym.
Tsiku limenelo Yehova Mulungu wawo adzawapulumutsa pakuti anthu ake ali ngati nkhosa. Adzanyezimira mʼdziko lake ngati miyala yokongola pa chipewa chaufumu.
17 For what is the good of hym, and what is the faire of hym, no but whete of chosun men, and wyn buriownynge virgyns?
Taonani chikoka ndi kukongola kwawo! Tirigu adzasangalatsa anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.

< Zechariah 9 >