< Psalms 133 >

1 The song of grecis. Lo! hou good and hou myrie it is; that britheren dwelle togidere.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2 As oynement in the heed; that goith doun in to the beerd, in to the beerd of Aaron. That goith doun in to the coler of his cloth; as the dew of Ermon,
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3 that goith doun in to the hil of Sion. For there the Lord sente blessing; and lijf til in to the world.
Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.

< Psalms 133 >