< Psalms 131 >

1 The song of greces, `to Dauith himself. Lord, myn herte is not enhaunsid; nether myn iyen ben reisid. Nether Y yede in the grete thingis; nether in merueilis aboue me.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 If Y feelide not mekely; but enhaunside my soule. As a childe wenyde on his modir; so yelding be in my soule.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Israel hope in the Lord; fro this tyme now and in to the world.
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalms 131 >