< Nehemiah 10 >
1 Forsothe the seeleris weren Neemye, Athersata, the sone of Achilai,
Amene anasindikiza chidindo anali awa: Nehemiya, bwanamkubwa uja, mwana wa Hakaliya. Zedekiya,
2 and Sedechie, Saraie, Azarie, Jeremye, Phasur,
Seraya, Azariya, Yeremiya
Pasuri, Amariya, Malikiya,
Hatusi, Sebaniya, Maluki,
5 Mellucarem, Nerymuth, Oddie, Danyel,
Harimu, Meremoti, Obadiya,
6 Genton, Baruc, Mosollam, Abia,
Danieli, Ginetoni, Baruki,
7 Mianymy, Mazie, Belga, and Semeie;
Mesulamu, Abiya, Miyamini
Maziya, Biligai ndi Semaya Awa anali ansembe.
9 Forsothe dekenes weren Josue, the sone of Azarie, Bennuy, of the sones of Ennadab,
Alevi anali awa: Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa fuko la Henadadi, Kadimieli,
10 Cedinyel, and hise britheren, Sethenye, Odenmye, Telita, Phalaie, Anam,
ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,
12 Zaccur, Serebie, Sabanye,
Zakuri, Serebiya, Sebaniya,
14 The heedis of the puple, Phetos, Moab, Elam,
Atsogoleri a anthu anali awa: Parosi, Pahati-Mowabu, Elamu, Zatu, Bani,
15 Zecu, Banny, Bonny, Azgad, Bebay,
Buni, Azigadi, Bebai,
18 Odenye, Assuyn, Bessaie,
Hodiya, Hasumu, Bezayi
20 Methpie, Mosollam, Azir,
Magipiyasi, Mesulamu, Heziri
21 Meizabel, Sadoch, Reddua,
Mesezabeli, Zadoki, Yaduwa
22 Pheltie, Ananye, Osee,
Pelatiya, Hanani, Ananiya,
Halohesi, Piliha, Sobeki,
25 Reu, Asebyne, Mathsie,
Rehumu, Hasabiya, Maaseya,
Maluki, Harimu ndi Baana.
28 and othere of the puple, prestis, dekenes, porteris, and syngeris, Natynneis, and alle men that departiden hem silf fro the puplis of londis to the lawe of God, the wyues of hem, and `the sones of hem, and the douytris of hem;
Ife otsalafe, ndiye kuti ansembe, Alevi, alonda a ku Nyumba ya Mulungu, oyimba nyimbo, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu, onse amene anadzipatula pakati pa anthu a mitundu ina kuti atsate malamulo a Yehova, pamodzi ndi akazi athu, ana athu ndi onse amene ali ndi nzeru,
29 alle that myyten vndurstonde, bihetynge for her britheren, the principal men of hem, `and thei that camen to biheete, and to swere, that thei schulden go in the lawe of the Lord, which he `hadde youe bi the hond of Moyses, his seruaunt, that thei schulden do and kepe alle the heestis of `oure Lord God, and hise domes, and hise cerymonyes; and that we schulden not yyue
tikuphatikana ndi abale athu wolemekezeka, ndipo tikulonjeza molumbira kuti tidzayenda motsata malamulo a Mulungu amene anapereka kudzera mwa Mose mtumiki wa Mulungu. Tilonjeza kumvera ndi kutsata bwino mawu onse, miyambo yonse ndi malangizo onse a Yehova. Yehova atilange ngati sitidzachita zimenezi.
30 oure douytris to the puple of the lond, and that we schulden not take her douytris to oure sones.
“Ife tikulonjeza kuti sitidzapereka ana athu aakazi kuti akwatiwe ndi amuna a mayiko ena kapena kutenga ana awo aakazi kuti akwatiwe ndi ana athu aamuna.
31 Also the puplis of the lond, `that bryngen in thingis set to sale, and alle thingis to vss, bi the dai of sabat, for to sille, we schulen not take of hem in the sabat, and in a dai halewid; and we schulen leeue the seuenthe yeer, and the axynge of al hond.
“Ngati anthu a mitundu ina abwera ndi zinthu za malonda, monga tirigu, kudzagulitsa pa tsiku la Sabata, sitidzawagula pa tsiku la Sabata kapena pa tsiku lina lililonse loyera. Pa chaka chilichonse cha chisanu ndi chiwiri tidzagoneka munda wosawulima ndipo tidzafafaniza ngongole zonse.
32 And we schulen ordeyne comaundementis `on vs, that we yyue the thridde part of a sicle `bi the yeer to the werk of `oure Lord God,
“Tikulonjezanso molumbira kuti chaka ndi chaka tizipereka magalamu anayi a siliva kuti zithandize ntchito ya ku Nyumba ya Mulungu wathu.
33 to the looues of settyngforth, and to the euerlastynge sacrifice, `and in to brent sacrifice euerlastynge, in sabatis, in calendis, `that is, bigynnyngis of monethis, in solempnytees, in halewid daies, and for synne, that `me preie for Israel, and in to al the vss of the hows of oure God.
Ndalamayi izithandiza kulipirira buledi wa pa tebulo, chopereka cha chakudya cha nthawi zonse, zopereka zopsereza za nthawi zonse, zopereka za pa tsiku la Sabata, za pachikondwerero cha Mwezi Watsopano, za pa masiku a chikondwerero osankhika, zopereka za zinthu zopatulika, zopereka za nsembe yopepesera machimo a Aisraeli ndi ntchito ina iliyonse ya ku Nyumba ya Mulungu.
34 `Therfor we senten `lottis on the offryng of trees, bitwixe prestis and dekenes and the puple, that tho schulden be brouyt in to the hows of oure God, bi the housis of oure fadris bi tymes, fro the tymes of a yeer `til to a yeer, that `tho schulden brenne on the auter of `oure Lord God, as it is writun in the lawe of Moyses;
“Ife ansembe, Alevi ndi anthu onse, tachita maere kuti tidziwe pamene banja lathu lililonse lidzabweretsa ku nyumba ya Mulungu wathu pa nthawi yoyikika ya chaka zopereka za nkhuni zoyaka pa guwa lansembe la Yehova Mulungu wathu, monga momwe zinalembedwera mʼMalamulo.”
35 and that we bringe the firste gendrid thingis of oure lond, and the firste fruytis of al fruyt of ech tree, fro yeer in to yeer,
“Tilonjezanso kuti tidzabwera ndi zipatso zoyamba kucha za mʼminda yathu ndi zipatso zoyamba kucha za mtengo uliwonse wa zipatso chaka ndi chaka kuti tidzapereke ku Nyumba ya Mulungu wathu.”
36 in to the hows of the Lord, and the firste gendrid thingis of oure sones, and of oure beestis, as it is writun in the lawe, and the firste gendrid thingis of oure oxis, and of oure scheep, that tho be offrid in the hows of oure God, to prestis that mynystren in the hows of oure God;
“Tidzabweranso nawo ku Nyumba ya Mulungu, kwa ansembe amene amatumikira ku Nyumba ya Mulungu ana athu aamuna oyamba kubadwa ndi ana angʼombe oyamba kubadwa monga zalembedwera mu Malamulo. Tidzaperekanso ana oyamba kubadwa a ziweto zathu ndi ana ankhosa oyamba kubadwa.”
37 and we schulen brynge the firste fruytis of oure metis, and of oure moiste sacrifices, and the applis of ech tre, and of vendage, and of oile, to `prestis, at the treserie of the Lord, and the tenthe part of oure lond to dekenes; thilke dekenes schulen take tithis of alle the citees of oure werkis.
“Ndiponso ku zipinda za Nyumba ya Mulungu wathu, kwa ansembe tidzaperekanso mtanda wathu wa buledi wa ufa ndi mphatso zina monga zipatso za mtengo uliwonse, vinyo ndi mafuta. Tidzaperekanso kwa alevi chakhumi cha mbewu zathu pakuti alevi ndiwo amasonkhanitsa chakhumi mʼmidzi yathu yonse.
38 Sotheli a prest, the sone of Aaron, schal be with the dekenes in the tithis of dekenes; and the dekenes schulen offre the tenthe part of her tithe in the hows of oure God, `at the tresorie, in the hows of tresour.
Wansembe, mdzukulu wa Aaroni azikhala pamodzi ndi Alevi pamene akulandira chakhumi. Ndipo Alevi azibwera ndi chakhumicho ku nyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda zosungiramo chuma.”
39 For the sones of Israel and the sones of Leuy schulen brynge the firste fruytis of wheete, of wiyn, and of oile; and halewid vessels schulen be there, and prestis, and syngeris, and porteris, and mynystris; and we schulen not forsake the hows of `oure God.
Choncho Israeli, kuphatikiza zidzukulu za Alevi, azipititsa zopereka za tirigu, vinyo ndi mafuta ku zipinda zosungiramo katundu wopatulika, komanso kokhala ansembe amene akutumikira pamodzi ndi alonda a ku Nyumba ya Mulungu ndi anthu oyimba nyimbo. “Kwambiri ife sitidzaleka kusamala Nyumba ya Mulungu.”