< Exodus 36 >

1 Therfor Beseleel, and Ooliab, and ech wijs man, to whiche the Lord yaf wisdom and vndurstondyng, that thei kouden worche crafteli, maden thingis that weren nedeful in to vsis of seyntuarie, and whiche the Lord comaundide to be maad.
Choncho Bezaleli, Oholiabu pamodzi ndi anthu aluso onse amene Yehova anawapatsa luso ndi nzeru zodziwira kupanga zofunika zonse zomangira malo opatulika, adzapanga zonse iwowo, monga momwe Yehova analamulira.”
2 And whanne Moises hadde clepid hem, and ech lerned man, to whom the Lord hadde youe wisdom and kunnyng, and whiche profriden hem bi her wille to make werk,
Ndipo Mose anayitana Bezaleli ndi Oholiabu ndiponso munthu aliyense waluso amene Yehova anamupatsa luso ndiponso amene anali ndi mtima wofuna kugwira ntchito.
3 he bitook to hem alle the yiftis of the sones of Israel. And whanne thei weren bisi in the werk ech dai, the puple offride auowis eerli.
Iwo analandira kuchokera kwa Mose zopereka zonse Aisraeli anabweretsa kuti agwirire ntchito yomanga malo wopatulika. Ndipo anthu anapitirira kupereka zopereka zaufulu mmawa uliwonse.
4 Wherfor the werkmen weren compellid to come,
Kotero amisiri onse amene amagwira ntchito yonse ya malo wopatulika anasiya ntchitoyo
5 and thei seiden to Moises, The puple offrith more than is nedeful.
ndipo anati kwa Mose, “Anthu akubweretsa kuposa zimene zikufunika kugwirira ntchito imene Yehova analamulira kuti ichitike.”
6 Therfor Moises comaundide to be cried bi the vois of a criere, Nether man nether womman offre more ony thing in the werk of seyntuarie; and so it was ceessid fro yiftis to be offrid, for the thingis offrid sufficiden,
Choncho Mose analamulira ndipo analengeza mu msasa onse, “Mwamuna kapena mayi aliyense asaperekenso chopereka chilichonse cha ku malo wopatulika.” Choncho anthu analetsedwa kubweretsa zambiri,
7 and weren ouer abundant.
chifukwa zimene anali nazo zinali zoposera zimene zimafunika kugwirira ntchito yonse.
8 And alle wise men in herte to fille the werk of the tabernacle maden ten curteyns of bijs foldid ayen, and of iacynct, and purpur, and of reed selk twies died, bi dyuerse werk, and bi the craft of many colouris.
Anthu onse aluso pakati pa anthu ogwira ntchitoyo anapanga chihema pogwiritsa ntchito nsalu khumi zofewa, zosalala ndi zolukidwa bwino, zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Ndipo anthu aluso anapeta pa nsaluzo Akerubi.
9 Of whiche curteyns oon hadde in lengthe eiyte and twenti cubitis, and foure cubitis in breede; o mesure was of alle curteyns.
Nsalu zonse zinali zofanana. Mulitali mwake zinali mamita khumi ndi atatu, mulifupi mamita awiri.
10 And he ioynede fyue curteyns oon to anothir, and he couplide othere fyue to hem silf to gidere;
Iwo analumikiza nsalu zisanu, kuti ikhale nsalu imodzi ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu zisanu zinazo.
11 and he made handlis of iacynt in the hemme of o curteyn on euer either side,
Kenaka anapanga zokolowekamo za nsalu yobiriwira mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsiriza ya mbali ina. Ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu yotsiriza ya mbali inayo.
12 and in lijk maner in the hemme of the tother curteyn, that the handlis schulen comen to gidere ayens hem silf, and schulen be ioyned togider;
Iwo anasokerera zokolowekamo makumi asanu pa nsalu yoyamba ndi zokolowekamo makumi asanu zinanso pa nsalu inayo. Anapanga kuti zokolowekamozo ziziyangʼanana.
13 wherfor he yettide also fifti goldun serclis, that schulen `bite the handlis of curteyns; and o tabernacle was maad.
Kenaka anapanga ngowe zagolide 50 zolumikizira nsalu ziwirizo kotero kuti zinapanga chihema chimodzi.
14 `He made also enleuene saies of the heeris of geet, to hile the roof of the tabernacle;
Iwo anapanga nsalu za ubweya wambuzi zophimba pamwamba pa chihemacho. Nsalu zonse pamodzi zinalipo khumi ndi imodzi.
15 o saie hadde thretti cubitis in lengthe, foure cubitis in breede; alle the saies weren of o mesure;
Nsalu zonse khumi ndi imodzi zinali zofanana. Mulitali mwake munali mamita khumi ndi anayi ndipo mulifupi mwake munali mamita awiri.
16 of whiche saies he ioynede fyue bi hem silf, and sixe othere bi hem silf.
Iwo analumikiza nsalu zisanu kukhala nsalu imodzi ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, analumikizanso kukhala nsalu imodzinso.
17 And he made fifti handlis in the hemme of o say, and fifti in the hemme of the tother say, that tho schulden be ioyned to hem silf to gidere; and he made fifti bokelis of bras bi whiche
Kenaka anasokerera zokolowekamo makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsirizira ya nsalu yoyamba yolumikiza ija ndiponso anapanga zokolowekamo zina makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu yotsirizira ya nsalu inanso yolumikiza ija.
18 the roof was fastned to gidere, that oon hilyng were maad of alle the saies.
Iwo anapanga ngowe 50 zamkuwa zolowetsa mu zokolowekazo ndipo anaphatikiza nsalu ziwirizo kuti tentiyo ikhale imodzi.
19 He made also an hilyng of the tabernacle of the skynnes of rammes maad reed, and another veil aboue of skynnes of iacynt.
Ndipo anapanga chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake anapanganso chophimbira china cha zikopa za akatumbu.
20 He made also stondynge tablis of the tabernacle of the trees of Sechym;
Iwo anapanga maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.
21 the lengthe of o table was of ten cubitis, and the breede helde o cubit and an half.
Feremu iliyonse inali yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake munali masentimita 69.
22 Twey dentyngis weren bi ech table, that the oon schulde be ioyned to the tother; so he made in al the tablis of the tabernacle.
Thabwa lililonse linali ndi zolumikizira ziwiri. Iwo anapanga maferemu onse a chihemacho ndi matabwa otere.
23 Of whiche tablis twenti weren at the mydday coost ayens the south,
Anapanga maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho,
24 with fourti foundementis of siluer; twey foundementis weren set vndur o table on euer either side of the corneris, where the dentyngis of the sidis weren endid in the corneris.
ndiponso anapanga matsinde 40 asiliva ndipo anawayika pansi pa maferemuwo. Pansi pa feremu iliyonse anayika matsinde awiri ogwiriziza zolumikizira ziwiri zija.
25 And at the coost of the tabernacle that biholdith to the north he made twenti tablis,
Iwo anapanganso maferemu makumi awiri a mbali yakumpoto ya chihemacho,
26 with fourti foundementis of siluer, twei foundementis bi ech table.
ndiponso matsinde makumi anayi asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.
27 Forsothe ayens the west he made sixe tablis,
Anapanganso maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo,
28 and tweyne othere tablis bi ech corner of the tabernacle bihinde,
ndiponso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.
29 whiche weren ioyned fro bynethe til to aboue, and weren borun in to o ioynyng to gidere; so he made on euer either part bi the corneris,
Pa ngodya ziwirizi panali maferemu awiri, kuyambira pansi mpaka pamwamba atalumikizidwa pa ngowe imodzi. Maferemu onse anali ofanana.
30 that tho weren eiyte tablis to gidere, and hadden sixtene foundementis of siluer, that is, twei foundementis vndur ech table.
Choncho panali maferemu asanu ndi atatu ndiponso matsinde 16 asiliva, awiri anali pansi pa feremu iliyonse.
31 He made also barris of the trees of Sechym, fyue barris to holde to gidere the tablis of o side of the tabernacle,
Iwo anapanganso mitanda ya matabwa amtengo wa mkesha. Mitanda isanu inali ya maferemu a mbali imodzi ya chihema,
32 and fyue othere barris to schappe to gidere the tablis of the tother side; and without these, he made fyue othere barris at the west coost of the tabernacle ayens the see.
mitanda isanu inanso inali ya maferemu a mbali inayo ndipo mitanda ina isanu ya mbali yakumadzulo, kumapeto kwenikweni kwa chihema.
33 He made also another barre, that schulde come bi the myddil tables fro corner til to corner.
Anapanga mtanda wapakati omwe umachokera pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.
34 Forsothe he ouergildide tho wallis of tablis, and yetide the siluerne foundementis `of tho, and he made the goldun serclis `of tho, bi whiche the barris myyten be brouyt in, and be hilide the same barris with goldun platis.
Iwo anakuta maferemuwo ndi golide ndiponso anapanga mphete zagolide zogwiriziza mitandayo. Ndipo mitandayonso anayikuta ndi golide.
35 He made also a veil dyuerse and departid, of iacynt, and purpur, and reed selk, and bijs foldid ayen bi werk of broiderie.
Anapanga nsalu yokhala ndi mtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira ndipo nsaluyo inali yolukidwa bwino, yofewa ndi yosalala. Ndipo anthu aluso anapetapo zithunzi za Akerubi.
36 He made also foure pileris of `the trees of Sechym, whyche pileris with the heedis he ouergildide, and yetide the siluerne foundementis `of tho.
Iwo anapanga nsanamira zinayi zamtengo wa mkesha zokutidwa ndi golide. Anapanganso ngowe zagolide za nsanamirazo ndi matsinde asiliva anayi.
37 He made also in the entryng of the tabernacle a tent of iacynt, and purpur, and reed selk `and bijs foldid ayen bi the werk of a broydreie.
Anapanga nsalu ya pa chipata cholowera mu chihema, yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira yomwe inali yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso.
38 And he made fyue pileris with her heedis, whiche he hilide with gold, and he yetide the brasun foundementis `of tho, whiche he hilide with gold.
Anapanga nsanamira zisanu ndi ngowe zake. Anakuta pamwamba pa nsanamirazo ndi zomangira zake ndi golide, ndipo anapanganso matsinde asanu amkuwa.

< Exodus 36 >