< 1 Chronicles 25 >

1 Therfor Dauid, and the magestratis of the oost, departiden in to the seruyce the sones of Asaph, and of Eman, and of Idithum, whiche schulden profecye in harpis, and sawtrees, and cymbalis, bi her noumbre, and serue the office halewid to hem.
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Of the sones of Asaph; Zaccur, and Joseph, and Nathania, and Asarela; sotheli the sones of Asaph vndir the hond of Asaph profesieden bisidis the kyng.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Forsothe the sones of Idithum weren these; Idithum, Godolie, Sori, Jesie, and Sabaie, and Mathatie, sixe; vndur the hond of hir fadir Idithum, that profesiede in an harpe on men knoulechynge and preysynge the Lord.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Also the sones of Heman weren Heman, Boccia, Mathanya, Oziel, Subuhel, and Jerymoth, Ananye, Anan, Elyatha, Gaeldothi, and Romenthi, Ezer, and Jesbacasi, Melothy, Othir, Mazioth;
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 alle these sones of Heman weren profetis of the kyng in the wordis of God, that he schulde enhaunse the horn. And God yaf to Heman fourtene sones, and thre douytris.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Alle vndur the hond of her fadir weren `delid, ethir asigned, to synge in the temple of the Lord, in cymbalis, and sawtrees, and harpis, in to the seruyces of the hows of the Lord nyy the kyng, that is to seie, Asaph, and Idithum, and Heman.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Sotheli the noumbre of hem with her britheren, that tauyten the songe of the Lord, alle the techeris, was twey hundrid `foure scoor and eiyte.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 And thei senten lottis bi her whiles euenli, as wel the gretter as the lesse, also a wijs man and vnwijs.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 And the firste lot yede out to Joseph, that was of Asaph; the secounde to Godolie, to hym, and hise sones and hise britheren twelue;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 the thridde to Zaccur, to hise sones and hise bretheren twelue;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 the fourthe to Isary, to hise sones and hise britheren twelue; the fyuethe to Nathanye,
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 to hise sones and hise britheren twelue;
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 the sixte to Boccian, to hise sones and hise britheren twelue;
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 the seuenthe to Israhela, to hise sones and britheren twelue;
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 the eiythe to Isaie, to his sones and britheren twelue;
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 the nynthe to Mathany, to his sones and britheren twelue;
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 the tenthe to Semei, to his sones and britheren twelue;
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 the elleuenthe to Ezrahel, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 the tweluethe to Asabie, to his sones and britheren twelue;
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 the thrittenthe to Subahel, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 the fourtenthe to Mathathatie, to hise sones and britheren twelue; the fiftenthe to Jerymoth,
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 to hise sones and britheren twelue;
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 the sixtenthe to Ananye, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 the seuententhe to Jesbocase, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 the eiytenthe to Annam, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 the nyntenthe to Mollothi, to hise sones and britheren twelue; the twentithe to Eliatha,
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 to hise sones and britheren twelue;
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 the oon and twentithe to Othir, to hise sones and britheren twelue;
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 the two and twentithe to Godoliathi, to hise sones and britheren twelue; the thre and twentithe to Mazioth,
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 to hise sones and britheren twelue;
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 the foure and twentithe to Romonathiezer, to his sones and britheren twelue.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< 1 Chronicles 25 >