< Psalms 131 >

1 A Song of Ascents. By David. LORD, my heart isn’t arrogant, nor my eyes lofty; nor do I concern myself with great matters, or things too wonderful for me.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 Surely I have stilled and quieted my soul, like a weaned child with his mother, like a weaned child is my soul within me.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Israel, hope in the LORD, from this time forward and forever more.
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalms 131 >