< Psalms 82 >
1 God gathers all the [rulers and judges who think they are] gods for a meeting in heaven; and he tells them that he has decided this:
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
2 “You must [RHQ] stop judging [people] unfairly; you must no longer make decisions that favor wicked [people]!
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
3 You must defend [people who are] poor and orphans; you must act fairly toward those who are needy and those who have no one to help them.
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
4 Rescue them from the power [MTY] of evil [people] [DOU]!”
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
5 [Those rulers] do not know or understand anything! They are very corrupt/evil, and [as a result of their corrupt/evil behavior], [it is as though] the foundation of the world is being shaken!
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
6 I [the all-powerful God, previously] said to them, “You think you are gods! [It is as though] you are all my sons,
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
7 but you will die like people do; your lives will end, like the lives of all rulers end.”
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
8 God, arise and judge [everyone on] [MTY] the earth, because all the people-groups belong to you!
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.