< Psalms 131 >
1 Yahweh, I am not proud and I have not thought highly about (myself/the things that I have done). And I do not concern myself about things [that you have done] that are very big or very wonderful.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 Instead, I am calm and peaceful, like a [small] child who lies quietly in its mother’s arms [SIM]. In the same way, I am peaceful.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 You [my fellow] Israelis, confidently expect that Yahweh [will do good things for you], now and forever!
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.