< Psalms 128 >

1 (Happy are/Yahweh is pleased with) those of you who revere him and do what he wants you to do [IDM].
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake.
2 You will [be able to earn the money] that you [MTY] need to buy food; you will be happy and you will be prosperous.
Udzadya chipatso cha ntchito yako; madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3 Your wife will be like a grapevine that bears many grapes [SIM]; she will give birth to many children. Your children who sit around your table will be like a strong olive [tree that has many] shoots [growing up around it] [SIM].
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka mʼkati mwa nyumba yako; ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi kuzungulira tebulo lako.
4 Every man who reveres Yahweh will be blessed like that.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
5 I wish/hope that Yahweh will bless all of you from [where he dwells] (on Zion [Hill]/[in Jerusalem]) and that you will see [the people of] Jerusalem prospering every day that you live!
Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni masiku onse a moyo wako; uwone zokoma za Yerusalemu,
6 I desire that you will live many years, long enough to see your grandchildren. I desire/hope that things will go well for [the people in] Israel!
ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako. Mtendere ukhale ndi Israeli.

< Psalms 128 >