< Psalms 58 >

1 to/for to conduct Do Not Destroy Do Not Destroy to/for David Miktam truly silence righteousness to speak: promise [emph?] uprightness to judge son: child man
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide. Kodi inu olamulira mumayankhuladi molungama? Kodi mumaweruza mwachilungamo pakati pa anthu?
2 also in/on/with heart injustice to work [emph?] in/on/with land: country/planet violence hand your to envy [emph?]
Ayi, mʼmitima mwanu mumakonzekera zosalungama, ndipo manja anu amatulutsa zachiwawa pa dziko lapansi.
3 be a stranger wicked from womb to go astray from belly: womb to speak: speak lie
Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera; kuchokera mʼmimba ya amayi awo, iwo ndi otayika ndipo amayankhula mabodza.
4 rage to/for them like/as likeness rage serpent like cobra deaf to shutter ear his
Ululu wawo uli ngati ululu wa njoka, ngati uja wa mphiri imene yatseka mʼmakutu mwake.
5 which not to hear: hear to/for voice to whisper to unite spell be wise
Imene simva liwu la munthu wamatsenga, ngakhale akhale wa luso lotani munthu wamatsengayo.
6 God to overthrow tooth their in/on/with lip their tooth lion to tear LORD
Gululani mano mʼkamwa mwawo, Inu Mulungu, Yehova khadzulani mano a mikango!
7 to flow like water to go: went to/for them to tread (arrow his *Q(K)*) like to circumcise
Mulole kuti asowe ngati madzi oyenda pamene iwo akoka uta mulole kuti mivi yawo ikhale yosathwa.
8 like snail melting to go: continue miscarriage woman not to see sun
Akhale ngati nkhono imene imasungunuka pamene ikuyenda; ngati mwana wakufa asanabadwe, iwo asaone dzuwa.
9 in/on/with before to understand pot your bramble like alive like burning anger to storm him
Miphika yanu isanagwire moto waminga ya mkandankhuku, kaya iyo ndi yobiriwira kapena yowuma, oyipa adzachotsedwa.
10 to rejoice righteous for to see vengeance beat his to wash: wash in/on/with blood [the] wicked
Olungama adzasangalala poona kubwezera chilango, pamene adzasambitsa mapazi awo mʼmagazi a anthu oyipa.
11 and to say man surely fruit to/for righteous surely there God to judge in/on/with land: country/planet
Ndipo anthu adzanena kuti, “Zoonadi, olungama amalandirabe mphotho; zoonadi kuli Mulungu amene amaweruza dziko lapansi.”

< Psalms 58 >