< Numbers 31 >
1 and to speak: speak LORD to(wards) Moses to/for to say
Yehova anawuza Mose kuti,
2 to avenge vengeance son: descendant/people Israel from with [the] Midianite (after *L(P)*) to gather to(wards) kinsman your
“Uwabwezere zoyipa Amidiyani chifukwa cha zimene anachitira Aisraeli. Ukatha kuchita zimenezi, iwe udzamwalira.”
3 and to speak: speak Moses to(wards) [the] people to/for to say to arm from with you human to/for army: war and to be upon Midian to/for to give: put vengeance LORD in/on/with Midian
Ndipo Mose anati kwa Aisraeli, “Perekani zida kwa ena mwa anthu anu kuti akamenyane ndi Amidiyani ndi kuwabwezera choyipa mʼmalo mwa Yehova.
4 thousand to/for tribe thousand to/for tribe to/for all tribe Israel to send: depart to/for army: war
Mutumize ku nkhondoko amuna 1,000 kuchokera ku fuko lililonse la Aisraeli.”
5 and to commit from thousand Israel thousand to/for tribe two ten thousand to arm army: war
Choncho amuna okwana 12,000 anatenga zida kukonzekera nkhondo, anthu 1,000 kuchokera ku fuko lililonse la Aisraeli.
6 and to send: depart [obj] them Moses thousand to/for tribe to/for army: war [obj] them and [obj] Phinehas son: child Eleazar [the] priest to/for army: war and article/utensil [the] holiness and trumpet [the] shout in/on/with hand his
Mose anawatumiza ku nkhondo, anthu 1,000 kuchokera ku fuko lililonse pamodzi ndi Finehasi mwana wa Eliezara wansembe amene ananyamula zipangizo zochokera ku malo wopatulika ndi malipenga okaliza.
7 and to serve upon Midian like/as as which to command LORD [obj] Moses and to kill all male
Iwo anamenyana ndi Amidiyani monga momwe Yehova analamulira Mose ndipo anapha mwamuna aliyense.
8 and [obj] king Midian to kill upon slain: killed their [obj] Evi and [obj] Rekem and [obj] Zur and [obj] Hur and [obj] Reba five king Midian and [obj] Balaam son: child Beor to kill in/on/with sword
Mwa anthu ophedwawo munali Evi, Rekemu, Zuri, Huri ndi Reba, mafumu asanu a Amidiyani. Ndipo anaphanso ndi lupanga Balaamu mwana wa Beori.
9 and to take captive son: descendant/people Israel [obj] woman Midian and [obj] child their and [obj] all animal their and [obj] all livestock their and [obj] all strength: rich their to plunder
Aisraeli anagwira ukapolo amayi a Chimidiyani ndi ana awo ndipo analandanso ngʼombe, ziweto zawo zina zonse ndi katundu wawo yense.
10 and [obj] all city their in/on/with seat their and [obj] all encampment their to burn in/on/with fire
Anawotcha mizinda yonse imene Amidiyani ankakhalamo pamodzi ndi misasa yawo yonse.
11 and to take: take [obj] all [the] spoil and [obj] all [the] prey in/on/with man and in/on/with animal
Anatenga zonse zimene analanda ku nkhondoko, anthu ndi zoweta zomwe.
12 and to come (in): bring to(wards) Moses and to(wards) Eleazar [the] priest and to(wards) congregation son: descendant/people Israel [obj] [the] captivity and [obj] [the] prey and [obj] [the] spoil to(wards) [the] camp to(wards) Plains (of Moab) (Plains of) Moab which upon Jordan Jericho
Ndipo anabwera nawo akapolowo ndi zolanda ku nkhondozo kwa Mose ndi kwa wansembe Eliezara ndi kwa gulu lonse la Aisraeli ku misasa yawo ku chigwa cha Mowabu, mʼmbali mwa mtsinje wa Yorodani ku Yeriko.
13 and to come out: come Moses and Eleazar [the] priest and all leader [the] congregation to/for to encounter: meet them to(wards) from outside to/for camp
Mose, wansembe Eliezara ndi atsogoleri onse a gululo anapita kukakumana nawo kunja kwa misasa.
14 and be angry Moses upon to reckon: overseer [the] strength: soldiers ruler [the] thousand and ruler [the] hundred [the] to come (in): come from army: duty [the] battle
Mose anakwiya nawo akuluakulu a magulu a ankhondowo: olamulira 1,000 ndi olamulira 100, amene ankachokera ku nkhondo.
15 and to say to(wards) them Moses to live all female
Iye anafunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani mwawaleka amoyo amayi onsewa?”
16 look! they(fem.) to be to/for son: descendant/people Israel in/on/with word Balaam to/for to commit unfaithfulness in/on/with LORD upon word: thing Peor and to be [the] plague in/on/with congregation LORD
Paja iwo ndi amene ankatsatira uphungu wa Balaamu ndiponso ndi amene anachititsa Aisraeli kuti asiye Yehova pa zimene zinachitika ku Peori, kotero mliri unagwera anthu a Yehova.
17 and now to kill all male in/on/with child and all woman to know man to/for bed male to kill
Tsopano iphani munthu wamwamuna aliyense. Ndiponso iphani mayi aliyense amene anagonapo ndi mwamuna,
18 and all [the] child in/on/with woman which not to know bed male to live to/for you
koma sungani mtsikana aliyense amene sanagonepo ndi mwamuna.
19 and you(m. p.) to camp from outside to/for camp seven day all to kill soul: person and all to touch in/on/with slain: killed to sin in/on/with day [the] third and in/on/with day [the] seventh you(m. p.) and captivity your
“Inu nonse amene mwaphapo wina wake, kapena kukhudza aliyense amene anaphedwa mukhale kunja kwa msasa masiku asanu ndi awiri. Pa tsiku lachitatu mudziyeretse nokha pamodzi ndi akapolo anu.
20 and all garment and all article/utensil skin and all deed: work goat and all article/utensil tree: wood to sin
Muyeretsenso zovala zanu ndi china chilichonse chopangidwa ndi chikopa, ubweya wa mbuzi kapenanso ndi mtengo.”
21 and to say Eleazar [the] priest to(wards) human [the] army [the] to come (in): come to/for battle this statute [the] instruction which to command LORD [obj] Moses
Tsono wansembe Eliezara anati kwa asilikali amene anapita ku nkhondo aja, “Lamulo limene Yehova anapereka kwa Mose ndi ili:
22 surely [obj] [the] gold and [obj] [the] silver: money [obj] [the] bronze [obj] [the] iron [obj] [the] tin and [obj] [the] lead
Golide, siliva, mkuwa, chitsulo, chiwaya, mtovu
23 all word: thing which to come (in): come in/on/with fire to pass in/on/with fire and be pure surely in/on/with water impurity to sin and all which not to come (in): come in/on/with fire to pass in/on/with water
ndi china chilichonse chimene sichingapse ndi moto muchidutsitse pa moto, ndipo chidzayeretsedwa. Komanso chiyeretsedwe ndi madzi oyeretsa. Ndipo chilichonse chimene chingapse ndi moto muchidutsitse mʼmadzimo.
24 and to wash garment your in/on/with day [the] seventh and be pure and after to come (in): come to(wards) [the] camp
Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muchape zovala zanu ndipo mudzayera. Mukatero mutha kulowa mu msasa.”
25 and to say LORD to(wards) Moses to/for to say
Yehova anawuza Mose kuti,
26 to lift: count [obj] head: count prey [the] captivity in/on/with man and in/on/with animal you(m. s.) and Eleazar [the] priest and head: leader father [the] congregation
“Iwe ndi wansembe Eliezara ndiponso akuluakulu a mabanja a anthuwa, muwerenge anthu onse ndi ziweto zomwe zinagwidwa ku nkhondo.
27 and to divide [obj] [the] prey between to capture [the] battle [the] to come out: come to/for army: war and between all [the] congregation
Mugawe zolanda ku nkhondozo magawo awiri, lina la ankhondo amene anapita ku nkhondo, lina la anthu onse.
28 and to exalt tribute to/for LORD from with human [the] battle [the] to come out: come to/for army: war one soul: person from five [the] hundred from [the] man and from [the] cattle and from [the] donkey and from [the] flock
Pa gawo la ankhondowo, mutengeko gawo la Yehova, pa zofunkha 500 zilizonse mutengeko chimodzi, pa akapolo, ngʼombe, bulu ndi nkhosa.
29 from half their to take: take and to give: give to/for Eleazar [the] priest contribution LORD
Utenge zimenezo pa theka la gawo la ankhondowo ndipo upereke kwa wansembe Eliezara kuti zikhale zopereka zanu kwa Yehova.
30 and from half son: descendant/people Israel to take: take one to grasp from [the] fifty from [the] man from [the] cattle from [the] donkey and from [the] flock from all [the] animal and to give: give [obj] them to/for Levi to keep: guard charge tabernacle LORD
Kuchokera pa theka la gawo la Aisraeli, utengeko cholanda chimodzi pa makumi asanu aliwonse, pa anthu, ngʼombe, abulu, nkhosa, mbuzi kapena zoweta zina. Uzipereke kwa Alevi amene ntchito yawo ndi yosamalira tenti ya Yehova.”
31 and to make: do Moses and Eleazar [the] priest like/as as which to command LORD [obj] Moses
Ndipo Mose ndi wansembe Eliezara anachita monga Yehova analamulira Mose.
32 and to be [the] prey remainder [the] plunder which to plunder people: soldiers [the] army flock six hundred thousand and seventy thousand and five thousand
Zotsala pa zolanda ku nkhondo zimene ankhondowo anatenga zinali nkhosa 675,000,
33 and cattle two and seventy thousand
Ngʼombe 72,000,
34 and donkey one and sixty thousand
abulu 61,000,
35 and soul: person man from [the] woman which not to know bed male all soul: person two and thirty thousand
ndi atsikana omwe sanagonepo ndi mwamuna 32,000.
36 and to be [the] half portion [the] to come out: come in/on/with army number [the] flock three hundred thousand and thirty thousand and seven thousand and five hundred
Gawo la ankhondo amene anapita ku nkhondo linali: nkhosa 337,500,
37 and to be [the] tribute to/for LORD from [the] flock six hundred five and seventy
mwa zimenezi gawo la Yehova linali 675;
38 and [the] cattle six and thirty thousand and tribute their to/for LORD two and seventy
ngʼombe zinalipo 36,000 ndipo gawo la Yehova linali 72;
39 and donkey thirty thousand and five hundred and tribute their to/for LORD one and sixty
abulu analipo 30,500 ndipo gawo la Yehova linali 61;
40 and soul: person man six ten thousand and tribute their to/for LORD two and thirty soul: person
anthu analipo 16,000 ndipo gawo la Yehova linali 32.
41 and to give: give Moses [obj] tribute contribution LORD to/for Eleazar [the] priest like/as as which to command LORD [obj] Moses
Mose anapereka kwa wansembe Eliezara gawo limene linali loyenera kupereka kwa Yehova monga momwe Yehova analamulira Mose.
42 and from half son: descendant/people Israel which to divide Moses from [the] human [the] to serve
Pa gawo la Aisraeli, Mose anapatula theka limodzi kuchotsa pa zolanda ku nkhondo zonse zimene zinabwera ndi ankhondo aja.
43 and to be half [the] congregation from [the] flock three hundred thousand and thirty thousand seven thousand and five hundred
Tsono gawo la Aisraeli linali ili: nkhosa 337,500,
44 and cattle six and thirty thousand
ngʼombe 36,000,
45 and donkey thirty thousand and five hundred
abulu 30,500,
46 and soul: person man six ten thousand
anthu 16,000.
47 and to take: take Moses from half son: descendant/people Israel [obj] [the] to grasp one from [the] fifty from [the] man and from [the] animal and to give: give [obj] them to/for Levi to keep: guard charge tabernacle LORD like/as as which to command LORD [obj] Moses
Kuchoka pa gawo la Aisraelilo, Mose anatengapo chimodzi pa zolanda ku nkhondo makumi asanu aliwonse, anthu ndi nyama, ndipo anazipereka kwa Alevi amene ankayangʼanira tenti ya Yehova monga Yehova analamulira Mose.
48 and to present: come to(wards) Moses [the] to reckon: overseer which to/for thousand [the] army ruler [the] thousand and ruler [the] hundred
Pamenepo omwe ankayangʼanira magulu a ankhondo olamulira 1,000 ndi olamulira 100 anabwera kwa Mose,
49 and to say to(wards) Moses servant/slave your to lift: count [obj] head: leader human [the] battle which in/on/with hand: power our and not to reckon: missing from us man: anyone
iwo anati kwa iye, “Ife anthu anu tawerenga ankhondo amene timawalamulira. Palibe munthu ndi mmodzi yemwe amene wasowa.
50 and to present: bring [obj] offering LORD man: anyone which to find article/utensil gold armlet and bracelet ring ring and bracelet to/for to atone upon soul: myself our to/for face: before LORD
Ndipo tabweretsa zopereka kwa Yehova zimene munthu aliyense anapeza: ziwiya zagolide, zibangiri, zigwinjiri, mphete zosindikizira, ndolo ndi mikanda kuti tichitire mwambo wopepesera machimo pamaso pa Yehova.”
51 and to take: recieve Moses and Eleazar [the] priest [obj] [the] gold from with them all article/utensil deed: work
Ndipo Mose ndi wansembe Eliezara analandira kuchokera kwa atsogoleriwo golide pamodzi ndi zipangizo zonse zosula.
52 and to be all gold [the] contribution which to exalt to/for LORD six ten thousand seven hundred and fifty shekel from with ruler [the] thousand and from with ruler [the] hundred
Golide yense wochokera kwa atsogoleri a 1,000 ndi atsogoleri a 100 zomwe Mose ndi Eliezara anapereka ngati mphatso kwa Yehova zinali zolemera makilogalamu 200.
53 human [the] army to plunder man: anyone to/for him
Wankhondo aliyense anatenga zomwe analanda yekha ku nkhondo.
54 and to take: recieve Moses and Eleazar [the] priest [obj] [the] gold from with ruler [the] thousand and [the] hundred and to come (in): bring [obj] him to(wards) tent meeting memorial to/for son: descendant/people Israel to/for face: before LORD
Mose ndi Eliezara wansembe analandira golide kuchokera kwa atsogoleri a 1,000 ndi atsogoleri a 100 ndi kukamuyika mu tenti ya msonkhano ngati chikumbutso cha Aisraeli pamaso pa Yehova.