< Psalms 129 >
1 [the] song of The ascents much people have opposed me since youth my let it say please Israel.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,” anene tsono Israeli;
2 Much people have opposed me since youth my also not they have prevailed to me.
“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane.
3 On back my they have plowed plowmen they have made long (furrows their. *Q(K)*)
Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali:
4 Yahweh [is] righteous he has cut off [the] rope of wicked [people].
Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”
5 May they be ashamed and they may be turned back backward all [those who] hate Zion.
Onse amene amadana ndi Ziyoni abwezedwe pambuyo mwamanyazi.
6 May they be like [the] grass of roofs that before it has shot up it has withered.
Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule;
7 That not he has filled hand his a reaper and bosom his [one who] binds sheaves.
sungadzaze manja a owumweta kapena manja a omanga mitolo.
8 And not they say - those [who] pass by [the] blessing of Yahweh [be] to you we bless you in [the] name of Yahweh.
Odutsa pafupi asanene kuti, “Dalitso la Yehova lili pa inu; tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”