< Psalms 136 >

1 Give ye thanks to Yahweh, for he is good, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.
2 Give ye thanks to the God of gods, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Yamikani Mulungu wa milungu.
3 Give ye thanks to the Lord of lords, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Yamikani Ambuye wa ambuye,
4 To him that doeth great wonders, by himself alone, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,
5 To him that made the heavens with understanding, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,
6 To him that stretched out the earth above the waters, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,
7 To him that made great lights, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anapanga miyuni ikuluikulu,
8 The sun to rule the day, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Dzuwa lilamulire usana,
9 The moon and stars to rule the night, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,
10 To him that smote Egypt in their firstborn, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,
11 And brought forth Israel out of their midst, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Natulutsa Israeli pakati pawo,
12 With a firm hand, and a stretched-out arm, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,
13 To him that divided the Red Sea into division, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,
14 And caused Israel to pass through the midst thereof, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,
15 And shook off Pharaoh and his army in the Red Sea, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,
16 To him that led his people through the desert, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu
17 To him that smote great kings, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anakantha mafumu akuluakulu,
18 And slew majestic kings, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Napha mafumu amphamvu,
19 Even Sihon, king of the Amorites, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Siloni mfumu ya Aamori,
20 Also Og, king of Bashan, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Ogi mfumu ya Basani,
21 And gave their land for an inheritance, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Napereka dziko lawo ngati cholowa,
22 An inheritance to Israel his servant, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Cholowa cha mtumiki wake Israeli;
23 Who in our low estate, remembered us, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,
24 And freed us with force from our adversaries, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene anatimasula kwa adani athu,
25 Who giveth food to all flesh, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,
26 Give ye thanks unto the GOD of the heavens, For, age-abiding, is his lovingkindness.
Yamikani Mulungu wakumwamba,

< Psalms 136 >