< Jeremiah 45 >

1 The message that Jeremiah the prophet spoke to Baruch the son of Neriah, when he wrote these words in a scroll at the mouth of Jeremiah, in the fourth year of Jehoiakim the son of Josiah, king of Judah, saying,
Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku.
2 "Thus says YHWH, the God of Israel, to you, Baruch:
“Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti:
3 'You said, "Woe is me now. For YHWH has added sorrow to my pain; I am weary with my groaning, and I find no rest."'"
Iwe unati, ‘Kalanga ine! Yehova wawonjezera chisoni pa mavuto anga. Ine ndatopa ndi kubuwula ndipo sindikupeza mpumulo.’”
4 "You shall tell him, 'Thus says YHWH: "Look, that which I have built will I break down, and that which I have planted I will pluck up; and this in the whole land.
Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse.
5 Do you seek great things for yourself? Do not seek them; for, look, I will bring disaster on all flesh, says YHWH; but your life will I give to you for a reward in all places where you go."'"
Kodi tsono ukudzifunira wekha zinthu zazikulu? Usadzifunire. Pakuti ndidzagwetsa mavuto pa anthu onse, koma ndidzasunga moyo wako kulikonse kumene ungadzapite.”

< Jeremiah 45 >