< Psalms 131 >
1 “A song of the degrees by David.” O Lord, my heart was not haughty, nor were my eyes lofty: neither have I walked after matters too great, or those too wonderful for me.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 Surely I have pacified and stilled my soul, like the suckling on its mother's breast: like a suckling is in me my soul.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Let Israel wait for the Lord from this time forth and for ever more.
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.