< 1 Chronicles 25 >

1 Moreover David and the chief. officers of the army separated for the ministry the sons of Asaph, and of Heman, and of Idithun: to prophesy with harps, and with psalteries, and with cymbals according to their number serving in their appointed office.
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 Of the sons of Asaph: Zacchur, and Joseph, and Nathania, and Asarela, sons of Asaph: under the hand of Asaph prophesying near the king.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 And of Idithun: the sons of Idithun, Godolias, Serf, Jeseias, and Hasabias, and Mathathias, six, under the hand of their father Idithun, who prophesied with a harp to give thanks and to praise the Lord.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Of Heman also: the sons of Heman, Bocciau, Mathaniau, Oziel, Subuel, and Jerimoth, Hananias, Hanani, Eliatha, Geddelthi, and Romemthiezer, and Jesbacassa, Mellothi, Othir, Mahazioth:
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 All these were the sons of Heman the seer of the king in the words of God, to lift up the horn: and God gave to Heman fourteen sons and three daughters.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 All these under their father’s hand were distributed to sing in the temple of the Lord, with cymbals, and psalteries and harps, for the service of the house of the Lord near the king: to wit, Asaph, and Idithun, and Heman.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 And the number of them with their brethren, that taught the song of the Lord, all the teachers, were two hundred and eighty-eight,
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 And they cast lots by their courses, the elder equally with the younger, the learned and the unlearned together.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 And the first lot came forth to Joseph, who was of Asaph. The second to Godolias, to him and his sons, and his brethren twelve.
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 The third to Zachur, to his sons and his brethren twelve.
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 The fourth to Isari, to his sons and his brethren twelve.
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 The fifth to Nathania, to his sons and his brethren twelve.
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 The sixth to Bocciau, to his sons and his brethren twelve.
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 The seventh to Isreela, to his sons and his brethren twelve.
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 The eighth to Jesaia, to his sons and his brethren twelve.
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 The ninth to Mathanaias, to his sons and his brethren twelve.
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 The tenth to Semeias, to his sons and his brethren twelve.
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 The eleventh to Azareel, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 The twelfth to Hasabia, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 The thirteenth to Subael, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 The fourteenth to Mathathias, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 The fifteenth to Jerimoth, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 The sixteenth to Hananias, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 The seventeenth to Jesbacassa, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 The eighteenth to Hanani, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 The nineteenth to Mellothi, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 The twentieth to Eliatha, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 The one and twentieth to Othir, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 The two and twentieth to Geddelthi, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 The three and twentieth to Mahazioth, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 The four and twentieth to Romemthiezer, to his sons and his brethren twelve.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< 1 Chronicles 25 >