< Psalms 131 >

1 A Song of Degrees. O Lord, my heart is not exalted, neither have mine eyes been [haughtily] raised: neither have I exercised myself in great [matters], nor in things too wonderful for me.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Davide. Inu Yehova, mtima wanga siwodzikuza, maso anga siwonyada; sinditengeteka mtima ndi zinthu zapamwamba ndi zodabwitsa.
2 [I shall have sinned] if I have not been humble, but have exulted my soul: according to [the relation of] a weaned child to his mother, so wilt thou recompense my soul.
Koma moyo wanga ndawutontholetsa ndi kuwukhalitsa chete ngati mwana amene amayi ake amuletsa kuyamwa, moyo wanga mʼkati mwanga uli ngati mwana amene amuletsa kuyamwa.
3 Let Israel hope in the Lord, from henceforth and for ever.
Yembekeza Yehova, iwe Israeli, kuyambira tsopano mpaka muyaya.

< Psalms 131 >