< Psalmen 150 >

1 Hallelujah! Looft God in Zijn heiligdom; looft Hem in het uitspansel Zijner sterkte!
Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
2 Looft Hem vanwege Zijn mogendheden; looft Hem naar de menigvuldigheid Zijner grootheid!
Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
3 Looft Hem met geklank der bazuin; looft Hem met de luit en met de harp!
Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
4 Looft Hem met de trommel en fluit; looft Hem met snarenspel en orgel!
Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
5 Looft Hem met hel klinkende cimbalen; looft Hem met cimbalen van vreugdegeluid! (questioned)
Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
6 Alles, wat adem heeft, love den HEERE! Hallelujah!
Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.

< Psalmen 150 >