< Psalmen 115 >

1 Niet ons, o HEERE! niet ons, maar Uw Naam geef eer, om Uwer goedertierenheid, om Uwer waarheid wil.
Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi koma ulemerero ukhale pa dzina lanu, chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika ndiponso chifukwa cha kukhulupirika kwanu.
2 Waarom zouden de heidenen zeggen: Waar is nu hun God?
Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti, “Mulungu wawo ali kuti?”
3 Onze God is toch in den hemel, Hij doet al wat Hem behaagt.
Mulungu wathu ali kumwamba; Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa.
4 Hunlieder afgoden zijn zilver en goud, het werk van des mensen handen;
Koma mafano awo ndi siliva ndi golide, opangidwa ndi manja a anthu.
5 Zij hebben een mond, maar spreken niet; zij hebben ogen, maar zien niet;
Pakamwa ali napo koma sayankhula, maso ali nawo koma sapenya;
6 Oren hebben zij, maar horen niet; zij hebben een neus, maar zij rieken niet;
makutu ali nawo koma samva, mphuno ali nazo koma sanunkhiza;
7 Hun handen hebben zij, maar tasten niet; hun voeten, maar gaan niet; zij geven geen geluid door hun keel.
manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu; mapazi ali nawo koma sayenda; kapena pakhosi pawo kutulutsa mawu.
8 Dat die hen maken hun gelijk worden, en al wie op hen vertrouwt.
Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo, chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo.
9 Israel! vertrouw gij op den HEERE; Hij is hun Hulp en hun Schild.
Inu Aisraeli, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
10 Gij huis van Aaron! vertrouw op den HEERE; Hij is hun Hulp en hun Schild.
Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova; Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.
11 Gijlieden, die den HEERE vreest! vertrouwt op den HEERE; Hij is hun Hulp en hun Schild.
Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
12 De HEERE is onzer gedachtig geweest, Hij zal zegenen; Hij zal het huis van Israel zegenen, Hij zal het huis van Aaron zegenen.
Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israeli, adzadalitsa nyumba ya Aaroni,
13 Hij zal zegenen, die den HEERE vrezen, de kleinen met de groten.
adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova; aangʼono ndi aakulu omwe.
14 De HEERE zal den zegen over ulieden vermeerderen, over ulieden en over uw kinderen.
Yehova akuwonjezereni madalitso; inuyo pamodzi ndi ana anu.
15 Gijlieden zijt den HEERE gezegend, Die den hemel en de aarde gemaakt heeft.
Mudalitsidwe ndi Yehova, Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
16 Aangaande den hemel, de hemel is des HEEREN; maar de aarde heeft Hij den mensenkinderen gegeven.
Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.
17 De doden zullen den HEERE niet prijzen, noch die in de stilte nedergedaald zijn.
Si anthu akufa amene amatamanda Yehova, amene amatsikira kuli chete;
18 Maar wij zullen den HEERE loven van nu aan tot in der eeuwigheid. Hallelujah!
ndi ife amene timatamanda Yehova, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Yehova.

< Psalmen 115 >