< Psalmen 87 >

1 Een psalm van de zonen van Kore; een lied. Zijn stichting op de heilige bergen Heeft Jahweh lief;
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 De poorten van Sion nog meer Dan alle woonsteden van Jakob!
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Heerlijke dingen zegt Hij van u, Stad van God:
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Ik zal Ráhab en Babel tellen Bij mijn belijders; Zie, Filistea, Tyrus en Koesj; Hier zijn ze geboren!
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 Ja, van Sion zal men eens zeggen: "Man voor man is daar geboren!" En de Allerhoogste zal het bevestigen,
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Jahweh het schrijven In het boek van de volkeren: "Hier zijn ze geboren!"
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Dan zullen ze allen in reidans zingen: "In U is mijn woning!"
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Psalmen 87 >