< Psalmen 120 >

1 Een bedevaartslied. Tot Jahweh riep ik in mijn nood, En Hij heeft mij verhoord.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Verlos mij, Jahweh, van leugenlippen En lastertongen!
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Wat kan een lastertong u al brengen, En wat er nog bij doen:
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Scherpgepunte oorlogspijlen, Met gloeiende houtskool!
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Wee mij, dat ik moet toeven In de tenten van Mésjek, En dat ik moet wonen In de tenten van Kedar!
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Reeds te lang leef ik samen Met vredeverstoorders;
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Als ìk over vrede wil spreken, Zoeken zij strijd!
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

< Psalmen 120 >