< Zekaria 5 >

1 Ne atingʼo wangʼa kendo, mi napo ka aneno kalatas mafuyo e kor yamo!
Ndinayangʼananso ndipo taonani ndinaona chikalata chimene chimawuluka.
2 Nopenja niya, “En angʼo mineno?” Ne adwoke niya, “Kalatas mafuyo e kor yamo, ma borne oromo fut piero ochiko gaboro, to lachne fut piero angʼwen gochiko.”
Mngelo uja anandifunsa kuti, “Kodi ukuona chiyani?” Ndinayankha kuti, “Ndikuona chikalata chikuwuluka, mulitali mwake mamita asanu ndi anayi ndipo mulifupi mwake mamita anayi ndi theka.”
3 Eka nowachona niya, “Ma e kwongʼ madhi e piny duto; nikech mana kaka owacho e bathe konchiel, jokwoge duto ibiro negi kendo kaluwore gi gima owacho e bathe komachielo, joma kwongʼore gi miriambo, bende ibiro negi.
Ndipo mngeloyo anandiwuza kuti, “Awa ndi matemberero amene akupita pa dziko lonse lapansi; potsata zimene zalembedwa mʼkati mwa chikalatamo, aliyense wakuba adzachotsedwa, ndipo potsata zomwe zalembedwa kunja kwake, aliyense wolumbira zabodza adzachotsedwanso.
4 Jehova Nyasaye Maratego wacho ni, ‘Abiro ore mondo odonji e od jakuo kendo e od ngʼat makwongʼore gi miriambo gi nyinga. Kwongʼno nosik e udigo matiekgi nyaka kite mogerego duto.’”
Yehova Wamphamvuzonse akunena kuti, ‘Temberero limeneli ndidzalitumiza, ndipo lidzalowa mʼnyumba ya munthu wakuba ndi munthu wolumbira zabodza mʼdzina langa. Lidzakhala mʼnyumbamo mpaka kuyiwonongeratu, matabwa ake ndi miyala yake yomwe.’”
5 Eka malaika mane loso koda nosudo machiegni mowachona niya, “Tingʼ wangʼi malo mondo ine gima bironi, ni en angʼo?”
Kenaka mngelo amene amayankhula nane uja anabwera patsogolo panga ndipo anandiwuza kuti, “Kweza maso ako tsopano kuti uwone kuti ndi chiyani chikubwerachi.”
6 Napenjo niya, “En angʼo?” To nodwoka niya, “En atonga mar pimo mopongʼ gi richo mag ji e piny ngima.”
Ndinafunsa kuti, “Kodi chimenechi nʼchiyani?” Mngeloyo anayankha kuti, “Limeneli ndi dengu loyezera.” Ndipo anawonjezera kunena kuti, “Umenewu ndi uchimo wa anthu mʼdziko lonse.”
7 Apoya nono raumne mapek mar chuma noel kendo ne aneno dhako moro kobet piny ei atongano!
Pamenepo chovundikira chake chamtovu chinatukulidwa, ndipo mʼdengumo munali mutakhala mkazi.
8 Malaika nowacho niya, “Ma en richo.” Omiyo nodhiro dhakono kodwoko ei atonga mi noumo dho atongano gi raum mapekno.
Mngeloyo anati, “Chimenechi ndi choyipa,” ndipo anamukankhira mkaziyo mʼdengu muja, nabwezera chovundikira chamtovu chija pamwamba pake.
9 Eka natingʼo wangʼa, mi napo kaneno mon ariyo ka huyo e kor yamo. Ne gin gi bwombe ariyo machalo gi mag nyamnaha, kendo negikawo atonga mi gidhigo e kor polo malo.
Kenaka ndinayangʼananso, ndipo ndinaona akazi awiri akuwuluka kubwera kumene kunali ine; akuwuluzika ndi mphepo. Iwo anali ndi mapiko ngati a kakowa, ndipo ananyamula dengu lija, kupita nalo pakati pa mlengalenga ndi dziko lapansi.
10 Napenjo malaika mane loso koda niya, “Gitero atongano kanye?”
Ine ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane kuti, “Dengulo akupita nalo kuti?”
11 Nodwoka niya, “Gitere e piny Babulon mondo gigerne ot kuno. Ka odno oseikore, to noket atongano kare moselosne kanyo.”
Iye anayankha kuti, “Ku dziko la Babuloni kuti akalimangire nyumba. Nyumbayo ikadzatha, adzayikamo dengulo.”

< Zekaria 5 >