< Zaburi 86 >

1 Lemo mar Daudi. Winj lamona, yaye Jehova Nyasaye, kendo dwoka, nimar adhier kendo achando.
Pemphero la Davide. Ndimvereni Yehova ndipo mundiyankhe, pakuti ndine wosauka ndi wosowa.
2 Rit ngimana, nikech achiworani. In e Nyasacha, omiyo res ngima jatichni, mogeno kuomi.
Yangʼanirani moyo wanga, pakuti ndine wodzipereka kwa Inu. Inu ndinu Mulungu wanga; pulumutsani mtumiki wanu amene amadalira Inu. Inu ndinu Mulungu wanga.
3 Kecha, yaye Ruoth Nyasaye, nimar aywakni odiechiengʼ duto.
Mundichitire chifundo, Inu Ambuye, pakuti ndikuyitana Inu tsiku lonse.
4 Mi jatichni obed mamor, yaye Ruoth Nyasaye, nimar in ema aketo genona kuomi.
Bweretsani chimwemwe kwa mtumiki wanu, Ambuye, pakuti ndimadalira Inu.
5 Nikech in iber kendo iweyo richo, yaye Ruoth Nyasaye in gihera mangʼeny kuom joma luongi.
Inu Ambuye, ndinu wokhululuka ndi wabwino, wodzaza ndi chikondi kwa onse amene amayitana Inu.
6 Winj lamona, yaye Jehova Nyasaye; chik iti ne ywakna ma akwayigo kech.
Yehova imvani pemphero langa; mvetserani kulira kwanga kofuna chifundo.
7 Chiengʼ ma chandruok omaka to abiro luongi mondo ikonya, nimar ibiro dwoka.
Pa tsiku la mavuto anga ndidzayitana Inu, pakuti Inu mudzandiyankha.
8 Onge nyasaye moro amora e dier nyiseche machalo kodi, yaye Ruoth Nyasaye; onge timbe minyalo pimo gi magi.
Pakati pa milungu palibe wina wofanana nanu Ambuye; palibe ntchito zolingana ndi ntchito zanu.
9 Ogendini duto michweyo biro lami kapodho e nyimi, yaye Ruoth Nyasaye; bende gibiro miyo nyingi duongʼ.
Mitundu yonse ya anthu imene munayipanga idzabwera ndi kudzalambira pamaso panu Ambuye; iwo adzabweretsa ulemerero pa dzina lanu.
10 Nimar iduongʼ kendo itimo timbe miwuoro; in e Nyasaye kende.
Pakuti ndinu wamkulu ndipo mumachita zodabwitsa; Inu nokha ndiye Mulungu.
11 Puonja yoreni, yaye Jehova Nyasaye, mondo eka awuothi e adierani; miya chuny ma ok ba koni gi koni, mondo omi aluor nyingi.
Ndiphunzitseni njira yanu Yehova, ndipo ndidzayenda mʼchoonadi chanu; patseni mtima wosagawikana kuti ndilemekeze dzina lanu.
12 Abiro paki gi chunya duto, yaye Ruoth Nyasacha, abiro miyo nyingi duongʼ nyaka chiengʼ.
Ndidzakutamandani Ambuye Mulungu wanga, ndi mtima wanga wonse; ndidzalemekeza dzina lanu kwamuyaya.
13 Nimar (hera) ma iherago duongʼ, kendo isegola ei chuny bur matut. (Sheol h7585)
Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu kwa ine; mwandipulumutsa ku malo ozama a manda. (Sheol h7585)
14 Josunga ma wengegi tek monja, yaye Nyasaye; migawo mar joma ok kech ngʼato dwaro tieko ngimana, joma ok dew kata in.
Inu Mulungu wanga, anthu odzikuza akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufuna kundipha, amene salabadira za Inu.
15 In to in Nyasaye ma kecho kendo ngʼwon, yaye Jehova Nyasaye, iyi ok wangʼ piyo, ipongʼ gihera kendo in ja-adiera.
Koma Ambuye ndinu Mulungu wachifundo ndi wokoma mtima, wosakwiya msanga, wodzaza ndi chikondi ndi wokhulupirika.
16 Duog ira mondo ikecha; med jatichni tekoni, kendo res jatichni mogeni.
Tembenukirani kwa ine ndipo ndichitireni chifundo; perekani mphamvu zanu kwa mtumiki wanu ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu.
17 Miyae ranyisi mar berni, mondo wasika one mi wigi okuodi, nimar in ema isebedo ka ikonya kendo ihoya, yaye Jehova Nyasaye.
Mundionetse chizindikiro cha ubwino wanu kuti adani achione ndi kuchititsidwa manyazi, pakuti Yehova mwandithandiza ndi kunditonthoza.

< Zaburi 86 >